Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 431 AKAPANDA kumanga,

  1. Home   »  
  2. Hymn 431 AKAPANDA kumanga,

Hymn 431 AKAPANDA kumanga,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 431 AKAPANDA kumanga,

 

AKAPANDA kumanga,
Nyumba Yehovayo;
Woyimanga nyumbayo,
Angomanga chabe.

Gwirani ntchito yake,
Ndi mapemphero;
Kuti Yehova adalitse,
Ntchito yanu.

Ngati mugwira ntchito,
Ndi nzeru zanuzo;
Mulibe phindu ndithu,
Pamaso pa Mbuye.

Tipempha ‘Nu Yehova,
M’dalitsetu ntchito;
Zathu kuti Ufumu,
Wanu Ukwezedwe.

Post navigation

Previous: Hymn 430 MLUNGU akuyang’aniredí,
Next: Hymn 432 KRISTU ndiye Mwala wathu,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1856 Mzimu, msandipitirire,
  • Hymn 1507 Ndikampempha anditenge,
  • Hymn 878 Zokoma inde nthawizi
  • Hymn 210 PEREKANI mtima wanu,
  • Hymn 1072 Mudzaze Yesu mtima wanga ndi chikondicho,
  • Hymn 239 Akumwambawo
  • Hymn 1167 Mulungu wanga,
  • Hymn 1023 Kodi m’njiramo ndimvadi
  • Hymn 6 LEMEKEZA Mulungu ’Tate,
  • Hymn 13 Mtiwerengere m’Mwamba ndi oyera;
  • Hymn 980 Tiyeni ku nkhondo iyi,
  • Hymn 408 ABALE nonse mulindiranji?
  • Hymn 1590 Mtima ndimakondweramo,
  • Hymn 589 Koma ineyu
  • Hymn 761 Natamndira Mlunguyo
  • Hymn 483 Ndife akuchoka,
  • Hymn 1395 Mulungu ali nane!
  • Hymn 1468 Zobvala zake zonse
  • Hymn 712 Mulungu akondadi leroli
  • Hymn 60 ZATHEDWA zonsetu
  • Hymn 1583 Dzina la Yesuyo
  • Hymn 273 Mlungu akuyang’aniredi
  • Hymn 418 UDINDO wolalikira Uthenga,
  • Hymn 1442 Khulupira mawu onse
  • Hymn 546 Kulibe wokwanira ‘yi
  • Hymn 115 Mbulu wanding’amba m’nthiti,
  • Hymn 1847 Ife tonse, ife tonse,
  • Hymn 772 Muwalimbikitse onse
  • Hymn 1041 Zosauka unvomere,
  • Hymn 1792 Mulungu ndiye wachifundo,
  • Hymn 1780 Titame Mlungu Wakumwamba,
  • Hymn 441 Tamverani, aitana:
  • Hymn 267 AMBUYE, thandizenitu
  • Hymn 396 PETURO ’nafunsa Hananiya:
  • Hymn 432 KRISTU ndiye Mwala wathu,
  • Hymn 237 SINDINANYENGEDWA konse
  • Hymn 310 MBUYE munditsogolere,
  • Hymn 80 KUDZA kwa Mbuye
  • Hymn 1130 Mbuyanga Yesu, mundigwire dzanja
  • Hymn 1074 Mubweretu nomwe ‘Nu munatsika kalelo;
  • Hymn 294 POYESEDWA ine
  • Hymn 490 YESU adza kuwerenga,
  • Hymn 332 Perekani mtima wanu,
  • Hymn 720 Anu Mbuye ndifetu!
  • Hymn 61 Ndi chimwemwe ndimaona
  • Hymn 1329 M’tali mutali m’phirimo
  • Hymn 868 Atate yemwe anatuma Mpulumutsi mmodzi
  • Hymn 433 MULUNGU wa Kumwamba bwera kunoku
  • Hymn 1578 Onsewa ‘nachimwa
  • Hymn 290 Ndi miyendo yathu iyinso njanu,
  • Hymn 216 NDISAUKA, ndinachimwa,
  • Hymn 124 Aliponso adani am’kati ndi akunja;
  • Hymn 537 Aleluya! Aleluya!
  • Hymn 548 Kale anthu m’kholamo
  • Hymn 1048 Kumwamba ndiona Ambuyangayo,
  • Hymn 143 KONZA mtima iwe mbale,
  • Hymn 257 Ndinasiya amayi,
  • Hymn 299 TIYENI, Akristu inu,
  • Hymn 1047 Ambuye, chotsani zonse zomwezo
  • Hymn 65 NLA Mlungu dzuŵali:

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version