Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 433 MULUNGU wa Kumwamba bwera kunoku

  1. Home   »  
  2. Hymn 433 MULUNGU wa Kumwamba bwera kunoku

Hymn 433 MULUNGU wa Kumwamba bwera kunoku

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 433 MULUNGU wa Kumwamba bwera kunoku

 

MULUNGU wa Kumwamba bwera kunoku
Ndi mtima wokondwera kuloŵa m’nyumbayi;
Chifukwa cha zabwino mwatichitirazi
Tikukuyamikirani leroli.

Inde, tikuyamikani, Atate, leroli,
Mwatimangira ’fe kuno kachisi wanuyu!
Ndi ulemerero wanu mudzaze m’nyumbayi;
Muyeretse, mudalitse munomu.

Tikondwa tonse ndikukuthokozani ’Nu
Poyamba kupemphera ndikuimbira ’mu;
Mommuno nsiku zonse mukhale nafetu,
Monga ndi angelo anu m’Mwambamo.

Ikhale ngati nyali yoŵala nyumbayi,
Yakutsogoza onse ophunthwa m’mdima bii;
Akunja ndi Akristu m’ŵapulumutse ndi
Kuunika kotuluka munomu.

Post navigation

Previous: Hymn 432 KRISTU ndiye Mwala wathu,
Next: Hymn 434 CHIKONDI cha Mulunguyo,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1029 Nkhawa tilibe; Yesuyo
  • Hymn 955 Komwe ndi chimwemwe ine
  • Hymn 1266 E, chimwemwe chachikulu, N’taperekadi
  • Hymn 599 Mlengi wathu Wakuyera,
  • Hymn 361 AMBUYE munapatsa tsiku
  • Hymn 1493 Mbiri yakalelomwe
  • Hymn 187 Kondwani nonsenu,
  • Hymn 1824 Mulungu wathu Mmodzi yekha
  • Hymn 1551 Mukhale m’kati mwathu,
  • Hymn 1856 Mzimu, msandipitirire,
  • Hymn 1697 Onani m’mutu, m’manjanso
  • Hymn 1649 Kutenga inetu, kutenga inetu
  • Hymn 271 Zoipa zangazi
  • Hymn 12 NDITAMATU Ambuyangayu,
  • Hymn 1172 Adzabweranso
  • Hymn 567 M’nyumba zonse ponseponse
  • Hymn 293 Tidziperekadi konse kwa Inu
  • Hymn 1072 Mudzaze Yesu mtima wanga ndi chikondicho,
  • Hymn 1711 Kwa munthu wasokerayo
  • Hymn 1206 Ndidzakukondani
  • Hymn 786 Yesu mkhale nafe
  • Hymn 1837 Mbuye ndiye wachifundo,
  • Hymn 270 NDILIRA mtima wotamanda
  • Hymn 172 Imfa yalephera
  • Hymn 652 Munene Mbuye ‘nenetu,
  • Hymn 1134 Pansi pano ndili mlendo,
  • Hymn 854 Timlemekeze Mlunguyu
  • Hymn 445 TILIMALIMA m’minda,
  • Hymn 61 Ndi chimwemwe ndimaona
  • Hymn 1336 Mwamva mawu a Mulungu;
  • Hymn 1744 Kale ophunzira ake
  • Hymn 650 Tikondwa tonse ndi kukuthokazani Nu
  • Hymn 827 Wonsewu usiku
  • Hymn 119 M’BUKU la moyotu Mbuye,
  • Hymn 972 Akristu limbikani,
  • Hymn 101 Lodala tsiku lomwelo
  • Hymn 1809 Yampatsa Nowa yemwe,
  • Hymn 1014 Tingolira kaya,
  • Hymn 105 Tiyamike Mbuye Yesu
  • Hymn 391 MUNDIMVERE, Mbuye wanga
  • Hymn 715 Mwapatsa Mwana wanu, ndi
  • Hymn 436 Yesu ndiye Mbusa,
  • Hymn 448 CHIFUKWA cha zokoma mtima zonse zaulelezo,
  • Hymn 102 MZIMU Woyera, mudzetu kwa ine
  • Hymn 1450 Ndi angelo akumwamba
  • Hymn 298 “Tadodoma, abusa,
  • Hymn 269 NDILIRA ine kukayenda
  • Hymn 943 Onse aliko takonda kalelo,
  • Hymn 466 Yesu, muli pa chimpando
  • Hymn 1608 Yesu, dzina lakukonda
  • Hymn 208 CHITHA n’chiyani kund’yeretsa?
  • Hymn 2 YEHOVA Mthandizi,
  • Hymn 11 NDI mitima yokondwera,
  • Hymn 1117 Ndifuna Yesuyo
  • Hymn 1242 Ku zoipa zonse zako,
  • Hymn 366 Anthu onse a padziko
  • Hymn 743 Mudze, anthuni, talawani ‘nu
  • Hymn 1141 Pakulekana ifetu
  • Hymn 1775 Oonadi mtima,
  • Hymn 190 CHITETEZO chachikulu

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version