Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 147 MUSAŴALOLE mawuwo

  1. Home   »  
  2. Hymn 147 MUSAŴALOLE mawuwo

Hymn 147 MUSAŴALOLE mawuwo

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 147 MUSAŴALOLE mawuwo

 

MUSAŴALOLE mawuwo
Apite ngati mphepozi,
Musaumitse mtimatu,
Polira Yesu Mbuyedi.

Idzanitu, idzanitu,
Idzani kwa Ambuyeyo.
Idzanitu, idzanitu
Apulumutse inunso.

Musachitenso nthantha ’yi,
Mufulumire inutu;
Tsiku labwino nleroli,
Mulandirenso moyowu.

Zokondweretsa m’dzikomu
Nzosakhutitsa m’mtimamu,
Koma za Yesu zonsezo
Zikwaniritsa inudi.

Sakukanani Yesudi,
E, mukalapa m’mtimamo;
Lolani kuti Mzimuyo
Agwire ntchito zakezo.

Post navigation

Previous: Hymn 146 KODI ulikulemedwa
Next: Hymn 148 PAKUPEMPHA ife pano,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 183 Mlemekeze, bukitsani,
  • Hymn 933 M’mene imfa yathu idza,
  • Hymn 1836 Ndi wamwayi munthu uja
  • Hymn 1023 Kodi m’njiramo ndimvadi
  • Hymn 276 MKRISTU, ulimbike
  • Hymn 1413 Ndichitenji kukapeza
  • Hymn 53 Dalitsani mafumu athu,
  • Hymn 997 Mawu ake atipatsa
  • Hymn 69 KONDWERANI dzuŵa lino,
  • Hymn 302 NDIDZE pafupi pa
  • Hymn 1849 Nthawi zonse monga ‘Tate
  • Hymn 328 KULIBE vuto
  • Hymn 966 Kodi inu, aulendo,
  • Hymn 173 MWAMVA Mawu a Mulungu;
  • Hymn 400 ONA Mwana wa Nkhosa,
  • Hymn 661 Tamva aku Makedonyako atero,
  • Hymn 331 NDILI ndi kwathu ine,
  • Hymn 1610 Waleka koronayo,
  • Hymn 86 Mwandipatulira ine,
  • Hymn 313 Muthire, Yesu, m’mtimanga
  • Hymn 31 Tamandani mbuye,
  • Hymn 288 HAYA! ’nzanga taonani
  • Hymn 887 Pakupempherera
  • Hymn 1624 Koma anthu onse omwe
  • Hymn 461 ANA inu, myamikeni
  • Hymn 379 MTSINJE woyerawo
  • Hymn 1208 Kalelo! Kalelo!
  • Hymn 150 Ndisauka, sindiona;
  • Hymn 1468 Zobvala zake zonse
  • Hymn 719 Anu Mbuye ndifetu!
  • Hymn 726 Mundidzze ndi chikondi,
  • Hymn 1640 Alinkudza Ambuye Yesu
  • Hymn 711 Ife tonse tichenjere
  • Hymn 1686 Ndi mtima wonse mwimbedi
  • Hymn 297 POKUMANA m’mayesero a dziko lino,
  • Hymn 1729 Munthu Wazisoniyo
  • Hymn 456 ANA inu, ana inu,
  • Hymn 24 TITAME Mlungu Wakumwamba,
  • Hymn 1753 Adzatipulumutsa
  • Hymn 1547 Mtisangalatse m’zonse,
  • Hymn 1671 Akhululukira iwe,
  • Hymn 608 Maluwa abwino aphuka m’mapiri ndi m’madambomo,
  • Hymn 593 Yesu, munditsogoza
  • Hymn 105 Tiyamike Mbuye Yesu
  • Hymn 1049 Zoipa zangazi
  • Hymn 1702 Pakufa ine Mbuye
  • Hymn 113 Likalira llipengalo,
  • Hymn 360 KRISTU wakuyeratu,
  • Hymn 330 Yesu ndiye Mtsogoleri
  • Hymn 1318 Ndibwera kwa Ambuyeyo,
  • Hymn 876 Mtidzutse, Mbuyetu,
  • Hymn 3 Ndinu wakuyera!
  • Hymn 1690 Titama Yesuyo,
  • Hymn 119 M’BUKU la moyotu Mbuye,
  • Hymn 223 ATI Yesu Mbuyeyo:
  • Hymn 1456 Pakuti anthu akumvera
  • Hymn 1054 Ndilira mtima wakulapa
  • Hymn 1304 Ndi ine sizitheka ‘yi
  • Hymn 1616 Anafera
  • Hymn 39 Poyang’ana ena ndi ndalamatu,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version