Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 81 MBUYE Yesu adzabwera,

  1. Home   »  
  2. Hymn 81 MBUYE Yesu adzabwera,

Hymn 81 MBUYE Yesu adzabwera,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 81 MBUYE Yesu adzabwera,

 

MBUYE Yesu adzabwera,
Asekere anthu onse;
Mawu awa achimwemwe
Azimveka m’dziko lonse.
Adzabwera, adzabwera;
E! bwerani Mbuye wathu.

Dziko lino linaona
Masauko a Mbuyathu,
Lidzaonanso ulemu,
M’mene adzabwera Iye.
Adzabwera, adzabwera;
Timvomera, E! mubwere

Anthu anu amafoka,
Pa ulendo nasokera;
Ha! Adzaonana nanu
Atabvalanso zoyera.
Mudzabwera, mudzabwera;
Inde Mbuyetu mubwere.

Ndi chiyembekezo ichi
Sitikhala chete ife:
Tiimbitsa nyimbo zathu
Zakulemekeza Mlungu.
Adzabwera, adzabwera
E!! mubwere msanga YESU.

Post navigation

Previous: Hymn 80 KUDZA kwa Mbuye
Next: Hymn 82 YANG’ANANI, anthu onse,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1077 Khalatu woyera,
  • Hymn 121 Imbira!
  • Hymn 257 Ndinasiya amayi,
  • Hymn 733 Ndimamva ludzu Yesu,
  • Hymn 880 Bwenzi lathu ndiye Yesu
  • Hymn 1351 Aleluya, Aleluya,
  • Hymn 120 MUNDINYEMERE ’ne
  • Hymn 780 Kwezani mitu yanuyo,
  • Hymn 392 Chimwemwe chomwe mpatseko
  • Hymn 985 Zonse zapadziko
  • Hymn 1245 Ine ndidzakuonetsa
  • Hymn 805 Madzulo ano mkhaletu
  • Hymn 1489 Idzanitu, idzanitu,
  • Hymn 1384 Mphamvu yake inalenga
  • Hymn 1561 Mzimu Woyera, n’dzipereka ndense,
  • Hymn 1714 Tiyeni, dzalireni nane,
  • Hymn 68 Kwathu ndidzaimba nyimbo
  • Hymn 1404 “Undipatsetu
  • Hymn 1295 Ambuye, mwazi wanuwo
  • Hymn 75 Ndiperekatu
  • Hymn 143 Lero lino Mbuye Yesu
  • Hymn 197 NDIKHULUPIRA’Nu,
  • Hymn 1522 Tikaona bvuto,
  • Hymn 822 Dzuwa lapitira,
  • Hymn 1759 Powalitsira omwe
  • Hymn 1375 Ndi anamwali obvekedwa mbuu!
  • Hymn 222 Ndilikudzatu,
  • Hymn 1649 Kutenga inetu, kutenga inetu
  • Hymn 835 Mukhale ndine, dzuwalo lalowa,
  • Hymn 526 Mnandidzera, Ambuye,
  • Hymn 1315 Ambuye ‘naitana ‘ne:
  • Hymn 1064 Moyowo
  • Hymn 419 ANYAMATA a Mulungu,
  • Hymn 4 INU Mulungu, tikuyamikani;
  • Hymn 1701 Nditani Bwenzi langa
  • Hymn 1334 Walandira inetu
  • Hymn 398 Lero lino mwatipatsa
  • Hymn 1255 Chitha nchiani kund’yeretsa?
  • Hymn 1142 Tidzathawira kuti ‘fe
  • Hymn 1616 Anafera
  • Hymn 1394 Paphiri ndi padambo
  • Hymn 1700 Ambuye Mwini moyo,
  • Hymn 166 Yendani, Munthu Wachisoni,
  • Hymn 1560 Mthandizi ndinu, mndithangate ine
  • Hymn 1439 Iwetu afuna,
  • Hymn 1721 Mapazi ake namvatu
  • Hymn 738 Mommuno, Mbuye, mkate wanuwu,
  • Hymn 1589 Ndinasokera kalelo,
  • Hymn 265 MUDZAZE Yesu mtima wanga ndi chikondicho,
  • Hymn 1089 Ndionetsere kuunika
  • Hymn 1213 Mwamva Yesu m’mtimamo,
  • Hymn 339 MTIMA wanga ndikonzera,
  • Hymn 1038 Limbikani nonse
  • Hymn 1854 Tate msandipitirire,
  • Hymn 1645 Nafera inetu, nafera inetu
  • Hymn 243 KONDWANI nonsenu,
  • Hymn 1281 Ndikhulupirira, Yesu, mndibvomereko;
  • Hymn 1844 Pamaso pa adaniwo mwayala gome langa;
  • Hymn 1229 Dzinalo la Yesu,
  • Hymn 1403 ‘Mvani liwu lomwe

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version