Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 409 ANTHU akum’maŵa

  1. Home   »  
  2. Hymn 409 ANTHU akum’maŵa

Hymn 409 ANTHU akum’maŵa

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 409 ANTHU akum’maŵa

 

ANTHU akum’maŵa
Nanka msangako,
Nzeru ’nali nazo,
Nafatsansowo;
Nanka kuli Mwana
Anabadwayo;
Anatsogozedwa
Ndi nyenyeziyo.

Anapeza Mwana
Ali m’kholamo,
Nagwadira Iwo
Mbuye wawoyo;
Anthu onse omwe
Ali pansipa,
Azitsata Mbuye
Ndi nyenyeziyo.

Mu ulemerero,
Yesu m’Mwambamo
Muli eni ake;
Anthu onsewo
Osadziŵa konse,
Akutalinso,
Akokedwe iwo
Ndi nyenyeziyo.

Akukhala kunja,
Osokeranso,
M’ŵaŵalire Mbuye,
Asagone’wo;
Amumdima omwe,
Olemedwanso,
Mtsogoleri wawo
Ndi nyenyeziyo.

Paulendo wathu
Tili pansipa,
Muŵalire tonse
Tili m’njiramo;
Mutitsogolere
Anthu tonsefe,
Mutifitse tonse
Ndi nyenyeziyo.

Post navigation

Previous: Hymn 408 ABALE nonse mulindiranji?
Next: Hymn 410 MAWU akewo anamveka ponse,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1682 Atha masiku aja ansoni,
  • Hymn 1530 Mndilimbitse ndipirire
  • Hymn 1632 Ndi chiyembekezo ichi
  • Hymn 1382 E, chifundo chake chonse
  • Hymn 1478 Azizwa anthu ajawo,
  • Hymn 134 INU ansembe ngakhale mufunsa,
  • Hymn 1456 Pakuti anthu akumvera
  • Hymn 1099 Sindidziwatu zamawa,
  • Hymn 540 Amithenga akumwamba
  • Hymn 1798 Mukondwe anthu a Mulungu,
  • Hymn 884 Mndikumbutse zomwe
  • Hymn 130 PHWANDO la Belisazara,
  • Hymn 1717 Mtima wangawe, uyenera
  • Hymn 25 ANGELO amayimba,
  • Hymn 819 Lero tigone,
  • Hymn 572 Anadza nazo mphatso zake
  • Hymn 1081 Ndikabisala mwanu
  • Hymn 291 ULENDO wachikhrisitu ngosawutsa ndithu,
  • Hymn 785 Yehova adalitse ‘nu,
  • Hymn 814 Mutichiritse ifenso
  • Hymn 1837 Mbuye ndiye wachifundo,
  • Hymn 1565 Mufike monga ngati njiwa yamtenderewo,
  • Hymn 542 Kuli kaphiri m’talimo
  • Hymn 34 AMITHENGA a Mulungu,
  • Hymn 1124 Ndifuna Inu, Yesu,
  • Hymn 357 Yesu ndiye Mtetezi,
  • Hymn 414 Ana ake adzapuma
  • Hymn 1411 Yesu akuitanani
  • Hymn 460 KULI kaphiri m’talimo
  • Hymn 909 Ife tikondwera, ife tikondwera,
  • Hymn 628 E! chisomo chosaleka
  • Hymn 1692 Timwimbire zomtamanda, Aleluya
  • Hymn 715 Mwapatsa Mwana wanu, ndi
  • Hymn 1489 Idzanitu, idzanitu,
  • Hymn 552 Analira ndaniyo
  • Hymn 945 Tiyeni pamodzi,
  • Hymn 176 Mleke mdaniyo, mwimbe m’njiramo
  • Hymn 177 Tate, ndili mwana wanu,
  • Hymn 183 Mlemekeze, bukitsani,
  • Hymn 1546 Mubwere Mzimu Inu
  • Hymn 1082 Ndidzaonana nanu
  • Hymn 171 IWE tiye, iwe tiye,
  • Hymn 1434 Lero lino m’bale wanga,
  • Hymn 434 CHIKONDI cha Mulunguyo,
  • Hymn 150 MIPINGO iyo idzatu,
  • Hymn 201 NDILINKUDZA kwa Ambuye,
  • Hymn 1715 Kodi misozi itisowa,
  • Hymn 365 DZUŴA lapita,
  • Hymn 710 Nthano ya Hananiyayo
  • Hymn 24 TITAME Mlungu Wakumwamba,
  • Hymn 1517 Lindionetsera ‘ne,
  • Hymn 1613 A Mulungu
  • Hymn 317 UKATHA moyo wanga
  • Hymn 1093 Odala ndi onsewo
  • Hymn 380 ATATE, muwapenya
  • Hymn 1272 Muyambe ntchito yanuyi,
  • Hymn 506 Ndikondwa kuti Yesu akonda,
  • Hymn 408 ABALE nonse mulindiranji?
  • Hymn 864 Ndi chikondi mtithandize kuigwira nkhondoyi;
  • Hymn 383 KASUPE ali wodzaza

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version