Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 81 MBUYE Yesu adzabwera,

  1. Home   »  
  2. Hymn 81 MBUYE Yesu adzabwera,

Hymn 81 MBUYE Yesu adzabwera,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 81 MBUYE Yesu adzabwera,

 

MBUYE Yesu adzabwera,
Asekere anthu onse;
Mawu awa achimwemwe
Azimveka m’dziko lonse.
Adzabwera, adzabwera;
E! bwerani Mbuye wathu.

Dziko lino linaona
Masauko a Mbuyathu,
Lidzaonanso ulemu,
M’mene adzabwera Iye.
Adzabwera, adzabwera;
Timvomera, E! mubwere

Anthu anu amafoka,
Pa ulendo nasokera;
Ha! Adzaonana nanu
Atabvalanso zoyera.
Mudzabwera, mudzabwera;
Inde Mbuyetu mubwere.

Ndi chiyembekezo ichi
Sitikhala chete ife:
Tiimbitsa nyimbo zathu
Zakulemekeza Mlungu.
Adzabwera, adzabwera
E!! mubwere msanga YESU.

Post navigation

Previous: Hymn 80 KUDZA kwa Mbuye
Next: Hymn 82 YANG’ANANI, anthu onse,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1621 Yang’anani anthu onse,
  • Hymn 485 POMPANO pandikonda
  • Hymn 100 MUBWERE Mzimu Wakuyera,
  • Hymn 1551 Mukhale m’kati mwathu,
  • Hymn 1088 Mndiyandikitse nanu, Yesu,
  • Hymn 178 ZAMBIRI zogona m’kholamo,
  • Hymn 1357 Mlemekeze, anakonda
  • Hymn 349 Aitana,
  • Hymn 906 Mulibe zoipa m’Dzikolo,
  • Hymn 1591 Sizitha ntchito zangazo,
  • Hymn 106 Ife, tapulumukadi,
  • Hymn 990 Poyesedwa ine
  • Hymn 446 Yesu alandira
  • Hymn 15 Mbuye, chifundo chanu chitigwere
  • Hymn 999 Amaliwongo ochuluka amalowa m’mtima
  • Hymn 331 Yesu ndimafuna Inu,
  • Hymn 349 MOSE anamenya thanthwe kawiri,
  • Hymn 248 M’MENE ine ndisauka
  • Hymn 851 E, nthawi ya mamawayi
  • Hymn 1061 Mundichotsere tchimo lonse
  • Hymn 259 CHISOMO chodabwitsacho,
  • Hymn 1507 Ndikampempha anditenge,
  • Hymn 115 Mbulu wanding’amba m’nthiti,
  • Hymn 1003 Kanganani nkhondo yanu
  • Hymn 384 USIKU uja kalero,
  • Hymn 644 M’wasunge, m’wayendetse
  • Hymn 832 Zochimwa za usana uno mndikhululukire ‘ne;
  • Hymn 353 Anatuma Mtetezi,
  • Hymn 14 MTIMA wanga uyamike,
  • Hymn 1711 Kwa munthu wasokerayo
  • Hymn 350 Yesu ati,
  • Hymn 88 Ufuna kuwomboledwa kodi?
  • Hymn 44 Mlungu dalitsani Malawi,
  • Hymn 1444 Wamoyo ndiye Yesudi,
  • Hymn 1463 Zoipa zakhululukidwa,
  • Hymn 1420 Abale ‘nu, abale ‘nu,
  • Hymn 1404 “Undipatsetu
  • Hymn 364 Ali wokhululukira;
  • Hymn 1563 Mufike monga nyali younika m’mtimamo,
  • Hymn 151 Inde, Yesu, mulandira,
  • Hymn 199 NDINASOKERA kutali,
  • Hymn 1443 Ambuye Yesu anatsira
  • Hymn 1445 Tiyeni tonse, tinkeko
  • Hymn 284 MAVUTO ndi ambiri,
  • Hymn 700 Mzimu woonadi
  • Hymn 252 MTIMA wa Mbuyako,
  • Hymn 1614 Anabadwa,
  • Hymn 1389 Tithawire kwa Mulungu,
  • Hymn 155 Pemphero ndiko kufuna
  • Hymn 376 PAMTANDA Mbuye anafera,
  • Hymn 1856 Mzimu, msandipitirire,
  • Hymn 1761 Amithenga anaimba
  • Hymn 490 Yesu, ndikabwera
  • Hymn 1263 Mbuye, ndingogonj tere, Ndibvomerapo;
  • Hymn 1518 Zonse mwazilembamo,
  • Hymn 1004 A! mizimu yakuipa
  • Hymn 202 NDIKHULUPIRIRA, Yesu,
  • Hymn 893 Mtima wanga ndikonzera,
  • Hymn 1218 Pakufa pangapo
  • Hymn 909 Ife tikondwera, ife tikondwera,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version