Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 64 LERO Kristu anauka,

  1. Home   »  
  2. Hymn 64 LERO Kristu anauka,

Hymn 64 LERO Kristu anauka,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 64 LERO Kristu anauka,

 

LERO Kristu anauka,
Aleluya.
Ndilo tsiku lokondwera.
Aleluya.
Iye kale anafera,
Aleluya.
Nawombola otaika,
Aleluya.

Timwimbire zomtamanda
Aleluya.
Ndiye Kristu wa Kumwamba
Aleluya.
Natsikira kumanda,
Aleluya.
Nalanditsa akuipa.
Aleluya

Koma masauko ake,
Aleluya.
Anatiwombola ife.
Aleluya.
Ndiye Mfumu ya mafumu,
Aleluya.
Mwana ndithu wa Mulungu.
Aleluya.

Timwimbire Mulungu wathu,
Aleluya.
Kuti atikonda ndithu:
Aleluya.
Mtamenso angelo inu,
Aleluya.
Ndiye ‘Tate, Mwana, Mzimu
Aleluya.

Post navigation

Previous: Hymn 63 POKUMBUKIRA mtandawo
Next: Hymn 65 NLA Mlungu dzuŵali:

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 953 Ichi chindisangalatsa
  • Hymn 542 Kuli kaphiri m’talimo
  • Hymn 1611 Nadzuka m’mandamo
  • Hymn 758 Sindili woyenera ‘ne;
  • Hymn 1079 Khalatu woyera,
  • Hymn 1357 Mlemekeze, anakonda
  • Hymn 257 NJIRA yanga sindiziŵa,
  • Hymn 452 Tiana ife tingofoka,
  • Hymn 1054 Ndilira mtima wakulapa
  • Hymn 1570 Mutidziwitse ‘Tate wathu,
  • Hymn 1352 Atate wa Kumwambako,
  • Hymn 356 YESU Mbuye onani,
  • Hymn 1329 M’tali mutali m’phirimo
  • Hymn 142 Kukondwa kwa wodwalayo
  • Hymn 301 Mwanawankhosa
  • Hymn 689 Anapeza Mwana
  • Hymn 1829 Mulungu ndiye Mbusa wanga, sindisowa konse;
  • Hymn 228 Ataya zoipa,
  • Hymn 560 Kale m’mzinda wachifumu
  • Hymn 1633 Adzabwera, adzabwera;
  • Hymn 1725 Zochimwa zanga zonsezo
  • Hymn 1084 “Khala mwa Ine,” munachotsa tsoka,
  • Hymn 1715 Kodi misozi itisowa,
  • Hymn 1086 “Khala mwa Ine,” ndinu mwini moyo,
  • Hymn 968 Mzimu wakuipa
  • Hymn 413 ZIPATA zachitsulo zitseguke zonse mbee!
  • Hymn 235 ADALITSIKA munthuyo,
  • Hymn 430 Tero tidzakwera
  • Hymn 1226 Wandipatsa moyo wake,
  • Hymn 911 Mokhala mokhamokha
  • Hymn 1245 Ine ndidzakuonetsa
  • Hymn 112 ELISA mneneri,
  • Hymn 1056 Mkhalidwe wanu mundipatse,
  • Hymn 1788 Mtimanga, bwera kuti upumule
  • Hymn 85 Mtima wanga wabvutika,
  • Hymn 325 KODI uli ndi chisoni
  • Hymn 1622 Anthu onse amlambire
  • Hymn 320 NDIKONDA Mlungu pomva Mbuye wanga
  • Hymn 1742 Yesu ndinu moyo wathu,
  • Hymn 1594 Chikondano chakechi
  • Hymn 1748 Ambuye tsopano lino,
  • Hymn 20 Mbuye mtsitsimutse
  • Hymn 1338 Munachita nthantha kale,
  • Hymn 269 NDILIRA ine kukayenda
  • Hymn 1616 Anafera
  • Hymn 1250 Mndilandire ine Mbuye
  • Hymn 80 KUDZA kwa Mbuye
  • Hymn 1043 Mbiri yake ubukitse,
  • Hymn 319 Koma zina sizinadziwa ayi,
  • Hymn 781 Tatsegukani inutu,
  • Hymn 419 ANYAMATA a Mulungu,
  • Hymn 660 Tumizani kuunikako,
  • Hymn 1394 Paphiri ndi padambo
  • Hymn 1786 Ndikonda Mlungu pomva Mbuye wanga
  • Hymn 29 CHIKONDI cha
  • Hymn 444 YEMWE afesa nalira,
  • Hymn 934 Mnamwalira Inu paja,
  • Hymn 424 Yesu, mndiyeretse,
  • Hymn 835 Mukhale ndine, dzuwalo lalowa,
  • Hymn 401 A MULUNGU,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version