Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 320 NDIKONDA Mlungu pomva Mbuye wanga

  1. Home   »  
  2. Hymn 320 NDIKONDA Mlungu pomva Mbuye wanga

Hymn 320 NDIKONDA Mlungu pomva Mbuye wanga

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 320 NDIKONDA Mlungu pomva Mbuye wanga

 

NDIKONDA Mlungu pomva Mbuye wanga
Amva pemphero ndi kulira kwanga,
Namachereza khutu nditapfuula,
Andithandiza, nandipulumutsa.

Mulungu wanga ndiye wachifundo
Ndi wolungama mtima ndi wabwino;
Apulumutsa anthu akufoka,
Akathandiza nkhaŵa imachoka.

Mtimanga, bwera kuti upumule,
Wakuchitiranso zokoma Mbuye,
Wakuchotsera imfa ndi misozi,
Ndingakhumudwe asungira phazi.

Nditani ine kubwezera Mbuye
Zokoma zonse anandichitira?
Chipulumutso chake ndidzatama,
Ndinalumbira zija ndidzapatsa.

Imfa ya anthu ake imkomera,
Aŵalandira m’nyumba zokonzeka.
Mbuye, kapolo wanu ndipereka
Nsembeyi yonga yanu, ndine ndekha.

Post navigation

Previous: Hymn 319 NDIDZATANI ine,
Next: Hymn 321 PAKUONA imfayo

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 212 Onse am’Mwamba ali mowemo,
  • Hymn 905 Iwo asekera, iwo asekera,
  • Hymn 334 Tsugulani mtima wanu
  • Hymn 1043 Mbiri yake ubukitse,
  • Hymn 12 NDITAMATU Ambuyangayu,
  • Hymn 275 Mlungu akuyang’aniredi,
  • Hymn 998 Anatilemba Yesu tikagwire nkhondo yake,
  • Hymn 1490 Musachitenso nthantha ‘yi,
  • Hymn 1399 Yesu ponong’oneza, idzanitu;
  • Hymn 865 Pakubweradi Woyesa tidzamlaka ifetu;
  • Hymn 44 NTHAWIYO anam’gwira Yesu,
  • Hymn 156 Yesu Mbuye, onani
  • Hymn 1576 Khamulo liliko
  • Hymn 1280 Kuti mundipatsa mphamvu yopambanayo;
  • Hymn 1525 Mbuye, mtiphunzitse
  • Hymn 1427 Penyetsetsa Yesu,
  • Hymn 1071 Kumwamba Yesu mthandize,
  • Hymn 823 M’mwambamo nyenyezi
  • Hymn 249 MBUYANGA Yesu, mundigwire
  • Hymn 979 Limbikani inu nonse,
  • Hymn 1172 Adzabweranso
  • Hymn 1047 Ambuye, chotsani zonse zomwezo
  • Hymn 398 KODI mbale wasimba zachikhululukiro,
  • Hymn 536 Ana inu, myamikeni
  • Hymn 610 Nafenso tidzadzuka kwa ‘ke ngati maluwawo,
  • Hymn 546 Kulibe wokwanira ‘yi
  • Hymn 492 DZIKO lilipolo
  • Hymn 1435 Ndiwe mlendo lero lino,
  • Hymn 1532 Mubwere kuno Mzimu ‘Nu,
  • Hymn 636 Yehova Mlungu wathu,
  • Hymn 182 YESU watidzera, watidzera,
  • Hymn 332 Perekani mtima wanu,
  • Hymn 931 Tikagwidwa ndi chisoni,
  • Hymn 56 KU Mzinda wakuyerawo
  • Hymn 427 AULENDO amayenda
  • Hymn 113 Likalira llipengalo,
  • Hymn 695 Pomveka konsekonse mbiri
  • Hymn 1845 Zabwino ndi zokoma zinditsata chitsatire;
  • Hymn 534 Bwerani, kondwerani,
  • Hymn 25 ANGELO amayimba,
  • Hymn 334 KULI dziko labwino M’mwamba,
  • Hymn 324 TIKAGWIDWA ndi chisoni,
  • Hymn 276 MKRISTU, ulimbike
  • Hymn 1792 Mulungu ndiye wachifundo,
  • Hymn 765 Chikondi chili m’chikhomu
  • Hymn 1639 Aleluya, aleluya,
  • Hymn 400 ONA Mwana wa Nkhosa,
  • Hymn 787 Mzimu Wakuyera
  • Hymn 1165 Dzanja la Mulungu
  • Hymn 891 Akakusowa malo
  • Hymn 1385 Anatsogolera kale
  • Hymn 803 Mulungu wanga, Dzuwatu
  • Hymn 1322 Ntchito zanga zonsezo
  • Hymn 1001 Mafumu atiuza tikaletse ukapolo,
  • Hymn 1420 Abale ‘nu, abale ‘nu,
  • Hymn 1125 Ndifuna Inu, Yesu,
  • Hymn 1766 Ndilikulemekeza
  • Hymn 1116 Kwawo kwa Mbuyako
  • Hymn 457 KALE m’mzinda wachifumu
  • Hymn 1100 Inde wakukonda ndinu;

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version