Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 11 NDI mitima yokondwera,

  1. Home   »  
  2. Hymn 11 NDI mitima yokondwera,

Hymn 11 NDI mitima yokondwera,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 11 NDI mitima yokondwera,

 

NDI mitima yokondwera,
Mbuye wathu tiyamika.

E, chifundo chake chonse,
Ndi chosatha nthaŵi zonse.

Dzina lake tibukitsa,
Mlungu ndiye yekhayekha.

Mphamvu yake inalenga,
Dziko lonse ndi kumwamba.

Anatsogolera kale,
M’chipululu anthu ake.

Ndi chifundo atipenya,
Ife anthu osawuka.

Amaŵeta nyama zonse,
Zingasoŵe kanthu konse.

Tiimbire Mlungu wathu,
Waulemu ndi wamkulu.

Tithaŵire kwa Mulungu,
Ndiko tikapeze moyo.

Post navigation

Previous: Hymn 10 TSOPANO linoli,
Next: Hymn 12 NDITAMATU Ambuyangayu,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1255 Chitha nchiani kund’yeretsa?
  • Hymn 1458 Satana ndi unyolo
  • Hymn 1600 E! dzina la Yesu,
  • Hymn 772 Muwalimbikitse onse
  • Hymn 625 Chaka chino mutipatse
  • Hymn 1120 Ndifuna Yesuyo
  • Hymn 300 AKRISTU limbikani,
  • Hymn 60 Chitetezo chachikulu
  • Hymn 1737 “Senzani mtanda wanuwu.”
  • Hymn 582 A! Mulungu,
  • Hymn 80 KUDZA kwa Mbuye
  • Hymn 1142 Tidzathawira kuti ‘fe
  • Hymn 1030 Tioperanji ifetu?
  • Hymn 719 Anu Mbuye ndifetu!
  • Hymn 884 Mndikumbutse zomwe
  • Hymn 436 YEHOVA Mlungu wathu,
  • Hymn 1574 Anthu ose ndi mitundu
  • Hymn 386 Tiyamike Mlunguyo,
  • Hymn 389 Ambuye, mtidalitsetu,
  • Hymn 254 Adzanena kwa anthuwo
  • Hymn 596 Mlungu ali nane;
  • Hymn 447 OYAMIKA Mlungu m’bwere,
  • Hymn 1435 Ndiwe mlendo lero lino,
  • Hymn 145 MBIRI yakale lomwe
  • Hymn 1270 Ndayesa kudzikonzadi,
  • Hymn 1352 Atate wa Kumwambako,
  • Hymn 794 Ambuye, tasonkhana
  • Hymn 323 Tiwaliretu, tiwaliretu
  • Hymn 276 Dziko lonse mlambire
  • Hymn 485 POMPANO pandikonda
  • Hymn 844 Pogona ife, amadzuka
  • Hymn 552 Analira ndaniyo
  • Hymn 1301 Moyo ukatha zi,
  • Hymn 174 YESU wathu Mbuyeyo
  • Hymn 1766 Ndilikulemekeza
  • Hymn 1048 Kumwamba ndiona Ambuyangayo,
  • Hymn 71 DZIKO lino lapansi, ndilibetu abwenzi,
  • Hymn 295 Kubadwa kwa Yesu
  • Hymn 484 Mutiletse, Mbuye,
  • Hymn 28 Mbuye ndisaukadi,
  • Hymn 426 Mpulumutsi Yesu,
  • Hymn 1552 Mpume pa inetu, Mpweya wa Mulungu,
  • Hymn 245 KHALANI duu! Ambuye adzatu;
  • Hymn 967 Mbuye, ndapangana
  • Hymn 384 Mulungu akhale nawo
  • Hymn 710 Nthano ya Hananiyayo
  • Hymn 954 Mbuye andipeza lero,
  • Hymn 402 M’mtima mwangamu mlowemo,
  • Hymn 1138 Masiku onse m’mtima mwanga
  • Hymn 377 Yehova, Mbusa wangadi,
  • Hymn 153 NDAKUMANA ndi bwenzi lokomalo,
  • Hymn 1558 Wosangalatsa, ine ndikalira
  • Hymn 455 Mdileke kulimbna ndi
  • Hymn 946 Ngakhale enawo aleke kwimbako,
  • Hymn 287 POKONDWA ndi poona vuto
  • Hymn 261 Munafera pa mtanda
  • Hymn 337 ‘Tate ‘Nu,
  • Hymn 1157 Mtendere wapambana m’Mwambamo
  • Hymn 461 Inu nonse anzanga,
  • Hymn 773 Mtsinje woyerawo

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version