Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 4 INU Mulungu, tikuyamikani;

  1. Home   »  
  2. Hymn 4 INU Mulungu, tikuyamikani;

Hymn 4 INU Mulungu, tikuyamikani;

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 4 INU Mulungu, tikuyamikani;

 

INU Mulungu, tikuyamikani;
Tivomereza ndinu Ambuyathu;
Ponse, atate, akugwadirani,

Nanu akukuzani amithenga,
Nanu zam’mwamba ndi zamphamvu zake,
Nanu angelo a mitundu yonse
Akuimbirani:

“Mbuye Woyera! E, Woyera nokha!
Mbuye Woyera! Mbuye wa makamu!
Ponse ulemu wanu ndi wodzaza;
Pansi ndi Kumwamba.”

Inu atumwi akumweka aja,
Ndi aneneri oyanjana omwe;
Ndi aunyinji anakuferani;
Akuyamikani.

Mpingo Woyera! wa kwa anthu onse;
Ukumverani, Mfumu ndi Atate,
Mwana woona wa ulemu wonse,
Mzimu, Nkhoswe yemwe.

Khristu Mfumuyo yaulemerero!
Mwana wosatha wa Atate ndinu!
Simunanyoza mimba ya Namwali;
Potipulumutsa.

Imfa mutagonjetsa ndi zoŵaŵa.
Njira munatsegula tikaloŵe;
Momwe mukhala Inu ndi Atate;
Mu ulemerero

Kumva milandu yathu mudzabwera;
Mutithandize, atumiki anu;
Mwatiwombola nawo mwazi wanu;
Mutipulumutse.

M’tiŵerengere
M’Mwamba ndi oyera;
Mutidalitse, ndi’fe anthu anu;
Moyo wosatha, mutipatse tonse;
Mutilamulire.

Tsiku ndi Tsiku timalemekeza;
Nanu tikukuzani osaleka;
Mbuye, m’tisunge tingachimwe lero;
M’tichitire nsisi.

Mbuye, chifundo chanu chitigwere;
Monga tikhulupi’ra inu nokha;
Takhulupi’ra zedi mwa’Nu, Mbuye;
Tisagome konse!

Post navigation

Previous: Hymn 3 TIMYAMIKIRE Mlunguyo,
Next: Hymn 5 ATATE wa Kumwambako,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1294 Wakuba uja nachiona,
  • Hymn 1680 Aleluya, Aleluya, Aleluya!
  • Hymn 79 Mlendo ali pakhomo,
  • Hymn 105 IDZANI, Mzimu Inu,
  • Hymn 1195 Wafunafuna ine
  • Hymn 1071 Kumwamba Yesu mthandize,
  • Hymn 979 Limbikani inu nonse,
  • Hymn 1589 Ndinasokera kalelo,
  • Hymn 952 Ndimayenda paulendo,
  • Hymn 829 Titamadi ‘Tate,
  • Hymn 244 Ndidze pafupi pa
  • Hymn 1522 Tikaona bvuto,
  • Hymn 1658 Idza wolema,
  • Hymn 721 Anu Mbuye ndifetu!
  • Hymn 406 M’MENE umauka m’maŵa,
  • Hymn 182 Kondwani nonsenu,
  • Hymn 1404 “Undipatsetu
  • Hymn 69 KONDWERANI dzuŵa lino,
  • Hymn 1845 Zabwino ndi zokoma zinditsata chitsatire;
  • Hymn 1724 Ambuye mthandize inetu
  • Hymn 1343 M’dzina la Yesuyo
  • Hymn 834 Tiyamike Mlungu wotipatsa zachifundozi,
  • Hymn 1529 Mndithandize kukondana
  • Hymn 216 NDISAUKA, ndinachimwa,
  • Hymn 583 Anabadwa,
  • Hymn 274 YESU and’itana,
  • Hymn 666 Walitsani nyali yanu
  • Hymn 1323 M’manja mopanda kanthu,
  • Hymn 115 NTHAWI ija ya Sauli,
  • Hymn 888 Polowa ndi Inu
  • Hymn 353 Anatuma Mtetezi,
  • Hymn 309 ANA akumwamba ndife,
  • Hymn 411 Yesu adza kukundika
  • Hymn 658 Ndichitireni, Mbuye ‘ne,
  • Hymn 463 MNANDIDZERA, Ambuye,
  • Hymn 712 Mulungu akondadi leroli
  • Hymn 393 Tilikuimba nyimbo yomweyi,
  • Hymn 233 M’mene ndapenya mwazi wa
  • Hymn 1754 Ndiye akumbukira
  • Hymn 1822 Lawani chikondano chake;
  • Hymn 188 MPULUMUTSI Wokondedwa,
  • Hymn 984 Mpingo wa Mulungu
  • Hymn 482 Ndinu wakuyera,
  • Hymn 915 Mumzinda wa Mulungu
  • Hymn 342 Ambiri,
  • Hymn 207 Malo alimo m’nyumba ya Yesu,
  • Hymn 308 Ifetu kuchimwa, Mbuye,
  • Hymn 206 Uzanitu abale,
  • Hymn 1409 Kodi mufunatu Yesu?
  • Hymn 385 Tsopano, poyamba paja,
  • Hymn 408 Oipa tili tonsefe;
  • Hymn 328 KULIBE vuto
  • Hymn 1465 Akulu inu m’bwere nonse,
  • Hymn 645 Kristu ndiye mwala wathu,
  • Hymn 277 GWIRA zintchito zako,
  • Hymn 1367 Wamphamvu yosatha,
  • Hymn 1133 Ngatitu abwenzi anga
  • Hymn 1510 Mtume tsopanoli
  • Hymn 1128 Mbuyanga Yesu, mundisunge ine
  • Hymn 1650 E, moyo wanga’we

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version