Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 147 MUSAŴALOLE mawuwo

  1. Home   »  
  2. Hymn 147 MUSAŴALOLE mawuwo

Hymn 147 MUSAŴALOLE mawuwo

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 147 MUSAŴALOLE mawuwo

 

MUSAŴALOLE mawuwo
Apite ngati mphepozi,
Musaumitse mtimatu,
Polira Yesu Mbuyedi.

Idzanitu, idzanitu,
Idzani kwa Ambuyeyo.
Idzanitu, idzanitu
Apulumutse inunso.

Musachitenso nthantha ’yi,
Mufulumire inutu;
Tsiku labwino nleroli,
Mulandirenso moyowu.

Zokondweretsa m’dzikomu
Nzosakhutitsa m’mtimamu,
Koma za Yesu zonsezo
Zikwaniritsa inudi.

Sakukanani Yesudi,
E, mukalapa m’mtimamo;
Lolani kuti Mzimuyo
Agwire ntchito zakezo.

Post navigation

Previous: Hymn 146 KODI ulikulemedwa
Next: Hymn 148 PAKUPEMPHA ife pano,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 71 DZIKO lino lapansi, ndilibetu abwenzi,
  • Hymn 657 Ambuye, ndi chikondi tho!
  • Hymn 164 WANENA ndi Yesu,
  • Hymn 998 Anatilemba Yesu tikagwire nkhondo yake,
  • Hymn 860 Nthawi yina adzadzuka
  • Hymn 60 Chitetezo chachikulu
  • Hymn 952 Ndimayenda paulendo,
  • Hymn 156 OKOMA ndiwo mawu
  • Hymn 1216 Ndatsatatsatabe
  • Hymn 1117 Ndifuna Yesuyo
  • Hymn 1369 Paphiri paja papakulupo,
  • Hymn 1801 Nafuna kwaononga
  • Hymn 482 Ndinu wakuyera,
  • Hymn 1791 Tiimbe nyimbo zotamanda
  • Hymn 1600 E! dzina la Yesu,
  • Hymn 320 Ambuye, wakuti ndi mwaziwo
  • Hymn 1396 Ndi maso Ambuyathu
  • Hymn 748 Ndiye wa moyo wonse Mwiniyo,
  • Hymn 895 Ndikabwera ndi katundu
  • Hymn 707 Dalitseni, Mbuye, zonse
  • Hymn 1043 Mbiri yake ubukitse,
  • Hymn 198 M’dziko lino tikhalamo
  • Hymn 1212 Zina ndi zinanso
  • Hymn 1372 Zam’madzi zonse zakuopsyazo,
  • Hymn 451 MLUNGU alinane;
  • Hymn 455 TIIMBE ndi kulalikira
  • Hymn 726 Mundidzze ndi chikondi,
  • Hymn 1587 Nditama Mlungu m’mtimamo,
  • Hymn 773 Mtsinje woyerawo
  • Hymn 1527 Ndiye Mzimu Wakuyera
  • Hymn 1238 M’mene ndifa inedi,
  • Hymn 344 M’watame,
  • Hymn 129 WODALA ndiye munthuyo,
  • Hymn 1440 Yesu alindira,
  • Hymn 1769 Ndiye amachitira
  • Hymn 1758 Poti Mulungu wathu
  • Hymn 1521 Poyensedwa ife
  • Hymn 1697 Onani m’mutu, m’manjanso
  • Hymn 700 Mzimu woonadi
  • Hymn 1230 Lichiza mzimu wophwetekwa ukakhale bata,
  • Hymn 766 Monga zomera zonsezo
  • Hymn 210 Nyumba yodyera ilikudzaza;
  • Hymn 288 HAYA! ’nzanga taonani
  • Hymn 1742 Yesu ndinu moyo wathu,
  • Hymn 1000 Amatininkha zida zoteteza mtima, ndizo:
  • Hymn 350 Yesu ati,
  • Hymn 119 M’BUKU la moyotu Mbuye,
  • Hymn 1243 Kodi mayi wobereka
  • Hymn 146 Inu ndidzatama
  • Hymn 917 Ndi nkhondo ikaleka
  • Hymn 1141 Pakulekana ifetu
  • Hymn 553 M’munda muja ndaniyo
  • Hymn 1777 Mulungu wamkulu
  • Hymn 1265 Tere moyo wanga wonse,
  • Hymn 1662 Msandipitire, Yesu,
  • Hymn 1586 Mbuye Yesu timtamanda
  • Hymn 864 Ndi chikondi mtithandize kuigwira nkhondoyi;
  • Hymn 1809 Yampatsa Nowa yemwe,
  • Hymn 252 MTIMA wa Mbuyako,
  • Hymn 879 Zokoma etu nthawizi”

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version