Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 433 MULUNGU wa Kumwamba bwera kunoku

  1. Home   »  
  2. Hymn 433 MULUNGU wa Kumwamba bwera kunoku

Hymn 433 MULUNGU wa Kumwamba bwera kunoku

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 433 MULUNGU wa Kumwamba bwera kunoku

 

MULUNGU wa Kumwamba bwera kunoku
Ndi mtima wokondwera kuloŵa m’nyumbayi;
Chifukwa cha zabwino mwatichitirazi
Tikukuyamikirani leroli.

Inde, tikuyamikani, Atate, leroli,
Mwatimangira ’fe kuno kachisi wanuyu!
Ndi ulemerero wanu mudzaze m’nyumbayi;
Muyeretse, mudalitse munomu.

Tikondwa tonse ndikukuthokozani ’Nu
Poyamba kupemphera ndikuimbira ’mu;
Mommuno nsiku zonse mukhale nafetu,
Monga ndi angelo anu m’Mwambamo.

Ikhale ngati nyali yoŵala nyumbayi,
Yakutsogoza onse ophunthwa m’mdima bii;
Akunja ndi Akristu m’ŵapulumutse ndi
Kuunika kotuluka munomu.

Post navigation

Previous: Hymn 432 KRISTU ndiye Mwala wathu,
Next: Hymn 434 CHIKONDI cha Mulunguyo,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 511 Ntchito zake zatha,
  • Hymn 230 AMBUYANGA Yesu,
  • Hymn 705 Tikhaletu nawo, Mbuye,
  • Hymn 91 NDITAME Mlungu m’mtimamo,
  • Hymn 1261 Kale ndinakana Inu, Ndinathawatu;
  • Hymn 946 Ngakhale enawo aleke kwimbako,
  • Hymn 298 IFE tazingidwa ndi zinthu zoopsa,
  • Hymn 684 Zipata zatsegudwa mbee! Za m’dziko monsemo;
  • Hymn 1338 Munachita nthantha kale,
  • Hymn 991 Ndi zapansi pano
  • Hymn 809 Madzulo aja kalelo
  • Hymn 1118 Ndifuna Inu Yesu,
  • Hymn 964 Kodi simuona njira,
  • Hymn 609 Zanu zapansi nzokoma Mbuye; tikondwera ‘fe,
  • Hymn 1368 Mitambo inu yakumwambako,
  • Hymn 1068 Ambuye, thandizenitu
  • Hymn 1272 Muyambe ntchito yanuyi,
  • Hymn 265 MUDZAZE Yesu mtima wanga ndi chikondicho,
  • Hymn 1643 Kufuna inetu, kufuna inetu,
  • Hymn 754 Ndi mtanda uli m’maso mbuu,
  • Hymn 431 AKAPANDA kumanga,
  • Hymn 585 Alanditsa,
  • Hymn 873 Mtidzutse, Mbuyetu,
  • Hymn 961 Mbuye anatiitana
  • Hymn 1755 Choti timtumikire
  • Hymn 1060 Mubwere, Mzimu wa mpumulo
  • Hymn 302 Anasenza m’thupi mwake;
  • Hymn 905 Iwo asekera, iwo asekera,
  • Hymn 9 TAMANI Ambuye,
  • Hymn 444 YEMWE afesa nalira,
  • Hymn 393 Tilikuimba nyimbo yomweyi,
  • Hymn 1659 Ndiye mtsamiro
  • Hymn 842 Tipempha kuti Mpingo wanu
  • Hymn 679 Zipata zachitsulo zitseguke zonse mbee!
  • Hymn 365 DZUŴA lapita,
  • Hymn 1834 Chisomo ndi zokoma zake sizileka konse;
  • Hymn 416 PALIBE wina Kumwamba,
  • Hymn 1536 Ndilira Mzimu leroli,
  • Hymn 310 MBUYE munditsogolere,
  • Hymn 79 PAKWITANA Mbuye wanga
  • Hymn 1760 Amithenga a Mulungu
  • Hymn 145 MBIRI yakale lomwe
  • Hymn 498 AMBUYE, mtidalitsetu,
  • Hymn 116 MBUYE, Mawu anu
  • Hymn 80 Utsegule mtimawo,
  • Hymn 1772 Iye amakhutitsa
  • Hymn 375 YESU m’khale nafe
  • Hymn 852 Munkhani zako zonsetu
  • Hymn 10 TSOPANO linoli,
  • Hymn 325 Walira Yesu wolimbitsayo,
  • Hymn 833 Mundilimbitse ndikayese manda ngati mphasayi,
  • Hymn 583 Anabadwa,
  • Hymn 1557 M’phunzitsi, ndinu mudziwitse ine
  • Hymn 1099 Sindidziwatu zamawa,
  • Hymn 562 Mwa ubwana wake wonse
  • Hymn 805 Madzulo ano mkhaletu
  • Hymn 35 KODI mwaona chiyani,
  • Hymn 1604 Yesu, dzina lakukonda,
  • Hymn 498 Yesu akonda,
  • Hymn 173 Mema nkhondoyo, wadza mdaniyo,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version