Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 82 YANG’ANANI, anthu onse,

  1. Home   »  
  2. Hymn 82 YANG’ANANI, anthu onse,

Hymn 82 YANG’ANANI, anthu onse,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 82 YANG’ANANI, anthu onse,

 

YANG’ANANI, anthu onse,
Yesu Mbuye wathuyo:
Alinkudza ndi ulemu,
Kuoneka m’Mwambamo.

Anthu onse am’lambire
Yesu Mwana wa Mulungu
Alinkudza ndi ulemu
Wopambana, indetu.

Adzatenga anthu ake
Akumvera pansipo
Iwo adzakhala naye
M’dziko la Kumwambako.

Koma anthu onse omwe
Anamnyoza pansipo,
Nthaŵi Yesu alinkudza
Adzaopa m’mtimamo.

Ife tonse tikumbuke
Mawu ake onsewo;
Timuyang’anire Iye,
Yesu Mbuye wathuyo.

Post navigation

Previous: Hymn 81 MBUYE Yesu adzabwera,
Next: Hymn 83 MBUYEYO adzabwera,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1601 Zina za Yesu ndimvetu,
  • Hymn 1317 Ambuye naitana ‘ne:
  • Hymn 123 MULI ndi ludzu, idzani
  • Hymn 1229 Dzinalo la Yesu,
  • Hymn 1493 Mbiri yakalelomwe
  • Hymn 1552 Mpume pa inetu, Mpweya wa Mulungu,
  • Hymn 1775 Oonadi mtima,
  • Hymn 1274 Chisoni andichotsera Mbuyeyu,
  • Hymn 640 Anakwatira kale
  • Hymn 1556 Mzimu Woyera, mudzetu kwa ine,
  • Hymn 321 Ndi ponse paphiri ndi padambopo
  • Hymn 1195 Wafunafuna ine
  • Hymn 262 Tumphatumpha moyo wanga,
  • Hymn 586 Yesu Mfumu,
  • Hymn 1437 Yesu ndi wokonda;
  • Hymn 307 Atate Wamkulu ndi wamphamvu zonse,
  • Hymn 1562 Mzimu Woyera, mudze mumitima mwathumo,
  • Hymn 1696 Mndiletse, ndisateme ‘yi
  • Hymn 460 KULI kaphiri m’talimo
  • Hymn 393 Tilikuimba nyimbo yomweyi,
  • Hymn 15 YEHOVA ndiye Mbusa wanga,
  • Hymn 59 IMVANI uthenga,
  • Hymn 79 Mlendo ali pakhomo,
  • Hymn 1497 Simbani mobwereza,
  • Hymn 1629 Adzabwera, adzabwera;
  • Hymn 345 Ubwere,
  • Hymn 251 NDIFUNA Yesuyo,
  • Hymn 1602 M’mawu a Yesu Mbuyeyo,
  • Hymn 478 Ndife ana, mutikonda,
  • Hymn 1717 Mtima wangawe, uyenera
  • Hymn 284 MAVUTO ndi ambiri,
  • Hymn 1176 Sandinyenga, salephera;
  • Hymn 51 Mbuye dalitsani Afrika,
  • Hymn 129 WODALA ndiye munthuyo,
  • Hymn 1125 Ndifuna Inu, Yesu,
  • Hymn 1551 Mukhale m’kati mwathu,
  • Hymn 372 Potero onsewo
  • Hymn 840 Ambuye munapatsa tsiku
  • Hymn 919 ‘Tate, mwa kusunga kwanu
  • Hymn 1486 M’dziko lino pansi pano
  • Hymn 1171 Mulungu wanga
  • Hymn 995 Taya zako zochenjera,
  • Hymn 718 Anu Mbuye ndifetu!
  • Hymn 218 Mbuye Yesu ndi Atate,
  • Hymn 1615 Anakonda,
  • Hymn 455 TIIMBE ndi kulalikira
  • Hymn 1699 A! Mutu wakuyera,
  • Hymn 674 Anthu onse taukani,
  • Hymn 466 OSANATU, osana,
  • Hymn 1096 Tifuna Inu, Mbuye,
  • Hymn 264 KHALATU woyera, pempheratu m’tseri;
  • Hymn 589 Koma ineyu
  • Hymn 490 Yesu, ndikabwera
  • Hymn 622 Tiyamikira ‘Tate,
  • Hymn 101 MZIMU Woyera, mudze mumitima mwathumo,
  • Hymn 239 Akumwambawo
  • Hymn 776 Tikondwereratu
  • Hymn 1403 ‘Mvani liwu lomwe
  • Hymn 102 Mzimu ndi mtsogoleri
  • Hymn 290 Ndi miyendo yathu iyinso njanu,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version