Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 291 ULENDO wachikhrisitu ngosawutsa ndithu,

  1. Home   »  
  2. Hymn 291 ULENDO wachikhrisitu ngosawutsa ndithu,

Hymn 291 ULENDO wachikhrisitu ngosawutsa ndithu,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 291 ULENDO wachikhrisitu ngosawutsa ndithu,

 

ULENDO wachikhrisitu ngosawutsa ndithu,
Mavuto, mayesero adza kwa ine;
Komatu ndidziŵitsitsa kuti Mbuye wanga,
Asunga moyo wanga kosalekeza.

Ndine wanu Mbuye wanga,
Mavuto, mayesero adza kwa ine;
Komatu ndidziwitsitsa
Kuti Mbuye wanga,
Asunga moyo wanga kosalekeza.

Chifukwa cha dzina lake
Ndanyozedwa ‘ne,
Adani achuluka, ndachepa ine;
Ndiwakonda onse
Koma andisautsa ‘ne,
Pukutani m’maso mwanga misoziyi.

Tiyeni abale tonse
Tilimbe ndithu,
Pogwira ntchito zake
Za Mbuye wathu;
Iye analonjezatu
Tsiku lomaliza,
Tidzakhala muulemelero wake.

Post navigation

Previous: Hymn 290 NAMONDWE wawuka,
Next: Hymn 292 NDIPULUMUTSENI Mbuye,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 653 Nditsogolere m’njirayi
  • Hymn 133 NSEMBE yake ya Kaini,
  • Hymn 1609 Idzani nose’nu
  • Hymn 1100 Inde wakukonda ndinu;
  • Hymn 50 Akhristu nyamulani
  • Hymn 701 Inu Atatuwo,
  • Hymn 244 Ndidze pafupi pa
  • Hymn 171 M’manda munalibe
  • Hymn 127 Mwazi wake ndi chitsime changa,
  • Hymn 330 Yesu ndiye Mtsogoleri
  • Hymn 990 Poyesedwa ine
  • Hymn 202 Timpemphere kutipatsa
  • Hymn 311 VALANI zida tizinka kwathuko,
  • Hymn 400 ONA Mwana wa Nkhosa,
  • Hymn 685 Tamva mawu amwewo
  • Hymn 381 MONGA zomera zonsezo
  • Hymn 409 Yesu adza kuwerenga
  • Hymn 299 TIYENI, Akristu inu,
  • Hymn 1721 Mapazi ake namvatu
  • Hymn 1621 Yang’anani anthu onse,
  • Hymn 23 TIIMBE nyimbo zotamanda
  • Hymn 211 TIDZALAKALAKA kuwonana naye,
  • Hymn 335 KWATHU sipadziko, ndingopitilira,
  • Hymn 1576 Khamulo liliko
  • Hymn 318 TINALI ambiri ife,
  • Hymn 1163 Tili ndi mtendere
  • Hymn 811 Wopulumutsa mudzetu;
  • Hymn 118 PANALI munthu amene,
  • Hymn 388 MOMMUNO, Mbuye tionanetu,
  • Hymn 123 Koma mudzisungire chuma cha Kumwamba
  • Hymn 107 Panalibe mwa abale
  • Hymn 669 Anyamata limikani,
  • Hymn 708 Peturo ‘nafusa Hananiya:
  • Hymn 344 ’TATE, ’Nu.
  • Hymn 1040 Ukafuna kulemera,
  • Hymn 900 Mutipatse leroli
  • Hymn 751 Mongatu mawu anuwo,
  • Hymn 77 MMENE Yesu adzabwera,
  • Hymn 1780 Titame Mlungu Wakumwamba,
  • Hymn 81 Imva mawu akewo,
  • Hymn 966 Kodi inu, aulendo,
  • Hymn 365 DZUŴA lapita,
  • Hymn 349 Aitana,
  • Hymn 1231 Nlokoma dzinalo la Yesu, ndilo thanthwe langa,
  • Hymn 431 AKAPANDA kumanga,
  • Hymn 675 Pamaiko pali mdima,
  • Hymn 1225 Ndinachita mphulupulu,
  • Hymn 1332 Imba kawiri ndi kawirinso,
  • Hymn 155 Pemphero ndiko kufuna
  • Hymn 366 Anthu onse a padziko
  • Hymn 6 Nanu akukuzani amithenga,
  • Hymn 276 MKRISTU, ulimbike
  • Hymn 1585 Dzina ili ndi lokoma
  • Hymn 513 Atipempherera
  • Hymn 837 Koma kalelo mnakhalitsa pano,
  • Hymn 1358 Lemekeza Mfumu yathu,
  • Hymn 894 Mbuye, ndinu Mfumu yanga
  • Hymn 479 ANYAMATA inutu,
  • Hymn 258 MWA ine, moyo wanga ndi Yesu
  • Hymn 1731 Ife tinachimwadi,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version