Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 11 NDI mitima yokondwera,

  1. Home   »  
  2. Hymn 11 NDI mitima yokondwera,

Hymn 11 NDI mitima yokondwera,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 11 NDI mitima yokondwera,

 

NDI mitima yokondwera,
Mbuye wathu tiyamika.

E, chifundo chake chonse,
Ndi chosatha nthaŵi zonse.

Dzina lake tibukitsa,
Mlungu ndiye yekhayekha.

Mphamvu yake inalenga,
Dziko lonse ndi kumwamba.

Anatsogolera kale,
M’chipululu anthu ake.

Ndi chifundo atipenya,
Ife anthu osawuka.

Amaŵeta nyama zonse,
Zingasoŵe kanthu konse.

Tiimbire Mlungu wathu,
Waulemu ndi wamkulu.

Tithaŵire kwa Mulungu,
Ndiko tikapeze moyo.

Post navigation

Previous: Hymn 10 TSOPANO linoli,
Next: Hymn 12 NDITAMATU Ambuyangayu,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 681 Ankhondo a Mulungu ‘nu, yendani m’njiramo,
  • Hymn 45 Malawi dziko lokongola,
  • Hymn 107 Panalibe mwa abale
  • Hymn 462 ANANU, ziimbani,
  • Hymn 855 Aulendo amayenda
  • Hymn 2 Ndinu wakuyera!
  • Hymn 1404 “Undipatsetu
  • Hymn 1816 Anatikondakonda ‘Ye,
  • Hymn 839 Adani sindiopa mukalipo;
  • Hymn 106 Ife, tapulumukadi,
  • Hymn 476 MBUYE, tili ana anu,
  • Hymn 1096 Tifuna Inu, Mbuye,
  • Hymn 162 Angelo anu asunga
  • Hymn 244 Ndidze pafupi pa
  • Hymn 1226 Wandipatsa moyo wake,
  • Hymn 158 Mzimu, mlonge m’mtimamo
  • Hymn 105 Tiyamike Mbuye Yesu
  • Hymn 453 A! MULUNGU
  • Hymn 140 Panalitu wakudwala
  • Hymn 1011 M’mawa tizifesa
  • Hymn 58 Titasokera tinabwerera,
  • Hymn 994 Limba mtima mbale wanga,
  • Hymn 1507 Ndikampempha anditenge,
  • Hymn 1449 Pena imfa idza mawa,
  • Hymn 1461 Sing’anga ‘mkulu ndiye Yesu,
  • Hymn 1501 Inde, pakufa panga
  • Hymn 218 Mbuye Yesu ndi Atate,
  • Hymn 170 M’manda naukamo
  • Hymn 1423 Oipa inu nonsetu,
  • Hymn 136 Atumwi atummika, atumika,
  • Hymn 46 O! ufulu tigwirizane
  • Hymn 373 NYUMBA ya Mulungu, ili pano,
  • Hymn 1610 Waleka koronayo,
  • Hymn 974 Tsopano timenyana
  • Hymn 53 Dalitsani mafumu athu,
  • Hymn 16 Chikhulupiriro chathu
  • Hymn 1477 Anena anthu onsewo,
  • Hymn 694 Sadalekeza kuyamika
  • Hymn 1050 Ndafoka inetu,
  • Hymn 1081 Ndikabisala mwanu
  • Hymn 666 Walitsani nyali yanu
  • Hymn 903 Iwo salekana, iwo salekana,
  • Hymn 360 KRISTU wakuyeratu,
  • Hymn 164 Yendani, Mfumu yamtendere
  • Hymn 782 Aleluya, aleluya,
  • Hymn 72 Mayi watsogola ku Ulemerero,
  • Hymn 172 TADZA kukudyaku,
  • Hymn 1583 Dzina la Yesuyo
  • Hymn 1717 Mtima wangawe, uyenera
  • Hymn 457 KALE m’mzinda wachifumu
  • Hymn 989 Yochita ndi yodikha
  • Hymn 145 Kale ndinafuna
  • Hymn 1321 Thanthwe long’ambikatu,
  • Hymn 1490 Musachitenso nthantha ‘yi,
  • Hymn 52 Mbwere Mzimu, mbwere!
  • Hymn 364 Ali wokhululukira;
  • Hymn 650 Tikondwa tonse ndi kukuthokazani Nu
  • Hymn 1028 Yendani bwino m’njiramo
  • Hymn 752 Chakudya chakumwambachi
  • Hymn 1803 Nowayo nayendamo,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version