Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 334 KULI dziko labwino M’mwamba,

  1. Home   »  
  2. Hymn 334 KULI dziko labwino M’mwamba,

Hymn 334 KULI dziko labwino M’mwamba,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 334 KULI dziko labwino M’mwamba,

 

KULI dziko labwino M’mwamba,
Lakuwala koposa dzuwa;
Yesu watikonzera malo,
Pokhalira ife komweko.

Bwinoli tipita,
Tikomana mwa dziko lija;
Bwinoli tipita,
Tikomana mwa dziko lija.

Tidzayimba komweko nyimbo,
Za abwino omvera Yesu;
Sitidzamva chisoni ife,
Tidzakondwa masiku onse.

Tidzatama Atate wathu,
Kuti Iye ‘napatsa Yesu;
Kuchotsera zochimwa zonse,
Ndikutidalitsatu ife.

Post navigation

Previous: Hymn 333 M’DZIKO lino tikhalamo
Next: Hymn 335 KWATHU sipadziko, ndingopitilira,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1120 Ndifuna Yesuyo
  • Hymn 1032 Ntchito za Yesu gwira
  • Hymn 1815 Choposa nalo thupilo,
  • Hymn 1232 Ambuye ndinu Mbusa, Bwenzi, ndi Wansembe wanga,
  • Hymn 1250 Mndilandire ine Mbuye
  • Hymn 1854 Tate msandipitirire,
  • Hymn 411 Yesu adza kukundika
  • Hymn 1579 Akhala mafumu
  • Hymn 858 Anthu osawerengeka
  • Hymn 491 N’takafika kwanu
  • Hymn 1347 Akukonda, akukonda,
  • Hymn 1765 Zoonazi amithenga
  • Hymn 855 Aulendo amayenda
  • Hymn 769 Ndi kutsukidwa m’mwazimo
  • Hymn 32 YENDANI, Mfumu yamtendere
  • Hymn 1616 Anafera
  • Hymn 1324 M’moyo uno kunsiku
  • Hymn 1266 E, chimwemwe chachikulu, N’taperekadi
  • Hymn 160 MADALITSO ngati mvumbi,
  • Hymn 1271 Onani Mbuye ndigonja,
  • Hymn 1307 Ndi ine simufuna ‘yi
  • Hymn 223 Ndafoka, ndaipa,
  • Hymn 433 Zoipa ndi zabwino
  • Hymn 1332 Imba kawiri ndi kawirinso,
  • Hymn 407 ADZAPAMBANA Yesu ponse
  • Hymn 1082 Ndidzaonana nanu
  • Hymn 1003 Kanganani nkhondo yanu
  • Hymn 773 Mtsinje woyerawo
  • Hymn 28 AMBUYE ngwodalitsika,
  • Hymn 1253 Ndingopatsa Inu Mbuye
  • Hymn 256 NGATI mtima sumakonda
  • Hymn 1793 Pakuwoloka mtsinje wa imfa
  • Hymn 718 Anu Mbuye ndifetu!
  • Hymn 701 Inu Atatuwo,
  • Hymn 713 Ambuye, Mwini zonsezi,
  • Hymn 1674 Lambira Yesuyo,
  • Hymn 3 TIMYAMIKIRE Mlunguyo,
  • Hymn 1482 Tsopano inu ‘dzanitu,
  • Hymn 1043 Mbiri yake ubukitse,
  • Hymn 1177 Ndidziwitsitsa Yesu ndi wanga,
  • Hymn 1063 Pokhala mtendere mu mtimangamu,
  • Hymn 1044 Yesu sakusiya konse;
  • Hymn 98 YESU, Bwenzi la ochimwa,
  • Hymn 1150 Pamtanda Mbuyanga ‘nafera,
  • Hymn 1642 M’khola mwa ng’ombe ku Betelehemu
  • Hymn 849 Tadzuka mzimu wanga’we
  • Hymn 392 ANU Mbuye ndifetu!
  • Hymn 1042 Zonse umazinyadira
  • Hymn 869 Anatipatsa Mawu onse olimbitsa mtima;
  • Hymn 1154 Zakutsogolo sitidziwa ‘yi;
  • Hymn 1586 Mbuye Yesu timtamanda
  • Hymn 1549 Mtitsutse titachimwa
  • Hymn 355 Tinafuna m’phirimo,
  • Hymn 23 TIIMBE nyimbo zotamanda
  • Hymn 1157 Mtendere wapambana m’Mwambamo
  • Hymn 1782 Poyamba paja analenga
  • Hymn 801 Lero mwatipatsa moyo,
  • Hymn 1037 Mapemphero athu
  • Hymn 221 Yesu and’itana,
  • Hymn 379 Anditsogolera m’njira

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version