Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 447 OYAMIKA Mlungu m’bwere,

  1. Home   »  
  2. Hymn 447 OYAMIKA Mlungu m’bwere,

Hymn 447 OYAMIKA Mlungu m’bwere,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 447 OYAMIKA Mlungu m’bwere,

 

OYAMIKA Mlungu m’bwere,
Zamasika mudzayimbe;
Dzinthu dzathu takolola,
Sidzionongeka m’minda.
Mlungu Mlengi asamala,
Zotisowa akonzera;
M’lowe m’nyumba ya Chauta.
M’kweze nyimbo zamasika.

Dziko lonse n’la Mulungu,
Kuti lim’balire dzinthu;
M’munda zonse zimamera,
Zakukoma ndi zoipa.
Mmera udza, bwino ngala,
Maso omwe amakhwima;
Mutilole, mwini dzinthu,
Tikakhale dzinthu dzanu.

Adzabwera Mbuye wathu,
Kukolola dzinthu dzake;
M’munda mwake akachotse,
Minga ndi zoipa zonse.
Adzatumanso angelo,
Minga akaponye m’moto;
Koma tirigu amsunge,
M’nkhokwe yake nthawi zonse.

Post navigation

Previous: Hymn 446 YAMIKANI nonse ’nu,
Next: Hymn 448 CHIFUKWA cha zokoma mtima zonse zaulelezo,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1829 Mulungu ndiye Mbusa wanga, sindisowa konse;
  • Hymn 302 Anasenza m’thupi mwake;
  • Hymn 1003 Kanganani nkhondo yanu
  • Hymn 16 MTIMA wanga lemekeza,
  • Hymn 13 Mtiwerengere m’Mwamba ndi oyera;
  • Hymn 429 M’DZANJA lanu Ambuye,
  • Hymn 1154 Zakutsogolo sitidziwa ‘yi;
  • Hymn 1783 Tinasokera ngati nkhosa,
  • Hymn 1796 Ndikhulupira mwa Ambuye
  • Hymn 1150 Pamtanda Mbuyanga ‘nafera,
  • Hymn 1835 Mtima wanga lemekeza
  • Hymn 933 M’mene imfa yathu idza,
  • Hymn 750 Yesu Mbuyathu, Inu nomwe ‘Nu,
  • Hymn 1337 Bvomerani, Bvomerani,
  • Hymn 1462 Dzina la Yesu ndi lokoma,
  • Hymn 1189 Ambuye Mulungu,
  • Hymn 507 Yesu ndimkonda, akondanso ine,
  • Hymn 1634 Pakwitana Mbuye wanga
  • Hymn 1570 Mutidziwitse ‘Tate wathu,
  • Hymn 666 Walitsani nyali yanu
  • Hymn 851 E, nthawi ya mamawayi
  • Hymn 1500 Simbani Mbiri yomwe,
  • Hymn 471 YESU Mbuye ’Nu wofatsa
  • Hymn 859 Pakufika tsidya lija,
  • Hymn 16 Chikhulupiriro chathu
  • Hymn 924 Kodi uli ndi chisoni
  • Hymn 492 DZIKO lilipolo
  • Hymn 1689 Dzukani nayetu,
  • Hymn 1214 Mwamva Mzimu wakewo,
  • Hymn 144 Yesu, ndipemphera
  • Hymn 719 Anu Mbuye ndifetu!
  • Hymn 349 MOSE anamenya thanthwe kawiri,
  • Hymn 210 PEREKANI mtima wanu,
  • Hymn 473 YESU wa Kumwamba,
  • Hymn 1313 Zindichulukirazi
  • Hymn 350 MBUYE ndayima pano,
  • Hymn 1186 Yesu anafa pamtandapo,
  • Hymn 375 Zipatso zakezi
  • Hymn 59 Tinachoka munjira ya imfa,
  • Hymn 1131 M’mene ine ndisauka
  • Hymn 265 Imbirira moyo wanga,
  • Hymn 275 NTHAWI yathu yafikatu,
  • Hymn 247 MULUNGU anditsogolera,
  • Hymn 95 TAMANI mphamvu ya Yesu,
  • Hymn 320 NDIKONDA Mlungu pomva Mbuye wanga
  • Hymn 1587 Nditama Mlungu m’mtimamo,
  • Hymn 860 Nthawi yina adzadzuka
  • Hymn 827 Wonsewu usiku
  • Hymn 1597 Timchimwira kopambana,
  • Hymn 843 M’maiko monse, zisi zomwe,
  • Hymn 398 KODI mbale wasimba zachikhululukiro,
  • Hymn 84 Aleluya, Aleluya,
  • Hymn 772 Muwalimbikitse onse
  • Hymn 1141 Pakulekana ifetu
  • Hymn 577 Adagona m’ndyeromo
  • Hymn 54 MUNTHU wazisoniyo,
  • Hymn 532 Ukondwere mtima wanga
  • Hymn 1421 Alongo ‘nu, alongo ‘nu,
  • Hymn 569 Tiimbe ndi kulalikira
  • Hymn 1073 Mwa ine myatse moto wanu wakuyera mbuu,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version