Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 480 TIANA ife tingofoka,

  1. Home   »  
  2. Hymn 480 TIANA ife tingofoka,

Hymn 480 TIANA ife tingofoka,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 480 TIANA ife tingofoka,

 

TIANA ife tingofoka,
Sitikhala ’mphamvu ’yi;
Tikhoza kukachitiranji
Yesu kumkondwetsadi?

Tiana ta Ambuye tili
N’ntchito yaikuludi,
Kudzichepetsa ndi kusiya
Tchimo lili lonseli.

Kapena m’mtima ndimakwiya,
Nditukwana mnzangayo,
Kapena ndidzitama – izi
Ndilekere Mbuyeyo.

Ndileke kulimbana ndi
Kuŵanamiza enawo;
Ndinene zakufatsa,
Zakukondweretsa Yesuyo.

Tizikondana, tisekere
Tsiku lonse kwathuko,
Muyere m’mtima popeza
Yesu ndi Woyerayo.

Palibe mwana wakuchepa
Kunyamula mtandawu;
Ambuye Yesu mutipatse
Mtima wokondanatu.

Post navigation

Previous: Hymn 479 ANYAMATA inutu,
Next: Hymn 481 USACHIMWE konse,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 35 Zonse za m’dziko zidzatha,
  • Hymn 1787 Mulungu wanga ndiye wachifundo
  • Hymn 182 YESU watidzera, watidzera,
  • Hymn 81 MBUYE Yesu adzabwera,
  • Hymn 1202 Ndikhumba mtimawo
  • Hymn 310 MBUYE munditsogolere,
  • Hymn 190 Nsiku zonse kwanja kwake
  • Hymn 291 Ndi milomo yathu iyinso njanu,
  • Hymn 148 Ndisauka, ndimasowa
  • Hymn 1811 Tipulumuka mommo,
  • Hymn 1476 Mipingo iyo idzatu,
  • Hymn 259 CHISOMO chodabwitsacho,
  • Hymn 563 Ndipo Mwana uyu Yesu
  • Hymn 933 M’mene imfa yathu idza,
  • Hymn 634 Mtifungatire ndi mapiko paulendo pathu,
  • Hymn 24 TITAME Mlungu Wakumwamba,
  • Hymn 670 Isaleke ntchito yake
  • Hymn 238 Mbuye Yesu, lowani m’mtima,
  • Hymn 1468 Zobvala zake zonse
  • Hymn 56 KU Mzinda wakuyerawo
  • Hymn 1111 Pamene ndilemedwa
  • Hymn 1074 Mubweretu nomwe ‘Nu munatsika kalelo;
  • Hymn 110 Ndaima nji pa Kristuyo,
  • Hymn 77 MMENE Yesu adzabwera,
  • Hymn 385 Tsopano, poyamba paja,
  • Hymn 405 M’mtima mwangamu mlowemo,
  • Hymn 1411 Yesu akuitanani
  • Hymn 607 Dziko lonse lilikukondwa, mlengalenga mpheponso,
  • Hymn 1506 Ndikamfunafuna Iye,
  • Hymn 659 Anthu ali m’mdima akuitanitsa
  • Hymn 645 Kristu ndiye mwala wathu,
  • Hymn 1634 Pakwitana Mbuye wanga
  • Hymn 1858 Ha! Chikondi cha Mulungu,
  • Hymn 1383 Dzina lake tibukitsa,
  • Hymn 418 M’manja Yesu wanga
  • Hymn 1580 Akadakhalabe
  • Hymn 80 Utsegule mtimawo,
  • Hymn 300 AKRISTU limbikani,
  • Hymn 226 Nditama mwaziwo!
  • Hymn 454 TAONANI, m’kholamo,
  • Hymn 1095 Mumtima wakufatsa
  • Hymn 350 MBUYE ndayima pano,
  • Hymn 1039 Usafune chuma chokha,
  • Hymn 1650 E, moyo wanga’we
  • Hymn 1768 Ndiye wamphamvu zonse
  • Hymn 791 Anthu opembedzawo
  • Hymn 302 Anasenza m’thupi mwake;
  • Hymn 42 Masiku tikatsala ife
  • Hymn 240 Nyama za m’thengo
  • Hymn 1010 Ndipo ngati ungolema,
  • Hymn 709 Munthu aganize
  • Hymn 1781 Timwimbire nyimbo,
  • Hymn 1170 Pamtanda wake
  • Hymn 323 >APITA anzathu dzuŵa lino
  • Hymn 144 Yesu, ndipemphera
  • Hymn 1357 Mlemekeze, anakonda
  • Hymn 499 ‘Nafera Mbuye wanga
  • Hymn 422 DZIKO lonse lapansi,
  • Hymn 1570 Mutidziwitse ‘Tate wathu,
  • Hymn 115 NTHAWI ija ya Sauli,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version