Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 82 YANG’ANANI, anthu onse,

  1. Home   »  
  2. Hymn 82 YANG’ANANI, anthu onse,

Hymn 82 YANG’ANANI, anthu onse,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 82 YANG’ANANI, anthu onse,

 

YANG’ANANI, anthu onse,
Yesu Mbuye wathuyo:
Alinkudza ndi ulemu,
Kuoneka m’Mwambamo.

Anthu onse am’lambire
Yesu Mwana wa Mulungu
Alinkudza ndi ulemu
Wopambana, indetu.

Adzatenga anthu ake
Akumvera pansipo
Iwo adzakhala naye
M’dziko la Kumwambako.

Koma anthu onse omwe
Anamnyoza pansipo,
Nthaŵi Yesu alinkudza
Adzaopa m’mtimamo.

Ife tonse tikumbuke
Mawu ake onsewo;
Timuyang’anire Iye,
Yesu Mbuye wathuyo.

Post navigation

Previous: Hymn 81 MBUYE Yesu adzabwera,
Next: Hymn 83 MBUYEYO adzabwera,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1283 Yesu ndikhulupirira
  • Hymn 482 TCHIMO musalole, musadziipitse,
  • Hymn 1221 Bwenzi ndinamkomanayo,
  • Hymn 222 NDILIKUMVA m’mtima mwanga
  • Hymn 1638 Alinkudza wansoni Munthu
  • Hymn 264 Bvinabvina moyo wanga,
  • Hymn 1131 M’mene ine ndisauka
  • Hymn 1023 Kodi m’njiramo ndimvadi
  • Hymn 598 Mlungu ali nane;
  • Hymn 114 Ndine Mbusayo wabwino,
  • Hymn 8 Nanu Atumwi akumveka aja,
  • Hymn 357 Yesu ndiye Mtetezi,
  • Hymn 350 MBUYE ndayima pano,
  • Hymn 98 Ndidzamwona maso ndi maso
  • Hymn 632 Tsopano tipereka mapemphero athu ano,
  • Hymn 139 Bwerani inu nonse, inu nonse,
  • Hymn 1757 Udzadziwitsa anthu
  • Hymn 796 Timvere Mawu anu
  • Hymn 899 ‘Tate wa Kumwambako,
  • Hymn 1377 Ndi amithenga akumwambako,
  • Hymn 1381 Ndi mitima yokondwera
  • Hymn 1413 Ndichitenji kukapeza
  • Hymn 1554 Mpume pa inetu, Mpweya wa Mulungu,
  • Hymn 890 Kumbuka ‘bale ako
  • Hymn 1103 Ndakudani, mnandikonda
  • Hymn 507 Yesu ndimkonda, akondanso ine,
  • Hymn 1810 Kalelo Mbuye Yesu
  • Hymn 626 Inde, ‘Tate, mtiyendetse
  • Hymn 2 Ndinu wakuyera!
  • Hymn 271 Pomwalira Mbuyeyo
  • Hymn 969 Akathira nsembe
  • Hymn 538 Iye anachoka kwawo,
  • Hymn 1459 Ambuye mulowetse
  • Hymn 673 Mbwere Mzimu Wakuyera,
  • Hymn 463 MNANDIDZERA, Ambuye,
  • Hymn 430 MLUNGU akuyang’aniredí,
  • Hymn 1252 Pakukumbukira zanga
  • Hymn 1089 Ndionetsere kuunika
  • Hymn 60 ZATHEDWA zonsetu
  • Hymn 811 Wopulumutsa mudzetu;
  • Hymn 185 NDINE Mbusayo wabwino,
  • Hymn 90 Ufuna kuleka kunyadako?
  • Hymn 920 Yatha misoziyo,
  • Hymn 31 Tamandani mbuye,
  • Hymn 483 NTHAŴI yaubwana yatha,
  • Hymn 145 Kale ndinafuna
  • Hymn 1669 Ukafuna kumdziwitsa,
  • Hymn 953 Ichi chindisangalatsa
  • Hymn 354 Tinafunafunatu,
  • Hymn 995 Taya zako zochenjera,
  • Hymn 1126 Ndifuna Inu, Yesu,
  • Hymn 223 Ndafoka, ndaipa,
  • Hymn 441 MBUYE, tikuthokozani,
  • Hymn 1803 Nowayo nayendamo,
  • Hymn 1425 Apempha malo Ambuye;
  • Hymn 1593 Wina atikonda ife,
  • Hymn 1725 Zochimwa zanga zonsezo
  • Hymn 528 Amithenga ‘naimba pamlengapo,
  • Hymn 340 PEMPHERA m’mbanda kucha,
  • Hymn 1343 M’dzina la Yesuyo

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version