Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 222 NDILIKUMVA m’mtima mwanga

  1. Home   »  
  2. Hymn 222 NDILIKUMVA m’mtima mwanga

Hymn 222 NDILIKUMVA m’mtima mwanga

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 222 NDILIKUMVA m’mtima mwanga

 

NDILIKUMVA m’mtima mwanga
Mau ake a MbuyAnga,
Ati, “Ndakukonda iwe,
Kodi undikonda Ine?”

Ati; “Mwana, kumbukira
Zonse ndinakuchitira;
Ndakukonda, ndakufera,
Ndakufuna posokera.

“Ku zoipa zonse zako,
Goli la pakhosi pako,
Ndi kunthenda zosautsa
Ndine ndakupulumutsa

“Kodi mayi wobereka
Mwana wake adzamleka
Pena adzamwiŵalira,
Koma ndikukumbukira.

“Nthaŵi ilikudza yonse
Sindisinthanika konse;
Imfa sindiletsa Ine
Ndisakondekonde iwe.

“Ine ndidzakuonetsa
Zonse zakukondweretsa
Za Kumwamba zanga izo,
Mwana, sundikonda ine?”

Ambuyanga, ndalephera,
Mwachisoni ndipemphera
Mundipatse ine ndithu
Mtima wakukonda Inu.

Post navigation

Previous: Hymn 221 A! CHIKONDI chopambana,
Next: Hymn 223 ATI Yesu Mbuyeyo:

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 352 NONSE okhala pansipa,
  • Hymn 180 MALO alimo m’nyumba ya Yesu,
  • Hymn 506 Ndikondwa kuti Yesu akonda,
  • Hymn 57 TIYENI, dzalireni nane,
  • Hymn 299 “Posunga nkhosa ife
  • Hymn 306 Ona Mwanawanakhosayo
  • Hymn 1388 Tiimbire Mlungu wathu
  • Hymn 362 MUKHALE ndine, dzuŵalo laloŵa,
  • Hymn 65 Chisomo chodabwitsacho
  • Hymn 262 Tumphatumpha moyo wanga,
  • Hymn 917 Ndi nkhondo ikaleka
  • Hymn 230 Ndisamba ndiyera,
  • Hymn 1571 Tamani mphamvu ya Yesu,
  • Hymn 996 Leka zakuipa zako,
  • Hymn 522 Akazi anadza
  • Hymn 943 Onse aliko takonda kalelo,
  • Hymn 1704 Zintchito zakezi
  • Hymn 231 AMBUYE, m’imfamo
  • Hymn 1201 Kumwamba kwanuko
  • Hymn 1818 Kuzani Mlungu m’Mwambamo
  • Hymn 468 NDIKONDWA kuti
  • Hymn 1660 Ndikakhumudwa
  • Hymn 858 Anthu osawerengeka
  • Hymn 1730 Anapeputsidwako,
  • Hymn 1029 Nkhawa tilibe; Yesuyo
  • Hymn 367 MPULUMUTSI, tikagona
  • Hymn 409 ANTHU akum’maŵa
  • Hymn 1559 Wotsogolera, munditsogolere
  • Hymn 400 ONA Mwana wa Nkhosa,
  • Hymn 727 Imfa ikandifikira,
  • Hymn 1543 Idzani, Mzimu Inu,
  • Hymn 1568 Kudzoza kwanu kutipatsa
  • Hymn 691 Akukhala kunja,
  • Hymn 1742 Yesu ndinu moyo wathu,
  • Hymn 1241 Ati: Mwana, kumbukira
  • Hymn 3 TIMYAMIKIRE Mlunguyo,
  • Hymn 1015 Mbuye, mwatiuza ‘fe
  • Hymn 59 IMVANI uthenga,
  • Hymn 479 Munanena mulandira
  • Hymn 1496 Mawu amveke bwino,
  • Hymn 1485 Unachimwachimwa ndithu,
  • Hymn 1677 Zomkweza zili m’Mwamba,Aleluya
  • Hymn 550 Wosauka Iyedi
  • Hymn 319 NDIDZATANI ine,
  • Hymn 419 ANYAMATA a Mulungu,
  • Hymn 1524 Ndiwo alimbitsa
  • Hymn 1689 Dzukani nayetu,
  • Hymn 218 NDIPEREKA zanga zonse
  • Hymn 27 LEMEKEZANI Yehova,
  • Hymn 1134 Pansi pano ndili mlendo,
  • Hymn 1675 Lambira Mfumuyo
  • Hymn 210 Nyumba yodyera ilikudzaza;
  • Hymn 496 MBUYE dalitsani Afirika.
  • Hymn 60 Chitetezo chachikulu
  • Hymn 169 M’manda nagonamo
  • Hymn 147 MUSAŴALOLE mawuwo
  • Hymn 1634 Pakwitana Mbuye wanga
  • Hymn 1843 Chigwa choopsacho cha imfa ndikachilowera,
  • Hymn 1001 Mafumu atiuza tikaletse ukapolo,
  • Hymn 1785 Tiyeni tizipita kwathu,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version