Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 480 TIANA ife tingofoka,

  1. Home   »  
  2. Hymn 480 TIANA ife tingofoka,

Hymn 480 TIANA ife tingofoka,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 480 TIANA ife tingofoka,

 

TIANA ife tingofoka,
Sitikhala ’mphamvu ’yi;
Tikhoza kukachitiranji
Yesu kumkondwetsadi?

Tiana ta Ambuye tili
N’ntchito yaikuludi,
Kudzichepetsa ndi kusiya
Tchimo lili lonseli.

Kapena m’mtima ndimakwiya,
Nditukwana mnzangayo,
Kapena ndidzitama – izi
Ndilekere Mbuyeyo.

Ndileke kulimbana ndi
Kuŵanamiza enawo;
Ndinene zakufatsa,
Zakukondweretsa Yesuyo.

Tizikondana, tisekere
Tsiku lonse kwathuko,
Muyere m’mtima popeza
Yesu ndi Woyerayo.

Palibe mwana wakuchepa
Kunyamula mtandawu;
Ambuye Yesu mutipatse
Mtima wokondanatu.

Post navigation

Previous: Hymn 479 ANYAMATA inutu,
Next: Hymn 481 USACHIMWE konse,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1667 Yesu wakukoma mtima,
  • Hymn 1196 E! chikondi ndithu,
  • Hymn 143 Lero lino Mbuye Yesu
  • Hymn 506 Ndikondwa kuti Yesu akonda,
  • Hymn 1322 Ntchito zanga zonsezo
  • Hymn 994 Limba mtima mbale wanga,
  • Hymn 126 Mwa ine, moyo wanga ndi Yesu
  • Hymn 1828 Timtamande Iye ndi moyo wathunso
  • Hymn 353 ATATE Wamkulu ndi Wamphamvu zonse,
  • Hymn 897 Ndine mlendo pansi pano,
  • Hymn 73 Mu ulemerero tidzakhala m’yaya,
  • Hymn 436 YEHOVA Mlungu wathu,
  • Hymn 1132 Mlungu adzandilandila,
  • Hymn 1566 Mufike monga ngati mphepo yokokomayo,
  • Hymn 258 Kazembe wanga m’matenda,
  • Hymn 1063 Pokhala mtendere mu mtimangamu,
  • Hymn 12 Kumva milandu yathu mudzabwera
  • Hymn 1753 Adzatipulumutsa
  • Hymn 212 Onse am’Mwamba ali mowemo,
  • Hymn 1731 Ife tinachimwadi,
  • Hymn 229 POYAMBAPO ndakondwadi.
  • Hymn 113 KALERO anthu onse
  • Hymn 1855 Yesu, msandipitirire
  • Hymn 1003 Kanganani nkhondo yanu
  • Hymn 791 Anthu opembedzawo
  • Hymn 705 Tikhaletu nawo, Mbuye,
  • Hymn 1264 Chifuniro change, Mbuye, Ndiperekachi;
  • Hymn 220 MULUNGU mundichitire chifundo,
  • Hymn 1826 Amadyetsa Iye mbalame zam’mwamba,
  • Hymn 1376 Akulu nonse ndi mafumu ‘nu,
  • Hymn 1785 Tiyeni tizipita kwathu,
  • Hymn 326 TSIKU Iidzafika mbale,
  • Hymn 1272 Muyambe ntchito yanuyi,
  • Hymn 780 Kwezani mitu yanuyo,
  • Hymn 643 Mukhale nawo, yesu,
  • Hymn 1129 Mbuyanga Yesu, ndikapanda Inu
  • Hymn 15 Mbuye, chifundo chanu chitigwere
  • Hymn 1495 Simbani bwinobwino
  • Hymn 924 Kodi uli ndi chisoni
  • Hymn 584 Ndi angelo,
  • Hymn 1649 Kutenga inetu, kutenga inetu
  • Hymn 973 Tigwire nkhondo yomwe
  • Hymn 598 Mlungu ali nane;
  • Hymn 82 YANG’ANANI, anthu onse,
  • Hymn 341 Ayenda,
  • Hymn 766 Monga zomera zonsezo
  • Hymn 1427 Penyetsetsa Yesu,
  • Hymn 401 A MULUNGU,
  • Hymn 1640 Alinkudza Ambuye Yesu
  • Hymn 1168 Aleluya, muyenera!
  • Hymn 410 Ana ake angonga
  • Hymn 482 Ndinu wakuyera,
  • Hymn 881 Tili nazo zotiyesa,
  • Hymn 1155 Abale angakhale m’talimo
  • Hymn 979 Limbikani inu nonse,
  • Hymn 665 Pomangidwa anthu nayo
  • Hymn 650 Tikondwa tonse ndi kukuthokazani Nu
  • Hymn 1355 Atate, Mwana, Mzimunso,
  • Hymn 1578 Onsewa ‘nachimwa
  • Hymn 1544 Wakunga mwana ine,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version