Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 337 PADZIKO pano tikhalira M’moyo wosauka;

  1. Home   »  
  2. Hymn 337 PADZIKO pano tikhalira M’moyo wosauka;

Hymn 337 PADZIKO pano tikhalira M’moyo wosauka;

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 337 PADZIKO pano tikhalira M’moyo wosauka;

 

PADZIKO pano tikhalira M’moyo wosauka;
Komatu kwa Mulungu kuli
Dziko lakudala;
Mbuyathu Yesu wapitako,
Iye ’natsogola;
Tidzamtsatira ife tonse,
Tsiku lomaliza.

Tiyeni, tiyeni,
Ku dziko lakudala;
Tidzafikira m’dziko ilo
Tsiku lomaliza.

Masiku tikatsala ife
M’dziko mwathu momwe
Mulungu watipatsa ntchito,
Tikazigwiritse.
Pamene zakuipa zathu
Zisautsa ife,
Tikapemphere Mbuye wathu,
Atipulumutse.

Ulendo wathu ukadzatha
Tidzafika kwathu,
Adzatifitsa ife komwe
Yesu Mbuye wathu.
Sitidzapeza masautso
M’dziko la Mulungu,
Tidzakondwera chikondwere
Nthaŵi zathu zonse.

Post navigation

Previous: Hymn 336 KULINSO dziko lowala M’mwamba,
Next: Hymn 338 ’TATE wa Kumwambako,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 6 Nanu akukuzani amithenga,
  • Hymn 517 “Osana m’Mwambamwamba!”
  • Hymn 1611 Nadzuka m’mandamo
  • Hymn 189 MLENDO ali pakhomo,
  • Hymn 12 NDITAMATU Ambuyangayu,
  • Hymn 1444 Wamoyo ndiye Yesudi,
  • Hymn 1334 Walandira inetu
  • Hymn 514 Osanatu, osana,
  • Hymn 1843 Chigwa choopsacho cha imfa ndikachilowera,
  • Hymn 681 Ankhondo a Mulungu ‘nu, yendani m’njiramo,
  • Hymn 56 KU Mzinda wakuyerawo
  • Hymn 46 INALIPO nthawi,
  • Hymn 1103 Ndakudani, mnandikonda
  • Hymn 95 TAMANI mphamvu ya Yesu,
  • Hymn 188 Ine ndili ndi manyazi
  • Hymn 399 M’KHOLA mwa ng’ombe ku Betlehemu
  • Hymn 470 YESU andikonda ine,
  • Hymn 1076 Khalatu woyera,
  • Hymn 1108 Khala chete mtima wanga,
  • Hymn 498 AMBUYE, mtidalitsetu,
  • Hymn 1263 Mbuye, ndingogonj tere, Ndibvomerapo;
  • Hymn 140 NDINAMIRA m’machimo, wosaonekanso,
  • Hymn 996 Leka zakuipa zako,
  • Hymn 831 Mundikumbutse, ndikapanda tulo, za Kumwambako;
  • Hymn 1588 Wandiwombola inetu
  • Hymn 158 WOCHIMWA iwe, bweratu,
  • Hymn 424 Yesu, mndiyeretse,
  • Hymn 33 OWONADI mtima,
  • Hymn 246 Pajapo ndipenya
  • Hymn 83 Mpulumutsi Wokondedwa,
  • Hymn 1787 Mulungu wanga ndiye wachifundo
  • Hymn 1636 Potuluka m’manda mwawo
  • Hymn 99 TIYAMIKE mbuye Yesu
  • Hymn 770 Atate, muwapenye
  • Hymn 38 Kodi mubvutidwa naye katundu?
  • Hymn 1847 Ife tonse, ife tonse,
  • Hymn 390 A! YESU, ndapangana
  • Hymn 1170 Pamtanda wake
  • Hymn 1049 Zoipa zangazi
  • Hymn 1784 Komweko titasaukira,
  • Hymn 974 Tsopano timenyana
  • Hymn 1585 Dzina ili ndi lokoma
  • Hymn 646 Mudalitse nyumba yathu;
  • Hymn 2 YEHOVA Mthandizi,
  • Hymn 594 Monga may’ asusuza
  • Hymn 1158 Yesu ndiye Mbuye wanga,
  • Hymn 685 Tamva mawu amwewo
  • Hymn 539 Anafika ‘kazi omwe
  • Hymn 178 Machimo anga ngambiri
  • Hymn 1200 Ambuye, m’imfamo
  • Hymn 946 Ngakhale enawo aleke kwimbako,
  • Hymn 1014 Tingolira kaya,
  • Hymn 173 Mema nkhondoyo, wadza mdaniyo,
  • Hymn 583 Anabadwa,
  • Hymn 757 Sindili woyenera ‘ne;
  • Hymn 481 USACHIMWE konse,
  • Hymn 455 Mdileke kulimbna ndi
  • Hymn 279 MBUYE, nditsate bwanjiko?
  • Hymn 370 KWACHA lero kwati mbee,
  • Hymn 798 M’nyumba yanu, Mlungu, ‘yi

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version