Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 469 NDIKONDA mbiri yomwe

  1. Home   »  
  2. Hymn 469 NDIKONDA mbiri yomwe

Hymn 469 NDIKONDA mbiri yomwe

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 469 NDIKONDA mbiri yomwe

 

NDIKONDA mbiri yomwe
Ya amithengawo
Ya Mbuye, Mfumu yathu
Pofika pansipa;
Zochimwa zindizinga,
Koma ndidziŵatu
Anawombola ine
Pakundikondadi.

Ndikondwa kuti Yesu ’Nakhala mwanatu,
Chitsanzo atipatsa
Cha moyo wakewo;
Ndikati ndimtsatire
Zochita zakezo,
Sadzandinyoza konse
Pakundikondadi.

Pakumyamika Iye
Ndidzamwimbiratu;
Ngakhale sindimwona
Amandimveradi;
Pakuti walonjeza
Adzalandira ’ne
Ndiimbe ndi angelo,
Pakundikondadi.

Post navigation

Previous: Hymn 468 NDIKONDWA kuti
Next: Hymn 470 YESU andikonda ine,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 701 Inu Atatuwo,
  • Hymn 467 Ife ana sitiopa,
  • Hymn 1548 Mtitsitsimutse ife
  • Hymn 1444 Wamoyo ndiye Yesudi,
  • Hymn 85 Mtima wanga wabvutika,
  • Hymn 72 YESU wakukoma mtima,
  • Hymn 1504 Kodi ali ndi chilemba
  • Hymn 779 Yesu Mbuye wanga,
  • Hymn 1501 Inde, pakufa panga
  • Hymn 445 Mlewe oipawo,
  • Hymn 972 Akristu limbikani,
  • Hymn 1799 Mulungu atipatsa mphamvu
  • Hymn 748 Ndiye wa moyo wonse Mwiniyo,
  • Hymn 850 Pemphero, pemphero,
  • Hymn 1839 Yehova ndiye Mbusa wanga sin’ngasowe konse;
  • Hymn 160 MADALITSO ngati mvumbi,
  • Hymn 1033 Mkristu gwiratu ntchito
  • Hymn 1076 Khalatu woyera,
  • Hymn 291 Ndi milomo yathu iyinso njanu,
  • Hymn 210 Nyumba yodyera ilikudzaza;
  • Hymn 1831 M’mitsinje yamtendere mtima wanga aumwetsa;
  • Hymn 1226 Wandipatsa moyo wake,
  • Hymn 15 YEHOVA ndiye Mbusa wanga,
  • Hymn 756 Sindili woyenera ‘ne,
  • Hymn 660 Tumizani kuunikako,
  • Hymn 965 Mundiuze, aulendo,
  • Hymn 71 DZIKO lino lapansi, ndilibetu abwenzi,
  • Hymn 904 Komweko akhala Yesuyo
  • Hymn 1333 Idzatu kwa Yesuyo,
  • Hymn 346 Aitana,
  • Hymn 262 Tumphatumpha moyo wanga,
  • Hymn 1523 Atisangalatsa,
  • Hymn 307 ABALE anga ine ndikupita,
  • Hymn 1564 Mufike monga moto wakuotcha zomwezo.
  • Hymn 1113 Mtima wa Mbuyako
  • Hymn 1730 Anapeputsidwako,
  • Hymn 179 Ndinachimwa poganiza
  • Hymn 1611 Nadzuka m’mandamo
  • Hymn 172 TADZA kukudyaku,
  • Hymn 1173 Sindinanyengedwa konse
  • Hymn 58 PAMTANDAPO Ambuyeyo
  • Hymn 124 PAMTANDAPO, pamtanda,
  • Hymn 1192 Pamtanda woopsa
  • Hymn 367 Nonse okhala pansipa,
  • Hymn 1286 E, ndikukhulupirani,
  • Hymn 599 Mlengi wathu Wakuyera,
  • Hymn 1640 Alinkudza Ambuye Yesu
  • Hymn 1045 Ambuye, ndifuna nditsukenitu;
  • Hymn 19 MULUNGU akhale nawo,
  • Hymn 676 Adze amitundu yonse,
  • Hymn 1456 Pakuti anthu akumvera
  • Hymn 70 LAMBIRA, Mfumuyo,
  • Hymn 104 MUBWERE Mzimu Inu
  • Hymn 995 Taya zako zochenjera,
  • Hymn 1003 Kanganani nkhondo yanu
  • Hymn 154 SING’ANGA ‘mkulu ndiye Yesu,
  • Hymn 46 O! ufulu tigwirizane
  • Hymn 1012 Ndi zipatsozo,
  • Hymn 392 ANU Mbuye ndifetu!
  • Hymn 714 Dzuwa ndi mvula yonseyo

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version