Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 147 MUSAŴALOLE mawuwo

  1. Home   »  
  2. Hymn 147 MUSAŴALOLE mawuwo

Hymn 147 MUSAŴALOLE mawuwo

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 147 MUSAŴALOLE mawuwo

 

MUSAŴALOLE mawuwo
Apite ngati mphepozi,
Musaumitse mtimatu,
Polira Yesu Mbuyedi.

Idzanitu, idzanitu,
Idzani kwa Ambuyeyo.
Idzanitu, idzanitu
Apulumutse inunso.

Musachitenso nthantha ’yi,
Mufulumire inutu;
Tsiku labwino nleroli,
Mulandirenso moyowu.

Zokondweretsa m’dzikomu
Nzosakhutitsa m’mtimamu,
Koma za Yesu zonsezo
Zikwaniritsa inudi.

Sakukanani Yesudi,
E, mukalapa m’mtimamo;
Lolani kuti Mzimuyo
Agwire ntchito zakezo.

Post navigation

Previous: Hymn 146 KODI ulikulemedwa
Next: Hymn 148 PAKUPEMPHA ife pano,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1447 Yesu ngwachifundodi,
  • Hymn 338 Imvani
  • Hymn 100 MUBWERE Mzimu Wakuyera,
  • Hymn 877 Zokoma ndithu nthawizi
  • Hymn 1328 Ndani afuna kunkako
  • Hymn 1767 Ndiye anayang’ana
  • Hymn 352 Tiyamike Mlunguyo,
  • Hymn 755 Pamene padzakhalapo
  • Hymn 236 NDIDZIWITSITSA
  • Hymn 737 Mommuno, Mbuye, tionanetu,
  • Hymn 300 Ona Mwanawankhosayo
  • Hymn 354 Tinafunafunatu,
  • Hymn 658 Ndichitireni, Mbuye ‘ne,
  • Hymn 676 Adze amitundu yonse,
  • Hymn 184 LEKANI kubvutika ndi zinthu za padziko,
  • Hymn 60 ZATHEDWA zonsetu
  • Hymn 1184 Akondwerera nthawiyi
  • Hymn 296 TIYENI Akhristu,
  • Hymn 253 Adzakhala pampandopo
  • Hymn 1559 Wotsogolera, munditsogolere
  • Hymn 1390 Nditamatu Ambuyangayu,
  • Hymn 470 YESU andikonda ine,
  • Hymn 113 Likalira llipengalo,
  • Hymn 340 Imvani,
  • Hymn 1127 Mbuyanga Yesu, mundigwire dzanja;
  • Hymn 1610 Waleka koronayo,
  • Hymn 872 Mtidzutse, Mbuyetu,
  • Hymn 216 Ndi misozi ndi chisoni
  • Hymn 1348 Akupeza, akupeza,
  • Hymn 1675 Lambira Mfumuyo
  • Hymn 195 YESU wondikondadi,
  • Hymn 68 Kwathu ndidzaimba nyimbo
  • Hymn 1690 Titama Yesuyo,
  • Hymn 1032 Ntchito za Yesu gwira
  • Hymn 1029 Nkhawa tilibe; Yesuyo
  • Hymn 231 AMBUYE, m’imfamo
  • Hymn 1341 Tadza kukudyaku,
  • Hymn 186 MVERANI mbiri yozizwitsa
  • Hymn 1034 Mkristu, ulimbike
  • Hymn 847 Konse kuli mdima bii
  • Hymn 1089 Ndionetsere kuunika
  • Hymn 273 Mlungu akuyang’aniredi
  • Hymn 1798 Mukondwe anthu a Mulungu,
  • Hymn 346 Aitana,
  • Hymn 903 Iwo salekana, iwo salekana,
  • Hymn 1054 Ndilira mtima wakulapa
  • Hymn 491 N’takafika kwanu
  • Hymn 1486 M’dziko lino pansi pano
  • Hymn 1664 Ndigwadira Inu, Yesu,
  • Hymn 1599 Inde, ndifuna kumvatu
  • Hymn 348 CHIKHULUPIRIRO chathu
  • Hymn 320 Ambuye, wakuti ndi mwaziwo
  • Hymn 190 CHITETEZO chachikulu
  • Hello world!
  • Hymn 9 Mpingo woyera wa kwa anthuonse
  • Hymn 1758 Poti Mulungu wathu
  • Hymn 817 Tibvomereze,
  • Hymn 229 POYAMBAPO ndakondwadi.
  • Hymn 1282 Ndilinkudza kwa Ambuye,
  • Hymn 1542 Titamire nthawi zonse

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version