Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 422 DZIKO lonse lapansi,

  1. Home   »  
  2. Hymn 422 DZIKO lonse lapansi,

Hymn 422 DZIKO lonse lapansi,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 422 DZIKO lonse lapansi,

 

DZIKO lonse lapansi,
Linachimwa kwa Mlungu,
Chilango chake ndicho cha imfa;
Koma podza Yesuyo,
Anathetsa mlanduwo;
Potifera ife pamtandapo.

Onani,
Mwana wa Nkhosa,
Wachotsa tchimo lonse pansipa;
Ndiye Yesu Mfumuyo,
Ndiye Mpulumutsiyo;
Wotifera ife pamtandapo.

Tsono mmene tadziwa,
Kuti ndife ochimwa,
Tiyeni tinke kwa Ambuyewo;
Tisachite manyazi,
Tiwauze tchimolo;
Iwo adzatikhululukira.

Wotikhululukira,
Adzatiwuza tonse,
Kuti tisadzachimwenso ndithu;
Zakale zatha ndithu,
Zatsala zatsopano;
Tasamba mwazi wake tayera.

Post navigation

Previous: Hymn 421 ANTHU ali m’mdima akuyitanitsa,
Next: Hymn 423 MUNENE Mbuye, ’nenetu,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1018 Yesu afuna iwe unnke kwawoko,
  • Hymn 1192 Pamtanda woopsa
  • Hymn 1324 M’moyo uno kunsiku
  • Hymn 439 MLUNGU wathu mwatifitsa
  • Hymn 1741 Yesu munalaswa m’mtima,
  • Hymn 359 TADZUKA mzimu wanga ‘we,
  • Hymn 818 Mkhululukire,
  • Hymn 106 MZIMU Woyera, mudzetu,
  • Hymn 398 KODI mbale wasimba zachikhululukiro,
  • Hymn 226 BWENZI ndinamkomanayo
  • Hymn 1395 Mulungu ali nane!
  • Hymn 23 TIIMBE nyimbo zotamanda
  • Hymn 1374 Inu mumvere anyamatawo,
  • Hymn 1618 Anakwera,
  • Hymn 1745 Yesu aitana ife:
  • Hymn 1444 Wamoyo ndiye Yesudi,
  • Hymn 1755 Choti timtumikire
  • Hymn 446 YAMIKANI nonse ’nu,
  • Hymn 1630 Anthu anu amafoka,
  • Hymn 611 Tidzakhala naye nthawi zonse ndi kuimbako,
  • Hymn 892 Tilibe madalitso
  • Hymn 153 Pemphero ndiko kufuna,
  • Hymn 1686 Ndi mtima wonse mwimbedi
  • Hymn 1704 Zintchito zakezi
  • Hymn 636 Yehova Mlungu wathu,
  • Hymn 567 M’nyumba zonse ponseponse
  • Hymn 176 AITANA, aitana dziko lonse,
  • Hymn 1814 Thupi lamwazi wathu’li
  • Hymn 158 Mzimu, mlonge m’mtimamo
  • Hymn 209 Mdima ufika, dzuwa lalowa,
  • Hymn 13 PAPHIRI ndi padambo,
  • Hymn 537 Aleluya! Aleluya!
  • Hymn 52 POTULUKA m’mudzimo
  • Hymn 565 Koma sitimpenya m’khola
  • Hymn 313 MUNDIŴALIRE m’njira mwangamo,
  • Hymn 1725 Zochimwa zanga zonsezo
  • Hymn 1635 Pakwitana Mbuye wanga,
  • Hymn 1135 Mulungu anditsogolera,
  • Hymn 1563 Mufike monga nyali younika m’mtimamo,
  • Hymn 342 BWENZI lathu ndiye Yesu,
  • Hymn 800 Yesu munadzukanso
  • Hymn 483 NTHAŴI yaubwana yatha,
  • Hymn 256 Ndilira, ndilira,
  • Hymn 1313 Zindichulukirazi
  • Hymn 811 Wopulumutsa mudzetu;
  • Hymn 120 MUNDINYEMERE ’ne
  • Hymn 1274 Chisoni andichotsera Mbuyeyu,
  • Hymn 352 NONSE okhala pansipa,
  • Hymn 383 Zokoma ndi zakuyanja
  • Hymn 293 Tidziperekadi konse kwa Inu
  • Hymn 836 Kamoyo kanga katha lero lino,
  • Hymn 1056 Mkhalidwe wanu mundipatse,
  • Hymn 1816 Anatikondakonda ‘Ye,
  • Hymn 1004 A! mizimu yakuipa
  • Hymn 1438 Yesu akukonda,
  • Hymn 1306 Ndi ine ndasaukadi,
  • Hymn 1167 Mulungu wanga,
  • Hymn 1456 Pakuti anthu akumvera
  • Hymn 2 Ndinu wakuyera!
  • Hymn 271 Zoipa zangazi

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version