Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 447 OYAMIKA Mlungu m’bwere,

  1. Home   »  
  2. Hymn 447 OYAMIKA Mlungu m’bwere,

Hymn 447 OYAMIKA Mlungu m’bwere,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 447 OYAMIKA Mlungu m’bwere,

 

OYAMIKA Mlungu m’bwere,
Zamasika mudzayimbe;
Dzinthu dzathu takolola,
Sidzionongeka m’minda.
Mlungu Mlengi asamala,
Zotisowa akonzera;
M’lowe m’nyumba ya Chauta.
M’kweze nyimbo zamasika.

Dziko lonse n’la Mulungu,
Kuti lim’balire dzinthu;
M’munda zonse zimamera,
Zakukoma ndi zoipa.
Mmera udza, bwino ngala,
Maso omwe amakhwima;
Mutilole, mwini dzinthu,
Tikakhale dzinthu dzanu.

Adzabwera Mbuye wathu,
Kukolola dzinthu dzake;
M’munda mwake akachotse,
Minga ndi zoipa zonse.
Adzatumanso angelo,
Minga akaponye m’moto;
Koma tirigu amsunge,
M’nkhokwe yake nthawi zonse.

Post navigation

Previous: Hymn 446 YAMIKANI nonse ’nu,
Next: Hymn 448 CHIFUKWA cha zokoma mtima zonse zaulelezo,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 871 Tiphatikane tonsefe okonda Yesu Kristu;
  • Hymn 1726 Linadetsedwa dzuwa bii!
  • Hymn 678 Ibukike mbiri yanu,
  • Hymn 1516 Pakudera nkhawa ‘ne,
  • Hymn 1798 Mukondwe anthu a Mulungu,
  • Hymn 771 Tsopano alandira
  • Hymn 1265 Tere moyo wanga wonse,
  • Hymn 1652 Mabala ajawo
  • Hymn 1681 Mphamvu za imfa ndi za Satana
  • Hymn 1152 Pokonda Yesuyo, mtendere!
  • Hymn 1225 Ndinachita mphulupulu,
  • Hymn 58 Titasokera tinabwerera,
  • Hymn 1828 Timtamande Iye ndi moyo wathunso
  • Hymn 978 Mtima wanu wonse ndithu
  • Hymn 1412 Imfa idzafika msanga;
  • Hymn 745 Anatifera nsembe Iyeyo,
  • Hymn 536 Ana inu, myamikeni
  • Hymn 1436 Inde, lero lino Yesu
  • Hymn 1421 Alongo ‘nu, alongo ‘nu,
  • Hymn 1038 Limbikani nonse
  • Hymn 1277 Kuti mukhululukira tchimo langalo
  • Hymn 648 Mulungu wa Kumwamba,
  • Hymn 2 Ndinu wakuyera!
  • Hymn 140 Panalitu wakudwala
  • Hymn 359 Tonse timyamiketu,
  • Hymn 308 AULENDO, munka kuti
  • Hymn 385 SINDILI woyenera ’ne,
  • Hymn 620 Mphatso zonse zathu
  • Hymn 1158 Yesu ndiye Mbuye wanga,
  • Hymn 1660 Ndikakhumudwa
  • Hymn 832 Zochimwa za usana uno mndikhululukire ‘ne;
  • Hymn 1260 Yesu, mulikundipempha, Munaterodi:
  • Hymn 927 Pakutsazikana nanu
  • Hymn 640 Anakwatira kale
  • Hymn 761 Natamndira Mlunguyo
  • Hymn 372 DZUŴA la Mulungu
  • Hymn 263 Mulungu wakwezekatu,
  • Hymn 382 M’wabatize anzathuwa,
  • Hymn 1606 Yesu, dzina lakufatsa,
  • Hymn 607 Dziko lonse lilikukondwa, mlengalenga mpheponso,
  • Hymn 108 MBUYE wondipulumutsa,
  • Hymn 314 TIYENI nonsenu okonda YESUYO,
  • Hymn 566 Ana inu, ana inu,
  • Hymn 1849 Nthawi zonse monga ‘Tate
  • Hymn 438 Yesu ndiye Mbusa
  • Hymn 1723 Unakhetsedwa mwazi do!
  • Hymn 1112 Masiku anga onse
  • Hymn 1133 Ngatitu abwenzi anga
  • Hymn 113 KALERO anthu onse
  • Hymn 1610 Waleka koronayo,
  • Hymn 130 PHWANDO la Belisazara,
  • Hymn 269 Atate ‘nu, amayi ‘nu, nonsenu,
  • Hymn 1068 Ambuye, thandizenitu
  • Hymn 1351 Aleluya, Aleluya,
  • Hymn 1520 Mbuye, Mawu anu
  • Hymn 928 Usalire; Mpulumutsi
  • Hymn 828 Ndidzukanso m’mawa,
  • Hymn 617 Nthawi yina Mbuyeyu
  • Hymn 1829 Mulungu ndiye Mbusa wanga, sindisowa konse;
  • Hymn 1445 Tiyeni tonse, tinkeko

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version