Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 481 USACHIMWE konse,

  1. Home   »  
  2. Hymn 481 USACHIMWE konse,

Hymn 481 USACHIMWE konse,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 481 USACHIMWE konse,

 

USACHIMWE konse,
Lekatu kukwiya;
Uli mwana wake,
Mwana wa Mbuyathu.

Yesu ndi wofatsa,
Yesu ndi woyera;
Ana ake omwe
Aziyera m’mtima

Mzimu wakuipa
Ukusuzumira,
Umakuyesera
Kuti ukachimwe.

Koma usalole
Mawu a Satana;
Bweza tchimo lake,
Chita zolungama.

Yesu ndi Mbuyako,
Mbuyeyo ngwabwino;
Ana ake omwe
Aziyera m’mtima.

Post navigation

Previous: Hymn 480 TIANA ife tingofoka,
Next: Hymn 482 TCHIMO musalole, musadziipitse,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 133 NSEMBE yake ya Kaini,
  • Hymn 89 Muli mphamvu yodabwitsatu
  • Hymn 1387 Amaweta nyama zonse,
  • Hymn 508 Mzimu Woyera akhala mwa ine,
  • Hymn 457 KALE m’mzinda wachifumu
  • Hymn 85 Mtima wanga wabvutika,
  • Hymn 433 Zoipa ndi zabwino
  • Hymn 108 MBUYE wondipulumutsa,
  • Hymn 45 IFE timakufunani
  • Hymn 1339 Musaope pokumbuka
  • Hymn 5 Inu Mulungu, tikuyamikani;
  • Hymn 380 Ndipyola kodi chikhwawa
  • Hymn 602 Mpulumutsi wakukoma,
  • Hymn 747 Tadzanitu, okhulupiradi,
  • Hymn 131 MAWU a Mulungu awa,
  • Hymn 1706 Pamutu minga kwe!
  • Hymn 574 A! Yesu Mbuye wakuyera,
  • Hymn 1257 Mtanda m’mtima ndiyang’na,
  • Hymn 1018 Yesu afuna iwe unnke kwawoko,
  • Hymn 1289 Ndinasokeratu kutaliko,
  • Hymn 377 Yehova, Mbusa wangadi,
  • Hymn 560 Kale m’mzinda wachifumu
  • Hymn 1595 Ndani mwa abale athu
  • Hymn 1485 Unachimwachimwa ndithu,
  • Hymn 469 Lero mkhale nafe ndithu,
  • Hymn 1233 Tsopano ndibukitsabe chikondi chanu chija
  • Hymn 324 TIKAGWIDWA ndi chisoni,
  • Hymn 494 Yesu, E, ndikufunani,
  • Hymn 159 Kamwana Yesu ‘nabadwa,
  • Hymn 1340 Perekani mtima wanu
  • Hymn 603 Mzimu wanu Wakuyera,
  • Hymn 70 Mbuye ndinu bwenzi langa ndithu,
  • Hymn 699 Inu wakudzatu
  • Hymn 547 Anatikondakonda ‘Ye.
  • Hymn 1410 Nthawi zonse mufunabe
  • Hymn 1764 Yesu ndinu Mbuye wathu,
  • Hymn 989 Yochita ndi yodikha
  • Hymn 1097 Njira yanga sindidziwa,
  • Hymn 1279 Kuti munditsogolera paulendopo;
  • Hymn 390 Lalowa dzuwa, kwada bii!
  • Hymn 1722 Ambuye tikondweratu
  • Hymn 1201 Kumwamba kwanuko
  • Hymn 1522 Tikaona bvuto,
  • Hymn 461 Inu nonse anzanga,
  • Hymn 1318 Ndibwera kwa Ambuyeyo,
  • Hymn 466 OSANATU, osana,
  • Hymn 1047 Ambuye, chotsani zonse zomwezo
  • Hymn 10 Kristu Mfumuyo yaulemerero!
  • Hymn 1700 Ambuye Mwini moyo,
  • Hymn 207 Malo alimo m’nyumba ya Yesu,
  • Hymn 844 Pogona ife, amadzuka
  • Hymn 1468 Zobvala zake zonse
  • Hymn 362 MUKHALE ndine, dzuŵalo laloŵa,
  • Hymn 373 NYUMBA ya Mulungu, ili pano,
  • Hymn 1326 A! Mbusa wathu amvatu
  • Hymn 964 Kodi simuona njira,
  • Hymn 290 NAMONDWE wawuka,
  • Hymn 1666 Yesu, ndinutu chitsime
  • Hymn 1669 Ukafuna kumdziwitsa,
  • Hymn 982 Tiyeni Akristu,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version