Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 294 POYESEDWA ine

  1. Home   »  
  2. Hymn 294 POYESEDWA ine

Hymn 294 POYESEDWA ine

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 294 POYESEDWA ine

 

POYESEDWA ine
Yesu mudzetu,
Mundipempherere
Ndisachimwetu.
Mukaona kuti
Ndilefukatu,
Mbuye mndilimbitse
Nazo mphamvutu.

Ndi zapansi pano
Ndikokedwadi,
Koma ndi chisoni
Mndiphunzitsedi;
Ndisaiŵalire
Za Getsemane,
Pena mtanda wanu
Yesu Mbuye ’Nu.

Mukandipweteka,
Ndipirirapo:
Nsembe yanga ndiyo,
Landirani ’yo.
Ndikachita mantha Sindithaŵa ’yi:
Mtima udzalimba,
Ndidzaima nji!

Pakumalizidwa
Moyo wangawu,
Pomwalira ine,
Mudze Mbuyetu.
Ndidzadzipereka
M’manja mwanumo:
Mpulumutsi Yesu
Mndilandireko.

Post navigation

Previous: Hymn 293 LIMBA mtima mbale wanga
Next: Hymn 295 AMBUYE wa Kumwamba,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 547 Anatikondakonda ‘Ye.
  • Hymn 103 MPUME pa inetu, Mpweya wa Mulungu,
  • Hymn 1558 Wosangalatsa, ine ndikalira
  • Hymn 1656 Inu mundibisadi
  • Hymn 453 A! MULUNGU
  • Hymn 149 Ndisauka, sindikhoza
  • Hymn 414 Ana ake adzapuma
  • Hymn 862 Tidza kwa Mulungu Inu, ndinu wa chifundo;
  • Hymn 493 DZUŴA li
  • Hymn 145 Kale ndinafuna
  • Hymn 561 Uyu ‘natsikira kuno,
  • Hymn 1075 Ndikhazikike inetu, mumtima muli mwai,
  • Hymn 806 Kapena wina leroli
  • Hymn 620 Mphatso zonse zathu
  • Hymn 1424 Malo anachepa,
  • Hymn 4 Ndinu wakuyera!
  • Hymn 1570 Mutidziwitse ‘Tate wathu,
  • Hymn 418 M’manja Yesu wanga
  • Hymn 1553 Mpume pa inetu, Mpweya wa Mulungu,
  • Hymn 93 YAMIKANI dzina la Yesu Khrisituyo,
  • Hymn 251 NDIFUNA Yesuyo,
  • Hymn 10 Kristu Mfumuyo yaulemerero!
  • Hymn 630 Ena atsagana nafe
  • Hymn 1534 Mukonze mtima wangawu,
  • Hymn 1843 Chigwa choopsacho cha imfa ndikachilowera,
  • Hymn 1855 Yesu, msandipitirire
  • Hymn 524 Wokoma Mbuyathu
  • Hymn 412 Kudzachera tsiku lijalo
  • Hymn 685 Tamva mawu amwewo
  • Hymn 81 Imva mawu akewo,
  • Hymn 1078 Khalatu woyera
  • Hymn 202 Timpemphere kutipatsa
  • Hymn 1072 Mudzaze Yesu mtima wanga ndi chikondicho,
  • Hymn 1216 Ndatsatatsatabe
  • Hymn 143 Lero lino Mbuye Yesu
  • Hymn 542 Kuli kaphiri m’talimo
  • Hymn 59 IMVANI uthenga,
  • Hymn 1735 “Sezani mtanda wanuwu.”
  • Hymn 709 Munthu aganize
  • Hymn 179 TUMPHATUMPHA moyo wanga,
  • Hymn 583 Anabadwa,
  • Hymn 446 YAMIKANI nonse ’nu,
  • Hymn 1370 Mphepo yay’kulu yakuombayo,
  • Hymn 496 MBUYE dalitsani Afirika.
  • Hymn 1854 Tate msandipitirire,
  • Hymn 805 Madzulo ano mkhaletu
  • Hymn 259 Zoipa zakanikadi,
  • Hymn 1522 Tikaona bvuto,
  • Hymn 1494 Mbiri yakalelomwe,
  • Hymn 209 M’NDILANDIRE ine Mbuye
  • Hymn 1303 Aa! Mulungu wanga,
  • Hymn 351 Titi bwanji?
  • Hymn 1187 M’mitima mwathu mwakhala mbee!
  • Hymn 378 Ku madzi ake odikha
  • Hymn 295 Kubadwa kwa Yesu
  • Hymn 1010 Ndipo ngati ungolema,
  • Hymn 1440 Yesu alindira,
  • Hymn 995 Taya zako zochenjera,
  • Hymn 167 KODI mwalandira Yesu?
  • Hymn 121 Imbira!

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version