Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 446 YAMIKANI nonse ’nu,

  1. Home   »  
  2. Hymn 446 YAMIKANI nonse ’nu,

Hymn 446 YAMIKANI nonse ’nu,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 446 YAMIKANI nonse ’nu,

 

YAMIKANI nonse ’nu,
Pomwimbira nyimbozi
Za masika athuwa;
Potumiza mvulayi,
Mlungu wathu yemwedi
Atipatsa zonsezi;
Timwimbire m’nyumbayi
Za masika athuwa.

Dziko lathu lonseli
Nla Mulungu yemweyu;
Atumiza mphatsozi
Zakutilimbitsadi,
Mmera wathu wonsewu,
Mbewu zathu zonsezi;
Timtamande Mbuyeyu
Wotipatsa zonsezi.

Nthaŵi yina Mbuyeyu
Adzafika pansipa,
Nadzakonza zonsetu;
Zosakondweretsazi
Naziponya m’motowo,
Koma m’nkhokwe mwakemo
Mudzadzala mbewu tho!
Zokomera bwinotu.

’Dzani Mbuye msangatu,
Msonkhanitse zonse phe;
Anthu anu onsewa,
Muwapulumutse ’wo
Zopweteka zawozo,
Ziwathera zonse phe!
’Dzani mu Ufumu ndi,
K’wasonkhanitsa onse.

Post navigation

Previous: Hymn 445 TILIMALIMA m’minda,
Next: Hymn 447 OYAMIKA Mlungu m’bwere,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 140 NDINAMIRA m’machimo, wosaonekanso,
  • Hymn 269 Atate ‘nu, amayi ‘nu, nonsenu,
  • Hymn 1827 Abramu kalelo anamvera bwino;
  • Hymn 500 >AMEN, Amen, Amen.
  • Hymn 709 Munthu aganize
  • Hymn 228 MWAKHULUPIRIRADI
  • Hymn 525 Afike masiku
  • Hymn 540 Amithenga akumwamba
  • Hymn 1293 Chitsimecho cha mwaziwo
  • Hymn 1650 E, moyo wanga’we
  • Hymn 1551 Mukhale m’kati mwathu,
  • Hymn 839 Adani sindiopa mukalipo;
  • Hymn 1447 Yesu ngwachifundodi,
  • Hymn 1695 Pokumbukira mtandawo
  • Hymn 348 CHIKHULUPIRIRO chathu
  • Hymn 1310 Yesu wondikondadi,
  • Hymn 18 POKHALA Inu
  • Hymn 126 Mwa ine, moyo wanga ndi Yesu
  • Hymn 273 USAFUNE chuma chokha,
  • Hymn 921 Komwe Mbusa kwawoko
  • Hymn 430 MLUNGU akuyang’aniredí,
  • Hymn 1141 Pakulekana ifetu
  • Hymn 132 Ganizansoni, ali pano,
  • Hymn 456 ANA inu, ana inu,
  • Hymn 436 YEHOVA Mlungu wathu,
  • Hymn 1481 Timsankhe Yesu Mbuyeyo,
  • Hymn 492 DZIKO lilipolo
  • Hymn 906 Mulibe zoipa m’Dzikolo,
  • Hymn 1566 Mufike monga ngati mphepo yokokomayo,
  • Hymn 335 KWATHU sipadziko, ndingopitilira,
  • Hymn 510 Ngolizo zilira
  • Hymn 1383 Dzina lake tibukitsa,
  • Hymn 1212 Zina ndi zinanso
  • Hymn 386 MONGATU mawu anuwo,
  • Hymn 1170 Pamtanda wake
  • Hymn 1705 Pa Iye padzapo
  • Hymn 1556 Mzimu Woyera, mudzetu kwa ine,
  • Hymn 1127 Mbuyanga Yesu, mundigwire dzanja;
  • Hymn 441 MBUYE, tikuthokozani,
  • Hymn 1440 Yesu alindira,
  • Hymn 1097 Njira yanga sindidziwa,
  • Hymn 473 Mzinda woyerawo!
  • Hymn 363 Funani Mlungu tsopano,
  • Hymn 862 Tidza kwa Mulungu Inu, ndinu wa chifundo;
  • Hymn 199 NDINASOKERA kutali,
  • Hymn 298 IFE tazingidwa ndi zinthu zoopsa,
  • Hymn 926 Mbale wako unamkonda,
  • Hymn 939 Ambuye andisunga
  • Hymn 763 Ndiponso m’manja chikhocho
  • Hymn 1672 Lambira Mfumuyo,
  • Hymn 194 AMBUYE’naitan’ne;
  • Hymn 1359 Ndi Aleluya imbirani
  • Hymn 1205 Ndikonda chifukwa
  • Hymn 347 YESU, ndipemphera
  • Hymn 1041 Zosauka unvomere,
  • Hymn 297 POKUMANA m’mayesero a dziko lino,
  • Hymn 924 Kodi uli ndi chisoni
  • Hymn 846 Kristu wakuyeratu,
  • Hymn 722 Anu Mbuye ndifetu!
  • Hymn 299 TIYENI, Akristu inu,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version