Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 362 MUKHALE ndine, dzuŵalo laloŵa,

  1. Home   »  
  2. Hymn 362 MUKHALE ndine, dzuŵalo laloŵa,

Hymn 362 MUKHALE ndine, dzuŵalo laloŵa,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 362 MUKHALE ndine, dzuŵalo laloŵa,

 

MUKHALE ndine, dzuŵalo laloŵa,
Wagwa usiku, bwenzi lindisoŵa;
Ndilibe wina wakundithandiza,
Wamphamvu ndinu, mkhale ndinetu.

Kamoyo kanga katha lero lino,
Zidzachokanso zinthuzo za dziko;
Zimasinthika zonse zooneka,
Simusi nthika, mkhale ndinutu.

Koma kalelo mnakhalitsa pano,
Mukhale ndine, msandichokerenso,
Sin’pempha kuti Mbuye mungotsotse,
Komatu mukhalitse ndinetu.

E, tsiku lonse Inu ndifunitsa;
Ndi mphamvu yanu yokha ndisungika;
Mukatsogola ndidzadikha m’mtima;
Usiku, msana, mkhale ndinetu.

Adani sindiopa mukalipo
Muletse tsoka ndi chisoni chino;
Ikadza imfa n’dzalimbika m’mtima;
M’moyo ndi m’imfa mkhale ndinetu.

Post navigation

Previous: Hymn 361 AMBUYE munapatsa tsiku
Next: Hymn 363 ATATE ndiyamika,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 106 Ife, tapulumukadi,
  • Hymn 558 Mwanayo wa Mulunguyo
  • Hymn 303 MEMA nkhondoyo, wadza mdaniyo,
  • Hymn 856 Kuunika kuoneka
  • Hymn 1564 Mufike monga moto wakuotcha zomwezo.
  • Hymn 1725 Zochimwa zanga zonsezo
  • Hymn 1294 Wakuba uja nachiona,
  • Hymn 10 Kristu Mfumuyo yaulemerero!
  • Hymn 978 Mtima wanu wonse ndithu
  • Hymn 1836 Ndi wamwayi munthu uja
  • Hymn 192 ZAKEYU mkulu wa misonkho,
  • Hymn 219 Mtenderewo wosanyenga
  • Hymn 324 TIKAGWIDWA ndi chisoni,
  • Hymn 1388 Tiimbire Mlungu wathu
  • Hymn 933 M’mene imfa yathu idza,
  • Hymn 74 IDZA wolema,
  • Hymn 811 Wopulumutsa mudzetu;
  • Hymn 1709 Pamtandapo Ambuyeyo anafera ifetu,
  • Hymn 490 YESU adza kuwerenga,
  • Hymn 131 MAWU a Mulungu awa,
  • Hymn 1687 Alonda onsewo
  • Hymn 678 Ibukike mbiri yanu,
  • Hymn 1346 Ndaima pano, ndaima pakhomo:Lowa, lowa, lowa, lowa!
  • Hymn 1514 Dzinthu zakumundazo
  • Hymn 337 PADZIKO pano tikhalira M’moyo wosauka;
  • Hymn 288 HAYA! ’nzanga taonani
  • Hymn 872 Mtidzutse, Mbuyetu,
  • Hymn 265 Imbirira moyo wanga,
  • Hymn 1030 Tioperanji ifetu?
  • Hymn 909 Ife tikondwera, ife tikondwera,
  • Hymn 1803 Nowayo nayendamo,
  • Hymn 136 MKAZI wa ku Samariya,
  • Hymn 500 >AMEN, Amen, Amen.
  • Hymn 258 MWA ine, moyo wanga ndi Yesu
  • Hymn 1129 Mbuyanga Yesu, ndikapanda Inu
  • Hymn 1432 Lero lino m’bale wanga,
  • Hymn 1021 Kunsi kudambo, pena m’mwamba m’phirimo,
  • Hymn 1753 Adzatipulumutsa
  • Hymn 1348 Akupeza, akupeza,
  • Hymn 20 Mbuye mtsitsimutse
  • Hymn 308 AULENDO, munka kuti
  • Hymn 921 Komwe Mbusa kwawoko
  • Hymn 367 Nonse okhala pansipa,
  • Hymn 362 Imvani Yesu akuti:
  • Hymn 566 Ana inu, ana inu,
  • Hymn 369 LERO mwatipatsa moyo,
  • Hymn 1344 Yamba ulendowo
  • Hymn 1371 Mitengo yaitalitali ‘nu
  • Hymn 1590 Mtima ndimakondweramo,
  • Hymn 207 AMBUYE ndamvatu Mawu anu,
  • Hymn 895 Ndikabwera ndi katundu
  • Hymn 417 M’manja a Yesu wanga
  • Hymn 880 Bwenzi lathu ndiye Yesu
  • Hymn 1327 Bwezatu, bwezatu,
  • Hymn 293 Tidziperekadi konse kwa Inu
  • Hymn 7 “Mbuye Woyera! E, Woyeranokha!
  • Hymn 1318 Ndibwera kwa Ambuyeyo,
  • Hymn 407 ADZAPAMBANA Yesu ponse
  • Hymn 116 Nkhosa zanga zimandimva
  • Hymn 144 AMENE adzavomereza ndithu,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version