Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 4 INU Mulungu, tikuyamikani;

  1. Home   »  
  2. Hymn 4 INU Mulungu, tikuyamikani;

Hymn 4 INU Mulungu, tikuyamikani;

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 4 INU Mulungu, tikuyamikani;

 

INU Mulungu, tikuyamikani;
Tivomereza ndinu Ambuyathu;
Ponse, atate, akugwadirani,

Nanu akukuzani amithenga,
Nanu zam’mwamba ndi zamphamvu zake,
Nanu angelo a mitundu yonse
Akuimbirani:

“Mbuye Woyera! E, Woyera nokha!
Mbuye Woyera! Mbuye wa makamu!
Ponse ulemu wanu ndi wodzaza;
Pansi ndi Kumwamba.”

Inu atumwi akumweka aja,
Ndi aneneri oyanjana omwe;
Ndi aunyinji anakuferani;
Akuyamikani.

Mpingo Woyera! wa kwa anthu onse;
Ukumverani, Mfumu ndi Atate,
Mwana woona wa ulemu wonse,
Mzimu, Nkhoswe yemwe.

Khristu Mfumuyo yaulemerero!
Mwana wosatha wa Atate ndinu!
Simunanyoza mimba ya Namwali;
Potipulumutsa.

Imfa mutagonjetsa ndi zoŵaŵa.
Njira munatsegula tikaloŵe;
Momwe mukhala Inu ndi Atate;
Mu ulemerero

Kumva milandu yathu mudzabwera;
Mutithandize, atumiki anu;
Mwatiwombola nawo mwazi wanu;
Mutipulumutse.

M’tiŵerengere
M’Mwamba ndi oyera;
Mutidalitse, ndi’fe anthu anu;
Moyo wosatha, mutipatse tonse;
Mutilamulire.

Tsiku ndi Tsiku timalemekeza;
Nanu tikukuzani osaleka;
Mbuye, m’tisunge tingachimwe lero;
M’tichitire nsisi.

Mbuye, chifundo chanu chitigwere;
Monga tikhulupi’ra inu nokha;
Takhulupi’ra zedi mwa’Nu, Mbuye;
Tisagome konse!

Post navigation

Previous: Hymn 3 TIMYAMIKIRE Mlunguyo,
Next: Hymn 5 ATATE wa Kumwambako,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 73 M’SANDIPITILIRE Yesu,
  • Hymn 1776 Tiyeni timgwadire
  • Hymn 66 Chisomocho chachotsadi
  • Hymn 931 Tikagwidwa ndi chisoni,
  • Hymn 342 Ambiri,
  • Hymn 750 Yesu Mbuyathu, Inu nomwe ‘Nu,
  • Hymn 249 MBUYANGA Yesu, mundigwire
  • Hymn 173 Mema nkhondoyo, wadza mdaniyo,
  • Hymn 899 ‘Tate wa Kumwambako,
  • Hymn 198 CHITSIMECHO cha mwaziwo
  • Hymn 245 KHALANI duu! Ambuye adzatu;
  • Hymn 727 Imfa ikandifikira,
  • Hymn 422 Kwathu nkopambana,
  • Hymn 252 MTIMA wa Mbuyako,
  • Hymn 976 Muyendenso kunka komwe,
  • Hymn 1672 Lambira Mfumuyo,
  • Hymn 283 Ndalema ndathodwa
  • Hymn 1080 Ambuye mundisunge
  • Hymn 316 Ndikhazikike inetu,
  • Hymn 785 Yehova adalitse ‘nu,
  • Hymn 1673 Lambira Yesuyo
  • Hymn 1207 Poyambapo ndakondwadi,
  • Hymn 670 Isaleke ntchito yake
  • Hymn 1794 Mulungu awakonda anthu
  • Hymn 948 Tiimbe mokondwa, misozi iume;
  • Hymn 1754 Ndiye akumbukira
  • Hymn 920 Yatha misoziyo,
  • Hymn 126 DAVIDE kubusa kuja,
  • Hymn 185 NDINE Mbusayo wabwino,
  • Hymn 209 M’NDILANDIRE ine Mbuye
  • Hymn 867 Akristu ndi abale, tiziyenderana tonse,
  • Hymn 684 Zipata zatsegudwa mbee! Za m’dziko monsemo;
  • Hymn 1182 Chikhulupiro chomwenso
  • Hymn 1329 M’tali mutali m’phirimo
  • Hymn 807 Mpulumutsi tikagona
  • Hymn 246 NAMONDWE akawombabe,
  • Hymn 1698 Chinkana dziko lonselo
  • Hymn 173 MWAMVA Mawu a Mulungu;
  • Hymn 1216 Ndatsatatsatabe
  • Hymn 1690 Titama Yesuyo,
  • Hymn 1634 Pakwitana Mbuye wanga
  • Hymn 86 IYE wokhulupilira Yesu,
  • Hymn 735 Mwa chikho chokumbutsa
  • Hymn 97 TIYAMIKE Mlunguyo,
  • Hymn 706 Tisaiwalire ‘bale
  • Hymn 917 Ndi nkhondo ikaleka
  • Hymn 91 NDITAME Mlungu m’mtimamo,
  • Hymn 319 NDIDZATANI ine,
  • Hymn 490 Yesu, ndikabwera
  • Hymn 599 Mlengi wathu Wakuyera,
  • Hymn 1141 Pakulekana ifetu
  • Hymn 1492 Sakukanani Yesudi,
  • Hymn 1614 Anabadwa,
  • Hymn 1255 Chitha nchiani kund’yeretsa?
  • Hymn 1702 Pakufa ine Mbuye
  • Hymn 175 Mlungu mverani, mphamvu patseni,
  • Hymn 116 Nkhosa zanga zimandimva
  • Hymn 1091 Mulamulire mtima, Yesu,
  • Hymn 1044 Yesu sakusiya konse;
  • Hymn 305 M’mwazi wake tisambamo;

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version