Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 409 ANTHU akum’maŵa

  1. Home   »  
  2. Hymn 409 ANTHU akum’maŵa

Hymn 409 ANTHU akum’maŵa

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 409 ANTHU akum’maŵa

 

ANTHU akum’maŵa
Nanka msangako,
Nzeru ’nali nazo,
Nafatsansowo;
Nanka kuli Mwana
Anabadwayo;
Anatsogozedwa
Ndi nyenyeziyo.

Anapeza Mwana
Ali m’kholamo,
Nagwadira Iwo
Mbuye wawoyo;
Anthu onse omwe
Ali pansipa,
Azitsata Mbuye
Ndi nyenyeziyo.

Mu ulemerero,
Yesu m’Mwambamo
Muli eni ake;
Anthu onsewo
Osadziŵa konse,
Akutalinso,
Akokedwe iwo
Ndi nyenyeziyo.

Akukhala kunja,
Osokeranso,
M’ŵaŵalire Mbuye,
Asagone’wo;
Amumdima omwe,
Olemedwanso,
Mtsogoleri wawo
Ndi nyenyeziyo.

Paulendo wathu
Tili pansipa,
Muŵalire tonse
Tili m’njiramo;
Mutitsogolere
Anthu tonsefe,
Mutifitse tonse
Ndi nyenyeziyo.

Post navigation

Previous: Hymn 408 ABALE nonse mulindiranji?
Next: Hymn 410 MAWU akewo anamveka ponse,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 424 MTIDZUTSE, Mbuyetu,
  • Hymn 1332 Imba kawiri ndi kawirinso,
  • Hymn 215 TATE ndili mwana wanu,
  • Hymn 1305 Ndi ine pondibvutapo
  • Hymn 73 M’SANDIPITILIRE Yesu,
  • Hymn 943 Onse aliko takonda kalelo,
  • Hymn 1484 Idzatu, idzatu
  • Hymn 397 MBUYE wathu, mutipatsa
  • Hymn 194 AMBUYE’naitan’ne;
  • Hymn 495 MLUNGU dalitsani Malaŵi,
  • Hymn 847 Konse kuli mdima bii
  • Hymn 456 Tizikondana, tisekere
  • Hymn 434 CHIKONDI cha Mulunguyo,
  • Hymn 1225 Ndinachita mphulupulu,
  • Hymn 25 ANGELO amayimba,
  • Hymn 595 Mbuye, ndinu wamphamvu,
  • Hymn 159 YESU ndi wokonda,
  • Hymn 287 Mitima yathu iyi nayo njanu,
  • Hymn 1635 Pakwitana Mbuye wanga,
  • Hymn 1526 Mbuye wondipulumutsa
  • Hymn 105 IDZANI, Mzimu Inu,
  • Hymn 1027 Tithawiranji ifetu?
  • Hymn 175 A! MBUSA wathu amvatu
  • Hymn 1058 Chimwemwe chija chamumtima
  • Hymn 1805 Anafa m’mvula muja
  • Hymn 332 Perekani mtima wanu,
  • Hymn 131 MAWU a Mulungu awa,
  • Hymn 430 MLUNGU akuyang’aniredí,
  • Hymn 438 Yesu ndiye Mbusa
  • Hymn 438 TIYAMIKE Ambuye,
  • Hymn 1767 Ndiye anayang’ana
  • Hymn 133 Yesu watidzera, watidzera,
  • Hymn 230 AMBUYANGA Yesu,
  • Hymn 330 Yesu ndiye Mtsogoleri
  • Hymn 816 Mdima wafika,
  • Hymn 1596 Anamnyoza pansi pano,
  • Hymn 368 MULUNGU wanga, Dzuŵatu
  • Hymn 961 Mbuye anatiitana
  • Hymn 522 Akazi anadza
  • Hymn 1178 Mawu omwewo, nyimbo yomweyi,
  • Hymn 182 YESU watidzera, watidzera,
  • Hymn 958 Ndikalowa m’mtsinje muja,
  • Hymn 1438 Yesu akukonda,
  • Hymn 1049 Zoipa zangazi
  • Hymn 1786 Ndikonda Mlungu pomva Mbuye wanga
  • Hymn 61 A! MUTU wakuyera,
  • Hymn 405 POLENGA dzikoli
  • Hymn 906 Mulibe zoipa m’Dzikolo,
  • Hymn 1810 Kalelo Mbuye Yesu
  • Hymn 221 Yesu and’itana,
  • Hymn 495 Wonga Inu ndikhaledi,
  • Hymn 3 TIMYAMIKIRE Mlunguyo,
  • Hymn 1809 Yampatsa Nowa yemwe,
  • Hymn 1297 Kumwamba komwe n’dzaimbira
  • Hymn 74 IDZA wolema,
  • Hymn 1609 Idzani nose’nu
  • Hymn 565 Koma sitimpenya m’khola
  • Hymn 1176 Sandinyenga, salephera;
  • Hymn 385 Tsopano, poyamba paja,
  • Hymn 255 Pakuona imfayo

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version