Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 446 YAMIKANI nonse ’nu,

  1. Home   »  
  2. Hymn 446 YAMIKANI nonse ’nu,

Hymn 446 YAMIKANI nonse ’nu,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 446 YAMIKANI nonse ’nu,

 

YAMIKANI nonse ’nu,
Pomwimbira nyimbozi
Za masika athuwa;
Potumiza mvulayi,
Mlungu wathu yemwedi
Atipatsa zonsezi;
Timwimbire m’nyumbayi
Za masika athuwa.

Dziko lathu lonseli
Nla Mulungu yemweyu;
Atumiza mphatsozi
Zakutilimbitsadi,
Mmera wathu wonsewu,
Mbewu zathu zonsezi;
Timtamande Mbuyeyu
Wotipatsa zonsezi.

Nthaŵi yina Mbuyeyu
Adzafika pansipa,
Nadzakonza zonsetu;
Zosakondweretsazi
Naziponya m’motowo,
Koma m’nkhokwe mwakemo
Mudzadzala mbewu tho!
Zokomera bwinotu.

’Dzani Mbuye msangatu,
Msonkhanitse zonse phe;
Anthu anu onsewa,
Muwapulumutse ’wo
Zopweteka zawozo,
Ziwathera zonse phe!
’Dzani mu Ufumu ndi,
K’wasonkhanitsa onse.

Post navigation

Previous: Hymn 445 TILIMALIMA m’minda,
Next: Hymn 447 OYAMIKA Mlungu m’bwere,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 802 Ndife anthu aulendo,
  • Hymn 10 Kristu Mfumuyo yaulemerero!
  • Hymn 221 A! CHIKONDI chopambana,
  • Hymn 438 Yesu ndiye Mbusa
  • Hymn 131 MAWU a Mulungu awa,
  • Hymn 1604 Yesu, dzina lakukonda,
  • Hymn 1625 Ife tonse tikumbuke
  • Hymn 903 Iwo salekana, iwo salekana,
  • Hymn 633 Tikasokera m’njira mutilondolere ndithu,
  • Hymn 744 Kristu ndi mwini moyo wathuwu,
  • Hymn 331 Yesu ndimafuna Inu,
  • Hymn 807 Mpulumutsi tikagona
  • Hymn 41 MKATI mwa zovuta zathu
  • Hymn 976 Muyendenso kunka komwe,
  • Hymn 1034 Mkristu, ulimbike
  • Hymn 304 POZUNZIDWA inu ponseponse
  • Hymn 1177 Ndidziwitsitsa Yesu ndi wanga,
  • Hymn 484 Mutiletse, Mbuye,
  • Hymn 1798 Mukondwe anthu a Mulungu,
  • Hymn 1388 Tiimbire Mlungu wathu
  • Hymn 260 Angelo aitana,
  • Hymn 249 Amen, Amen, Amen.
  • Hymn 1151 Pomulambira Yesu Mbuyanga,
  • Hymn 354 Tinafunafunatu,
  • Hymn 199 Watitsogolera Mbuye,
  • Hymn 435 ANAKWATIRA kale
  • Hymn 86 Mwandipatulira ine,
  • Hymn 1194 Padziko lapansi
  • Hymn 1275 Mtima ‘we siya ndi Yesu nsonizi,
  • Hymn 963 Aulendo, munka kuti
  • Hymn 743 Mudze, anthuni, talawani ‘nu
  • Hymn 1431 Lero lino m’bale wanga,
  • Hymn 1451 Okoma ndiwo mawu
  • Hymn 113 Likalira llipengalo,
  • Hymn 181 PANALITU wakudwala
  • Hymn 888 Polowa ndi Inu
  • Hymn 1570 Mutidziwitse ‘Tate wathu,
  • Hymn 349 Aitana,
  • Hymn 49 ONA Mwanawankhosayo
  • Hymn 1448 Yesu ndiye Bwenzi lanu,
  • Hymn 1316 Ndabwera kwa Ambuyeyo:
  • Hymn 36 Nyengo ifika, chenjera!
  • Hymn 1594 Chikondano chakechi
  • Hymn 445 Mlewe oipawo,
  • Hymn 1079 Khalatu woyera,
  • Hymn 1698 Chinkana dziko lonselo
  • Hymn 493 DZUŴA li
  • Hymn 341 Ayenda,
  • Hymn 218 NDIPEREKA zanga zonse
  • Hymn 1311 Pothawira pena ‘yi,
  • Hymn 127 Mwazi wake ndi chitsime changa,
  • Hymn 615 Yamikani nonse ‘nu,
  • Hymn 1611 Nadzuka m’mandamo
  • Hymn 1047 Ambuye, chotsani zonse zomwezo
  • Hymn 998 Anatilemba Yesu tikagwire nkhondo yake,
  • Hymn 1398 Nditama mphamvu yake
  • Hymn 123 MULI ndi ludzu, idzani
  • Hymn 547 Anatikondakonda ‘Ye.
  • Hymn 233 M’mene ndapenya mwazi wa
  • Hymn 201 NDILINKUDZA kwa Ambuye,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version