Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 258 MWA ine, moyo wanga ndi Yesu

  1. Home   »  
  2. Hymn 258 MWA ine, moyo wanga ndi Yesu

Hymn 258 MWA ine, moyo wanga ndi Yesu

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 258 MWA ine, moyo wanga ndi Yesu

 

MWA ine, moyo wanga ndi Yesu
(Yesu) Yemwe anafera ine,
Ndiye anandiwombola;
Yesu, Yesu.

Mwazi wake ndi chitsime changa,
(Yesu) Pamene ndikasambamo
Zochimwa zanga zidzatha;
Yesu, Yesu.

Yesu Mfumu, ine ndingadzafe
(Yesu) ngati mundisiya ndekha,
Kukhala ndekha sinditha;
Yesu, Yesu.

Yesu Mfumu, ine ndisekere
(Yesu) Inu Mpulumutsi wanga
Pamene mukhala nane;
Yesu, Yesu.

Post navigation

Previous: Hymn 257 NJIRA yanga sindiziŵa,
Next: Hymn 259 CHISOMO chodabwitsacho,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 373 Ayamikire ‘Nu
  • Hymn 294 Yesu anali khanda
  • Hymn 802 Ndife anthu aulendo,
  • Hymn 329 Yesu atonthoza mtima
  • Hymn 105 Tiyamike Mbuye Yesu
  • Hymn 983 Nkhondo ya Satana
  • Hymn 990 Poyesedwa ine
  • Hymn 525 Afike masiku
  • Hymn 351 CHIYEMBEKEZO changacho,
  • Hymn 520 Tamva tikondane naye,
  • Hymn 478 Ndife ana, mutikonda,
  • Hymn 1341 Tadza kukudyaku,
  • Hymn 656 Ndipumulire panupo,
  • Hymn 501 Yesu andikonda ine;
  • Hymn 1788 Mtimanga, bwera kuti upumule
  • Hymn 254 PAMENE ndisawuka,
  • Hymn 413 Yesu ndiye Bwenzi lathu,
  • Hymn 1770 Iye amazichita zamphamvu
  • Hymn 833 Mundilimbitse ndikayese manda ngati mphasayi,
  • Hymn 2 Ndinu wakuyera!
  • Hymn 1652 Mabala ajawo
  • Hymn 185 Kondwani nonsenu,
  • Hymn 1843 Chigwa choopsacho cha imfa ndikachilowera,
  • Hymn 1601 Zina za Yesu ndimvetu,
  • Hymn 363 Funani Mlungu tsopano,
  • Hymn 1072 Mudzaze Yesu mtima wanga ndi chikondicho,
  • Hymn 1740 Yesu, ndi chifundo chanu
  • Hymn 1093 Odala ndi onsewo
  • Hymn 910 Nlokoma Dziko langa!
  • Hymn 279 MBUYE, nditsate bwanjiko?
  • Hymn 923 Dothili kudothilo,
  • Hymn 403 Dzuwa liwala, m’tulotu
  • Hymn 181 Zonse ndinakonda kale
  • Hymn 371 Mulungu, anthu ‘fe
  • Hymn 157 Mbuye, Mzimu Woyera
  • Hymn 534 Bwerani, kondwerani,
  • Hymn 1184 Akondwerera nthawiyi
  • Hymn 426 Mpulumutsi Yesu,
  • Hymn 1394 Paphiri ndi padambo
  • Hymn 143 KONZA mtima iwe mbale,
  • Hymn 704 Monga tilandira, Mbuye,
  • Hymn 39 MUNASIYATU dziko lanulo,
  • Hymn 1833 Podwala ine pobvutidwa Andisamalira;
  • Hymn 312 NDIMAYENDA paulendo
  • Hymn 214 Msanga adzachitseka chitseko,
  • Hymn 180 MALO alimo m’nyumba ya Yesu,
  • Hymn 182 Kondwani nonsenu,
  • Hymn 122 KUNALI munthu wa Mlungu,
  • Hymn 1293 Chitsimecho cha mwaziwo
  • Hymn 88 Yesu, dzina lakukonda,
  • Hymn 838 E, tsiku lonse Inu ndifunitsa;
  • Hymn 64 LERO Kristu anauka,
  • Hymn 297 Anapita nasiya
  • Hymn 1485 Unachimwachimwa ndithu,
  • Hymn 198 CHITSIMECHO cha mwaziwo
  • Hymn 1121 Ndifuna Yesuyo,
  • Hymn 1203 Zambiri zangazo
  • Hymn 527 Idzani mumtima mwanga,
  • Hymn 114 Ndine Mbusayo wabwino,
  • Hymn 32 Tamandani Mbuye,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version