Site icon Treasure Hymns – Chichewa

Hymn 431 AKAPANDA kumanga,

Chichewa Christian Hymns

Hymn 431 AKAPANDA kumanga,

 

AKAPANDA kumanga,
Nyumba Yehovayo;
Woyimanga nyumbayo,
Angomanga chabe.

Gwirani ntchito yake,
Ndi mapemphero;
Kuti Yehova adalitse,
Ntchito yanu.

Ngati mugwira ntchito,
Ndi nzeru zanuzo;
Mulibe phindu ndithu,
Pamaso pa Mbuye.

Tipempha ‘Nu Yehova,
M’dalitsetu ntchito;
Zathu kuti Ufumu,
Wanu Ukwezedwe.

Exit mobile version