Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 480 TIANA ife tingofoka,

  1. Home   »  
  2. Hymn 480 TIANA ife tingofoka,

Hymn 480 TIANA ife tingofoka,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 480 TIANA ife tingofoka,

 

TIANA ife tingofoka,
Sitikhala ’mphamvu ’yi;
Tikhoza kukachitiranji
Yesu kumkondwetsadi?

Tiana ta Ambuye tili
N’ntchito yaikuludi,
Kudzichepetsa ndi kusiya
Tchimo lili lonseli.

Kapena m’mtima ndimakwiya,
Nditukwana mnzangayo,
Kapena ndidzitama – izi
Ndilekere Mbuyeyo.

Ndileke kulimbana ndi
Kuŵanamiza enawo;
Ndinene zakufatsa,
Zakukondweretsa Yesuyo.

Tizikondana, tisekere
Tsiku lonse kwathuko,
Muyere m’mtima popeza
Yesu ndi Woyerayo.

Palibe mwana wakuchepa
Kunyamula mtandawu;
Ambuye Yesu mutipatse
Mtima wokondanatu.

Post navigation

Previous: Hymn 479 ANYAMATA inutu,
Next: Hymn 481 USACHIMWE konse,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1565 Mufike monga ngati njiwa yamtenderewo,
  • Hymn 884 Mndikumbutse zomwe
  • Hymn 215 TATE ndili mwana wanu,
  • Hymn 336 KULINSO dziko lowala M’mwamba,
  • Hymn 291 ULENDO wachikhrisitu ngosawutsa ndithu,
  • Hymn 1127 Mbuyanga Yesu, mundigwire dzanja;
  • Hymn 18 Mbuye mtsitsimutse
  • Hymn 930 Leroli chisoni chokha,
  • Hymn 691 Akukhala kunja,
  • Hymn 1751 Mbuye ngwodalitsika,
  • Hymn 458 USIKUWO, woyerawo!
  • Hymn 793 Tikondwera kuti
  • Hymn 1092 Ndimamva njala kuno, Yesu,
  • Hymn 879 Zokoma etu nthawizi”
  • Hymn 1849 Nthawi zonse monga ‘Tate
  • Hymn 39 Poyang’ana ena ndi ndalamatu,
  • Hymn 1076 Khalatu woyera,
  • Hymn 537 Aleluya! Aleluya!
  • Hymn 206 YESU, mulikundipempha
  • Hymn 663 Anyamata a Mulungu,
  • Hymn 1458 Satana ndi unyolo
  • Hello world!
  • Hymn 43 Ulendo wathu ukadzatha
  • Hymn 126 Mwa ine, moyo wanga ndi Yesu
  • Hymn 1333 Idzatu kwa Yesuyo,
  • Hymn 123 Koma mudzisungire chuma cha Kumwamba
  • Hymn 1592 Tsono mubwere inunso,
  • Hymn 1816 Anatikondakonda ‘Ye,
  • Hymn 1440 Yesu alindira,
  • Hymn 759 Ndilawako tsopanoli
  • Hymn 28 Mbuye ndisaukadi,
  • Hymn 1147 Khalani duu! Pakufa ifetu,
  • Hymn 651 Ikhale ngati nyali
  • Hymn 483 Ndife akuchoka,
  • Hymn 1227 Ndiyamika Mbuye wanga
  • Hymn 217 CHIPULUMUTSO chathu chayandika,
  • Hymn 457 Palibe mwana wakuchepa
  • Hymn 228 Ataya zoipa,
  • Hymn 1415 Iye anatsika m’Mwamba,
  • Hymn 995 Taya zako zochenjera,
  • Hymn 1203 Zambiri zangazo
  • Hymn 1266 E, chimwemwe chachikulu, N’taperekadi
  • Hymn 1173 Sindinanyengedwa konse
  • Hymn 382 Mwadzoza mutu wanga ndi
  • Hymn 353 Anatuma Mtetezi,
  • Hymn 282 INU muli mehere,
  • Hymn 1479 Ndi Yesu yemwe kalelo
  • Hymn 333 M’DZIKO lino tikhalamo
  • Hymn 1681 Mphamvu za imfa ndi za Satana
  • Hymn 203 Pamtandapo, pamtanda,
  • Hymn 1372 Zam’madzi zonse zakuopsyazo,
  • Hymn 1297 Kumwamba komwe n’dzaimbira
  • Hymn 1070 Mthandize Mbuye, timvetu,
  • Hymn 213 Mawu a Yesu ati: “Msangatu
  • Hymn 1141 Pakulekana ifetu
  • Hymn 459 KALE anthu m’kholamo,
  • Hymn 1230 Lichiza mzimu wophwetekwa ukakhale bata,
  • Hymn 449 Mzimu wakuipa
  • Hymn 1255 Chitha nchiani kund’yeretsa?
  • Hymn 218 Mbuye Yesu ndi Atate,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version