Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 291 ULENDO wachikhrisitu ngosawutsa ndithu,

  1. Home   »  
  2. Hymn 291 ULENDO wachikhrisitu ngosawutsa ndithu,

Hymn 291 ULENDO wachikhrisitu ngosawutsa ndithu,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 291 ULENDO wachikhrisitu ngosawutsa ndithu,

 

ULENDO wachikhrisitu ngosawutsa ndithu,
Mavuto, mayesero adza kwa ine;
Komatu ndidziŵitsitsa kuti Mbuye wanga,
Asunga moyo wanga kosalekeza.

Ndine wanu Mbuye wanga,
Mavuto, mayesero adza kwa ine;
Komatu ndidziwitsitsa
Kuti Mbuye wanga,
Asunga moyo wanga kosalekeza.

Chifukwa cha dzina lake
Ndanyozedwa ‘ne,
Adani achuluka, ndachepa ine;
Ndiwakonda onse
Koma andisautsa ‘ne,
Pukutani m’maso mwanga misoziyi.

Tiyeni abale tonse
Tilimbe ndithu,
Pogwira ntchito zake
Za Mbuye wathu;
Iye analonjezatu
Tsiku lomaliza,
Tidzakhala muulemelero wake.

Post navigation

Previous: Hymn 290 NAMONDWE wawuka,
Next: Hymn 292 NDIPULUMUTSENI Mbuye,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 99 Tsopano ndimwona Iye
  • Hymn 330 Yesu ndiye Mtsogoleri
  • Hymn 150 MIPINGO iyo idzatu,
  • Hymn 1799 Mulungu atipatsa mphamvu
  • Hymn 1306 Ndi ine ndasaukadi,
  • Hymn 1466 Ambuye wathu Yesu
  • Hymn 431 Pompano pandikonda
  • Hymn 148 PAKUPEMPHA ife pano,
  • Hymn 1100 Inde wakukonda ndinu;
  • Hymn 1846 Mtima wanga uyamike
  • Hymn 1779 M’dzikomo Ambuye
  • Hymn 469 Lero mkhale nafe ndithu,
  • Hymn 584 Ndi angelo,
  • Hymn 1204 Ambuyanga Yesu,
  • Hymn 408 ABALE nonse mulindiranji?
  • Hymn 476 Mpaka ndabvala mbuu!
  • Hymn 1235 Yesu wathadi
  • Hymn 1651 Kwa Mulungu m’Mwambamo
  • Hymn 560 Kale m’mzinda wachifumu
  • Hymn 1083 “Khala mwa Ine,” Yesu anatero;
  • Hymn 1397 Okwawa pansi inu,
  • Hymn 1436 Inde, lero lino Yesu
  • Hymn 1614 Anabadwa,
  • Hymn 972 Akristu limbikani,
  • Hymn 1272 Muyambe ntchito yanuyi,
  • Hymn 1379 Mulungu yemweyo
  • Hymn 161 LERO lino mbale wanga,
  • Hymn 604 ‘Tate, Mwana, Mzimu, ndinu
  • Hymn 1501 Inde, pakufa panga
  • Hymn 190 CHITETEZO chachikulu
  • Hymn 1820 Kwezani nane Ambuyathu,
  • Hymn 485 POMPANO pandikonda
  • Hymn 1054 Ndilira mtima wakulapa
  • Hymn 79 Mlendo ali pakhomo,
  • Hymn 358 Dzina lake Yesuyo,
  • Hymn 1091 Mulamulire mtima, Yesu,
  • Hymn 743 Mudze, anthuni, talawani ‘nu
  • Hymn 1463 Zoipa zakhululukidwa,
  • Hymn 1577 “Kwa Iye atikonda
  • Hymn 1595 Ndani mwa abale athu
  • Hymn 5 Inu Mulungu, tikuyamikani;
  • Hymn 1516 Pakudera nkhawa ‘ne,
  • Hymn 840 Ambuye munapatsa tsiku
  • Hymn 383 Zokoma ndi zakuyanja
  • Hymn 181 Zonse ndinakonda kale
  • Hymn 53 Dalitsani mafumu athu,
  • Hymn 1063 Pokhala mtendere mu mtimangamu,
  • Hymn 1775 Oonadi mtima,
  • Hymn 120 MUNDINYEMERE ’ne
  • Hymn 1814 Thupi lamwazi wathu’li
  • Hymn 208 CHITHA n’chiyani kund’yeretsa?
  • Hymn 1502 Kodi ulikulemedwa
  • Hymn 344 ’TATE, ’Nu.
  • Hymn 300 Ona Mwanawankhosayo
  • Hymn 1079 Khalatu woyera,
  • Hymn 1196 E! chikondi ndithu,
  • Hymn 1726 Linadetsedwa dzuwa bii!
  • Hymn 957 Mundimwetse madzi anu,
  • Hymn 1677 Zomkweza zili m’Mwamba,Aleluya
  • Hymn 33 OWONADI mtima,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version