Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 457 KALE m’mzinda wachifumu

  1. Home   »  
  2. Hymn 457 KALE m’mzinda wachifumu

Hymn 457 KALE m’mzinda wachifumu

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 457 KALE m’mzinda wachifumu

 

KALE m’mzinda wachifumu
Munalimo m’kholamo,
Momwe mkazi anaika
Mwana wake m’ndyeromo.
Ndiye mkaziyo Mariya,
Yesu Kristu Mwanayo.

Uyu ’natsikira kuno,
Mlungu Mbuye wathuyo;
Anabadwa uyu m’khola
Anagona m’ndyeromo.
Mwa osoŵa ndi oipa
Yesu anakhalamo.

Mwa ubwana wake wonse
Anakula m’mtima phee!
Anakonda, anafatsa,
Amay’ wake namvabe;
Ndipo ana nonsenu,
Mukamtsate bwinotu.

Ndipo Mwana uyu Yesu
Anakulakulabe;
Ndi wamng’ono ndi wofoka,
Anagona enawo.
Nsoni zathu anazimva
Ndi chimwemwe chathunso.

Ndi chifukwa atikonda,
Tidzampenya masowa,
Kuti Mwanayo wofatsa
Ndiye Mwini m’Mwambamo;
Atengera ana ake
Komwe adapitako.

Koma sitimpenya m’khola
Muli ng’ombe momwemo;
Ayi, tidzamwona m’Mwamba
Muli Mlungu ’Tatewo.
Ana akuyera mbuu
Adzamzunguliratu.

Post navigation

Previous: Hymn 456 ANA inu, ana inu,
Next: Hymn 458 USIKUWO, woyerawo!

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 91 Ufuna kuyera kopambana?
  • Hymn 269 NDILIRA ine kukayenda
  • Hymn 765 Chikondi chili m’chikhomu
  • Hymn 1508 Mundinyemere ‘ne
  • Hymn 1533 Ndipatsa inu mtimawu,
  • Hymn 1293 Chitsimecho cha mwaziwo
  • Hymn 1820 Kwezani nane Ambuyathu,
  • Hymn 482 TCHIMO musalole, musadziipitse,
  • Hymn 197 NDIKHULUPIRA’Nu,
  • Hymn 392 Chimwemwe chomwe mpatseko
  • Hymn 537 Aleluya! Aleluya!
  • Hymn 308 Ifetu kuchimwa, Mbuye,
  • Hymn 1151 Pomulambira Yesu Mbuyanga,
  • Hymn 1284 Kale ndinalira Inu,
  • Hymn 592 Kuti m’Mwambamo
  • Hymn 1770 Iye amazichita zamphamvu
  • Hymn 561 Uyu ‘natsikira kuno,
  • Hymn 1652 Mabala ajawo
  • Hymn 966 Kodi inu, aulendo,
  • Hymn 1794 Mulungu awakonda anthu
  • Hymn 654 Ndilimbikitse, Mbuye, nji!
  • Hymn 908 Ndikonda kuganizirabe
  • Hymn 470 YESU andikonda ine,
  • Hymn 545 Anatifera tonsefe
  • Hymn 95 Palibe mmodzi akanatha
  • Hymn 747 Tadzanitu, okhulupiradi,
  • Hymn 1413 Ndichitenji kukapeza
  • Hymn 159 Kamwana Yesu ‘nabadwa,
  • Hymn 479 ANYAMATA inutu,
  • Hymn 432 KRISTU ndiye Mwala wathu,
  • Hymn 1358 Lemekeza Mfumu yathu,
  • Hymn 410 Ana ake angonga
  • Hymn 1086 “Khala mwa Ine,” ndinu mwini moyo,
  • Hymn 808 Atipsinjadi masoka,
  • Hymn 237 Munasiyatu
  • Hymn 1300 Poyenda m’mdima bii,
  • Hymn 458 USIKUWO, woyerawo!
  • Hymn 738 Mommuno, Mbuye, mkate wanuwu,
  • Hymn 58 PAMTANDAPO Ambuyeyo
  • Hymn 1660 Ndikakhumudwa
  • Hymn 1426 Wina panalibe
  • Hymn 1725 Zochimwa zanga zonsezo
  • Hymn 995 Taya zako zochenjera,
  • Hymn 1076 Khalatu woyera,
  • Hymn 570 Ndikhulupirira Yesu
  • Hymn 503 Ndikondwa kuti Yesu
  • Hymn 459 Aphunzitse anthuwo,
  • Hymn 776 Tikondwereratu
  • Hymn 1853 Etu ine, etu ine,
  • Hymn 1790 Imfa ya anthu ake imkomera,
  • Hymn 1014 Tingolira kaya,
  • Hymn 420 FESANI mbewuzo,
  • Hymn 169 ’MVANI liu lomwe
  • Hymn 254 PAMENE ndisawuka,
  • Hymn 278 Aweruza ndi mphamvu
  • Hymn 892 Tilibe madalitso
  • Hymn 368 MULUNGU wanga, Dzuŵatu
  • Hymn 644 M’wasunge, m’wayendetse
  • Hymn 327 NTCHITO yonse yakeyo
  • Hymn 182 Kondwani nonsenu,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version