Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 431 AKAPANDA kumanga,

  1. Home   »  
  2. Hymn 431 AKAPANDA kumanga,

Hymn 431 AKAPANDA kumanga,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 431 AKAPANDA kumanga,

 

AKAPANDA kumanga,
Nyumba Yehovayo;
Woyimanga nyumbayo,
Angomanga chabe.

Gwirani ntchito yake,
Ndi mapemphero;
Kuti Yehova adalitse,
Ntchito yanu.

Ngati mugwira ntchito,
Ndi nzeru zanuzo;
Mulibe phindu ndithu,
Pamaso pa Mbuye.

Tipempha ‘Nu Yehova,
M’dalitsetu ntchito;
Zathu kuti Ufumu,
Wanu Ukwezedwe.

Post navigation

Previous: Hymn 430 MLUNGU akuyang’aniredí,
Next: Hymn 432 KRISTU ndiye Mwala wathu,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1108 Khala chete mtima wanga,
  • Hymn 1232 Ambuye ndinu Mbusa, Bwenzi, ndi Wansembe wanga,
  • Hymn 1697 Onani m’mutu, m’manjanso
  • Hymn 228 MWAKHULUPIRIRADI
  • Hymn 399 M’KHOLA mwa ng’ombe ku Betlehemu
  • Hymn 850 Pemphero, pemphero,
  • Hymn 137 UTHENGA wa Ambuye
  • Hymn 1712 E! Yesu Mbuye wangadi,
  • Hymn 1631 Mudzabwera, mudzabwera;
  • Hymn 1743 M’kati mwa zobvuta zathu
  • Hymn 96 Kodi mudzampembedza Mbuye
  • Hymn 1090 Chitsime chakuyera ine
  • Hymn 792 Dzuwa la Mulungu
  • Hymn 216 Ndi misozi ndi chisoni
  • Hymn 871 Tiphatikane tonsefe okonda Yesu Kristu;
  • Hymn 88 Yesu, dzina lakukonda,
  • Hymn 339 Tipempha,
  • Hymn 1343 M’dzina la Yesuyo
  • Hymn 147 Ndisauka, ndinachimwa,
  • Hymn 923 Dothili kudothilo,
  • Hymn 266 MBUYE ndamva mwawazira
  • Hymn 68 M’MANDA, nagonamo
  • Hymn 486 MPULUMUTSI Yesu,
  • Hymn 219 YESU Mbuyetu, mwafera
  • Hymn 408 Oipa tili tonsefe;
  • Hymn 1718 Ona chikondi cha Mulungu,
  • Hymn 276 MKRISTU, ulimbike
  • Hymn 1794 Mulungu awakonda anthu
  • Hymn 994 Limba mtima mbale wanga,
  • Hymn 106 Ife, tapulumukadi,
  • Hymn 856 Kuunika kuoneka
  • Hymn 1250 Mndilandire ine Mbuye
  • Hymn 109 MUTHIRE, Yesu, m’mtimanga
  • Hymn 20 CHIKONDI cha Mulungu wathu,
  • Hymn 790 Zimbalame zonsezi
  • Hymn 1638 Alinkudza wansoni Munthu
  • Hymn 167 Yendanitu, Wansembe wathu,
  • Hymn 103 Bwenzi lathu ndinutu,
  • Hymn 360 Muli ndi ludzu, idzani
  • Hymn 1399 Yesu ponong’oneza, idzanitu;
  • Hymn 400 Dzuwa liwala, m’tulotu
  • Hymn 1030 Tioperanji ifetu?
  • Hymn 106 MZIMU Woyera, mudzetu,
  • Hymn 269 NDILIRA ine kukayenda
  • Hymn 762 “Ndi thupi lopatsidwali
  • Hymn 1181 Adalitsika munthuyo
  • Hymn 473 Mzinda woyerawo!
  • Hymn 563 Ndipo Mwana uyu Yesu
  • Hymn 731 Mundionetse, Yesu,
  • Hymn 1811 Tipulumuka mommo,
  • Hymn 1386 Ndi chifundo atipenya
  • Hymn 94 Ndani anatiwombola?
  • Hymn 1810 Kalelo Mbuye Yesu
  • Hymn 336 KULINSO dziko lowala M’mwamba,
  • Hymn 1423 Oipa inu nonsetu,
  • Hymn 1652 Mabala ajawo
  • Hymn 952 Ndimayenda paulendo,
  • Hymn 47 Anthu m’maiko onse
  • Hymn 285 DZIKO lino lapansi,
  • Hymn 457 Palibe mwana wakuchepa

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version