Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 469 NDIKONDA mbiri yomwe

  1. Home   »  
  2. Hymn 469 NDIKONDA mbiri yomwe

Hymn 469 NDIKONDA mbiri yomwe

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 469 NDIKONDA mbiri yomwe

 

NDIKONDA mbiri yomwe
Ya amithengawo
Ya Mbuye, Mfumu yathu
Pofika pansipa;
Zochimwa zindizinga,
Koma ndidziŵatu
Anawombola ine
Pakundikondadi.

Ndikondwa kuti Yesu ’Nakhala mwanatu,
Chitsanzo atipatsa
Cha moyo wakewo;
Ndikati ndimtsatire
Zochita zakezo,
Sadzandinyoza konse
Pakundikondadi.

Pakumyamika Iye
Ndidzamwimbiratu;
Ngakhale sindimwona
Amandimveradi;
Pakuti walonjeza
Adzalandira ’ne
Ndiimbe ndi angelo,
Pakundikondadi.

Post navigation

Previous: Hymn 468 NDIKONDWA kuti
Next: Hymn 470 YESU andikonda ine,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1459 Ambuye mulowetse
  • Hymn 113 Likalira llipengalo,
  • Hymn 1784 Komweko titasaukira,
  • Hymn 328 Yesu ndiye mphamvu yanga,
  • Hymn 118 Musaone zobvalazo,
  • Hymn 1489 Idzanitu, idzanitu,
  • Hymn 1484 Idzatu, idzatu
  • Hymn 217 E! kwa Inu, E! kwa Inu!
  • Hymn 350 MBUYE ndayima pano,
  • Hymn 393 Tilikuimba nyimbo yomweyi,
  • Hymn 988 Ndikhumba Mzimu wanu
  • Hymn 88 Yesu, dzina lakukonda,
  • Hymn 394 Titanka kwathu mkhale nafeko,
  • Hymn 267 Usekere moyo wanga,
  • Hymn 399 M’KHOLA mwa ng’ombe ku Betlehemu
  • Hymn 1416 Mbuye wanga ndilikumva,
  • Hymn 1360 Ndi Aleluya imbirani
  • Hymn 1848 Tiyamike Mlungu wathu
  • Hymn 807 Mpulumutsi tikagona
  • Hymn 259 Zoipa zakanikadi,
  • Hymn 710 Nthano ya Hananiyayo
  • Hymn 86 IYE wokhulupilira Yesu,
  • Hymn 1196 E! chikondi ndithu,
  • Hymn 190 Nsiku zonse kwanja kwake
  • Hymn 220 Kalekale ndinathawa,
  • Hymn 298 IFE tazingidwa ndi zinthu zoopsa,
  • Hymn 792 Dzuwa la Mulungu
  • Hymn 524 Wokoma Mbuyathu
  • Hymn 1205 Ndikonda chifukwa
  • Hymn 1013 Tizifesa m’dzuwa,
  • Hymn 1121 Ndifuna Yesuyo,
  • Hymn 1658 Idza wolema,
  • Hymn 1712 E! Yesu Mbuye wangadi,
  • Hymn 726 Mundidzze ndi chikondi,
  • Hymn 395 Usiku uno mutisungedi,
  • Hymn 83 MBUYEYO adzabwera,
  • Hymn 76 E, MOYO wanga’we
  • Hymn 929 Chikondano sichifera;
  • Hymn 266 MBUYE ndamva mwawazira
  • Hymn 1389 Tithawire kwa Mulungu,
  • Hymn 211 Chakudya ichi ndi cha iwenso,
  • Hymn 1734 “Senzani mtanda wanuwu.”
  • Hymn 11 NDI mitima yokondwera,
  • Hymn 367 MPULUMUTSI, tikagona
  • Hymn 1653 Mulungu ali wokhulula mtimatu,
  • Hymn 1357 Mlemekeze, anakonda
  • Hymn 1113 Mtima wa Mbuyako
  • Hymn 419 ANYAMATA a Mulungu,
  • Hymn 3 TIMYAMIKIRE Mlunguyo,
  • Hymn 450 YESU, munditsogoza
  • Hymn 1694 Timwimbire Mlungu wathu, Aleluya
  • Hymn 282 Ine ndili munthu
  • Hymn 801 Lero mwatipatsa moyo,
  • Hymn 327 Yesu salephera ‘yi.
  • Hymn 143 Lero lino Mbuye Yesu
  • Hymn 1075 Ndikhazikike inetu, mumtima muli mwai,
  • Hymn 589 Koma ineyu
  • Hymn 74 IDZA wolema,
  • Hello world!
  • Hymn 101 MZIMU Woyera, mudze mumitima mwathumo,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version