Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 446 YAMIKANI nonse ’nu,

  1. Home   »  
  2. Hymn 446 YAMIKANI nonse ’nu,

Hymn 446 YAMIKANI nonse ’nu,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 446 YAMIKANI nonse ’nu,

 

YAMIKANI nonse ’nu,
Pomwimbira nyimbozi
Za masika athuwa;
Potumiza mvulayi,
Mlungu wathu yemwedi
Atipatsa zonsezi;
Timwimbire m’nyumbayi
Za masika athuwa.

Dziko lathu lonseli
Nla Mulungu yemweyu;
Atumiza mphatsozi
Zakutilimbitsadi,
Mmera wathu wonsewu,
Mbewu zathu zonsezi;
Timtamande Mbuyeyu
Wotipatsa zonsezi.

Nthaŵi yina Mbuyeyu
Adzafika pansipa,
Nadzakonza zonsetu;
Zosakondweretsazi
Naziponya m’motowo,
Koma m’nkhokwe mwakemo
Mudzadzala mbewu tho!
Zokomera bwinotu.

’Dzani Mbuye msangatu,
Msonkhanitse zonse phe;
Anthu anu onsewa,
Muwapulumutse ’wo
Zopweteka zawozo,
Ziwathera zonse phe!
’Dzani mu Ufumu ndi,
K’wasonkhanitsa onse.

Post navigation

Previous: Hymn 445 TILIMALIMA m’minda,
Next: Hymn 447 OYAMIKA Mlungu m’bwere,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 167 Yendanitu, Wansembe wathu,
  • Hymn 578 Falitsani mbiriyi,
  • Hymn 1079 Khalatu woyera,
  • Hymn 123 MULI ndi ludzu, idzani
  • Hymn 413 ZIPATA zachitsulo zitseguke zonse mbee!
  • Hymn 51 PANTHAWI yakufa Ambuye,
  • Hymn 1725 Zochimwa zanga zonsezo
  • Hymn 306 YAMBA ulendo mnzanga,
  • Hymn 93 YAMIKANI dzina la Yesu Khrisituyo,
  • Hymn 807 Mpulumutsi tikagona
  • Hymn 1118 Ndifuna Inu Yesu,
  • Hymn 801 Lero mwatipatsa moyo,
  • Hymn 1185 Imfa ndi mfumu ya mdimawo,
  • Hymn 1132 Mlungu adzandilandila,
  • Hymn 1604 Yesu, dzina lakukonda,
  • Hymn 843 M’maiko monse, zisi zomwe,
  • Hymn 256 Ndilira, ndilira,
  • Hymn 467 Ife ana sitiopa,
  • Hymn 1181 Adalitsika munthuyo
  • Hymn 477 Mpulumutsi, Mbusa wathu,
  • Hymn 1155 Abale angakhale m’talimo
  • Hymn 1229 Dzinalo la Yesu,
  • Hymn 1163 Tili ndi mtendere
  • Hymn 936 Ukatha moyo wanga
  • Hymn 658 Ndichitireni, Mbuye ‘ne,
  • Hymn 1391 Ndiye wokondwa, E, munthuyo
  • Hymn 1470 Chikondi cha Mbuyathu
  • Hymn 21 Mbuye mtsitsimutse!
  • Hymn 212 NDI MISOZI, ndi chisoni,
  • Hymn 1687 Alonda onsewo
  • Hymn 122 Musadziunjikire chuma cha padziko,
  • Hymn 1274 Chisoni andichotsera Mbuyeyu,
  • Hymn 450 Koma usalole
  • Hymn 890 Kumbuka ‘bale ako
  • Hymn 333 Perekani, perekani
  • Hymn 251 NDIFUNA Yesuyo,
  • Hymn 866 Pa la Mulungu tibwera kulandira zidazo;
  • Hymn 957 Mundimwetse madzi anu,
  • Hymn 544 Zoopsya sitidziwapo
  • Hymn 1417 Atate ‘nu, atate ‘nu,
  • Hymn 212 Onse am’Mwamba ali mowemo,
  • Hymn 1532 Mubwere kuno Mzimu ‘Nu,
  • Hymn 26 “Ndakukonda ku imfa
  • Hymn 166 Yendani, Munthu Wachisoni,
  • Hymn 976 Muyendenso kunka komwe,
  • Hymn 439 Nthawi yaubwana yatha,
  • Hymn 1180 Ndine kapolo wa Mbuye wanga;
  • Hymn 26 NDIKULEMEKEZA
  • Hymn 1117 Ndifuna Yesuyo
  • Hymn 788 Moyo watsopano
  • Hymn 665 Pomangidwa anthu nayo
  • Hymn 303 MEMA nkhondoyo, wadza mdaniyo,
  • Hymn 139 Bwerani inu nonse, inu nonse,
  • Hymn 297 POKUMANA m’mayesero a dziko lino,
  • Hymn 2 YEHOVA Mthandizi,
  • Hymn 920 Yatha misoziyo,
  • Hymn 275 Mlungu akuyang’aniredi,
  • Hymn 405 M’mtima mwangamu mlowemo,
  • Hymn 329 MUMZINDA wa Mulungu
  • Hymn 65 Chisomo chodabwitsacho

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version