Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 422 DZIKO lonse lapansi,

  1. Home   »  
  2. Hymn 422 DZIKO lonse lapansi,

Hymn 422 DZIKO lonse lapansi,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 422 DZIKO lonse lapansi,

 

DZIKO lonse lapansi,
Linachimwa kwa Mlungu,
Chilango chake ndicho cha imfa;
Koma podza Yesuyo,
Anathetsa mlanduwo;
Potifera ife pamtandapo.

Onani,
Mwana wa Nkhosa,
Wachotsa tchimo lonse pansipa;
Ndiye Yesu Mfumuyo,
Ndiye Mpulumutsiyo;
Wotifera ife pamtandapo.

Tsono mmene tadziwa,
Kuti ndife ochimwa,
Tiyeni tinke kwa Ambuyewo;
Tisachite manyazi,
Tiwauze tchimolo;
Iwo adzatikhululukira.

Wotikhululukira,
Adzatiwuza tonse,
Kuti tisadzachimwenso ndithu;
Zakale zatha ndithu,
Zatsala zatsopano;
Tasamba mwazi wake tayera.

Post navigation

Previous: Hymn 421 ANTHU ali m’mdima akuyitanitsa,
Next: Hymn 423 MUNENE Mbuye, ’nenetu,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 315 Munagwa pa Atumwiwo;
  • Hymn 1131 M’mene ine ndisauka
  • Hymn 1651 Kwa Mulungu m’Mwambamo
  • Hymn 1781 Timwimbire nyimbo,
  • Hymn 755 Pamene padzakhalapo
  • Hymn 391 MUNDIMVERE, Mbuye wanga
  • Hymn 67 Chisomo chandisungadi
  • Hymn 1505 Ndikampeza, ndikamtsata
  • Hymn 420 Mtima umabisala
  • Hymn 1395 Mulungu ali nane!
  • Hymn 209 M’NDILANDIRE ine Mbuye
  • Hymn 1325 Maiwe! Thanthwe long’ambikatu,
  • Hymn 884 Mndikumbutse zomwe
  • Hymn 361 Munka kangati kulawa
  • Hymn 203 NTHAWI yathadi bwerera mbale,
  • Hymn 38 ANGELO ayimba,
  • Hymn 469 NDIKONDA mbiri yomwe
  • Hymn 118 Musaone zobvalazo,
  • Hymn 398 KODI mbale wasimba zachikhululukiro,
  • Hymn 254 Adzanena kwa anthuwo
  • Hymn 842 Tipempha kuti Mpingo wanu
  • Hymn 193 A! Kumwamba
  • Hymn 1777 Mulungu wamkulu
  • Hymn 100 MUBWERE Mzimu Wakuyera,
  • Hymn 857 Mlungu amaunikira
  • Hymn 542 Kuli kaphiri m’talimo
  • Hymn 1044 Yesu sakusiya konse;
  • Hymn 1835 Mtima wanga lemekeza
  • Hymn 489 Yesu, ndikabwera,
  • Hymn 1559 Wotsogolera, munditsogolere
  • Hymn 1629 Adzabwera, adzabwera;
  • Hymn 554 Iye ndani pamtanda
  • Hymn 1497 Simbani mobwereza,
  • Hymn 382 M’wabatize anzathuwa,
  • Hymn 1663 Yesu Mbuye,
  • Hymn 1786 Ndikonda Mlungu pomva Mbuye wanga
  • Hymn 51 PANTHAWI yakufa Ambuye,
  • Hymn 1136 Mulungu anditsogolera
  • Hymn 1168 Aleluya, muyenera!
  • Hymn 1470 Chikondi cha Mbuyathu
  • Hymn 1552 Mpume pa inetu, Mpweya wa Mulungu,
  • Hymn 329 MUMZINDA wa Mulungu
  • Hymn 1100 Inde wakukonda ndinu;
  • Hymn 1574 Anthu ose ndi mitundu
  • Hymn 916 Akondwerera anthu
  • Hymn 444 YEMWE afesa nalira,
  • Hymn 188 Ine ndili ndi manyazi
  • Hymn 1344 Yamba ulendowo
  • Hymn 69 Kwathu sipadziko, ndingopitirira,
  • Hymn 1333 Idzatu kwa Yesuyo,
  • Hymn 64 LERO Kristu anauka,
  • Hymn 145 Kale ndinafuna
  • Hymn 256 Ndilira, ndilira,
  • Hymn 142 MULUNGU aŵakonda anthu
  • Hymn 1598 Mtiphunzitse, Mbuye Yesu,
  • Hymn 316 NDAMVATU kuti tifika komweko
  • Hymn 544 Zoopsya sitidziwapo
  • Hymn 444 Mpemphe Mbuye asunge
  • Hymn 372 DZUŴA la Mulungu
  • Hymn 946 Ngakhale enawo aleke kwimbako,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version