Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 481 USACHIMWE konse,

  1. Home   »  
  2. Hymn 481 USACHIMWE konse,

Hymn 481 USACHIMWE konse,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 481 USACHIMWE konse,

 

USACHIMWE konse,
Lekatu kukwiya;
Uli mwana wake,
Mwana wa Mbuyathu.

Yesu ndi wofatsa,
Yesu ndi woyera;
Ana ake omwe
Aziyera m’mtima

Mzimu wakuipa
Ukusuzumira,
Umakuyesera
Kuti ukachimwe.

Koma usalole
Mawu a Satana;
Bweza tchimo lake,
Chita zolungama.

Yesu ndi Mbuyako,
Mbuyeyo ngwabwino;
Ana ake omwe
Aziyera m’mtima.

Post navigation

Previous: Hymn 480 TIANA ife tingofoka,
Next: Hymn 482 TCHIMO musalole, musadziipitse,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 315 YENDANI munjira yake,
  • Hymn 774 Tibatizidweko,
  • Hymn 153 Pemphero ndiko kufuna,
  • Hymn 621 Wolenga ndi Yemweyo
  • Hymn 1251 Ndasokera m’tali ndithu
  • Hymn 748 Ndiye wa moyo wonse Mwiniyo,
  • Hymn 480 TIANA ife tingofoka,
  • Hymn 1128 Mbuyanga Yesu, mundisunge ine
  • Hymn 1694 Timwimbire Mlungu wathu, Aleluya
  • Hymn 75 Ndiperekatu
  • Hymn 1688 Mulibe m’mandamu,
  • Hymn 57 Ife tiyembekezera Yesu,
  • Hymn 765 Chikondi chili m’chikhomu
  • Hymn 1468 Zobvala zake zonse
  • Hymn 98 Ndidzamwona maso ndi maso
  • Hymn 1073 Mwa ine myatse moto wanu wakuyera mbuu,
  • Hymn 939 Ambuye andisunga
  • Hymn 957 Mundimwetse madzi anu,
  • Hymn 1571 Tamani mphamvu ya Yesu,
  • Hymn 1670 Bwenzi ndiye wakufera,
  • Hymn 120 MUNDINYEMERE ’ne
  • Hymn 447 Usachimwe konse,
  • Hymn 198 CHITSIMECHO cha mwaziwo
  • Hymn 732 1 Ndinamva njala, Yesu,
  • Hymn 492 Yesu Mbuye ‘Nu wafatsa
  • Hymn 1753 Adzatipulumutsa
  • Hymn 1189 Ambuye Mulungu,
  • Hymn 1746 Mwachimwemwe, mwachisoni,
  • Hymn 1162 Mumvetu abwenzi athu,
  • Hymn 1754 Ndiye akumbukira
  • Hymn 1348 Akupeza, akupeza,
  • Hymn 90 WINA atikonda ife,
  • Hymn 1458 Satana ndi unyolo
  • Hymn 243 KONDWANI nonsenu,
  • Hymn 1085 “Khala mwa Ine,” ndinu mwini mphamvu,
  • Hymn 530 Munaneneratu mawu a moyonso
  • Hymn 820 Ndife ananu,
  • Hymn 783 Antchito a Mulungu ‘nu
  • Hymn 1010 Ndipo ngati ungolema,
  • Hymn 339 Tipempha,
  • Hymn 930 Leroli chisoni chokha,
  • Hymn 139 MLUNGU anapatsa moyo,
  • Hymn 397 Yesu Mbusa, mutimvere,
  • Hymn 942 Kaamba chisomo cha Mbuyathu
  • Hymn 133 NSEMBE yake ya Kaini,
  • Hymn 374 NDI lokoma m’Mwambamo,
  • Hymn 1695 Pokumbukira mtandawo
  • Hymn 1099 Sindidziwatu zamawa,
  • Hymn 1565 Mufike monga ngati njiwa yamtenderewo,
  • Hymn 1596 Anamnyoza pansi pano,
  • Hymn 677 Ponse padakhala mdima
  • Hymn 279 Mbwere mudzamve nonse
  • Hymn 600 Mbuye Yesu, myandikire,
  • Hymn 1481 Timsankhe Yesu Mbuyeyo,
  • Hymn 358 MLUNGU ali muno,
  • Hymn 170 YESU ponong’oneza, idzanitu;
  • Hymn 560 Kale m’mzinda wachifumu
  • Hymn 307 Atate Wamkulu ndi wamphamvu zonse,
  • Hymn 1500 Simbani Mbiri yomwe,
  • Hymn 1502 Kodi ulikulemedwa

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version