Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 453 A! MULUNGU

  1. Home   »  
  2. Hymn 453 A! MULUNGU

Hymn 453 A! MULUNGU

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 453 A! MULUNGU

 

A! MULUNGU
A! Mulungu
Anatuma mwana wake
Uja, ndiye Yesu

Anabadwa,
Anabadwa
Ndi Maria Mbeta ija
M’Betlehem muja.

Ndi angelo,
Ndi angelo
Anaimba: “Ndiye Yesu
Mpulumutsi wanu.”

Alanditsa,
Alanditsa
Ife anthu muzoipa
Zonse tazichita.

Yesu Mfumu
Yesu Mfumu,
Timagonja, mutisunge
Moyo wathu wonse.

Mutisuke,
Mutisuke
M’mwazi wanu, tikakhale
Ana anu tonse.

Post navigation

Previous: Hymn 452 MLUNGU, Inutu,
Next: Hymn 454 TAONANI, m’kholamo,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1086 “Khala mwa Ine,” ndinu mwini moyo,
  • Hymn 1251 Ndasokera m’tali ndithu
  • Hymn 761 Natamndira Mlunguyo
  • Hymn 1479 Ndi Yesu yemwe kalelo
  • Hymn 400 Dzuwa liwala, m’tulotu
  • Hymn 407 Zochimwa sizilowako,
  • Hymn 1498 Simbani Mbiri yonse
  • Hymn 809 Madzulo aja kalelo
  • Hymn 1333 Idzatu kwa Yesuyo,
  • Hymn 619 Tilimalima m’minda,
  • Hymn 482 TCHIMO musalole, musadziipitse,
  • Hymn 881 Tili nazo zotiyesa,
  • Hymn 883 Pokupempherani
  • Hymn 709 Munthu aganize
  • Hymn 129 Mudze kwa Yesu, musachedwe,
  • Hymn 1500 Simbani Mbiri yomwe,
  • Hymn 73 M’SANDIPITILIRE Yesu,
  • Hymn 1726 Linadetsedwa dzuwa bii!
  • Hymn 57 TIYENI, dzalireni nane,
  • Hymn 846 Kristu wakuyeratu,
  • Hymn 888 Polowa ndi Inu
  • Hymn 554 Iye ndani pamtanda
  • Hymn 279 MBUYE, nditsate bwanjiko?
  • Hymn 1217 Chisoni chonsecho
  • Hymn 1674 Lambira Yesuyo,
  • Hymn 926 Mbale wako unamkonda,
  • Hymn 1102 Dziko lonse ndilitaya;
  • Hymn 1605 Yesu, dzina lokondwetsa
  • Hymn 1601 Zina za Yesu ndimvetu,
  • Hymn 1193 Tsopano Mulungu
  • Hymn 497 TILIKUIMBA nyimbo yomweyi,
  • Hymn 1235 Yesu wathadi
  • Hymn 257 Ndinasiya amayi,
  • Hymn 444 Mpemphe Mbuye asunge
  • Hymn 139 MLUNGU anapatsa moyo,
  • Hymn 31 Tamandani mbuye,
  • Hymn 1492 Sakukanani Yesudi,
  • Hymn 637 Mbuyathu wokondedwa,
  • Hymn 38 Kodi mubvutidwa naye katundu?
  • Hymn 259 CHISOMO chodabwitsacho,
  • Hymn 1458 Satana ndi unyolo
  • Hymn 335 Mtembenuke mtima wanu,
  • Hymn 1106 Mlungu ndi wachikhalire.
  • Hymn 242 NDIIMBA mumtima mokondwa,
  • Hymn 321 PAKUONA imfayo
  • Hymn 381 Chakudya changa chabwino
  • Hymn 173 Mema nkhondoyo, wadza mdaniyo,
  • Hymn 1774 Poti akumbukira
  • Hymn 937 Chitsime chachikondi
  • Hymn 661 Tamva aku Makedonyako atero,
  • Hymn 339 Tipempha,
  • Hymn 1672 Lambira Mfumuyo,
  • Hymn 802 Ndife anthu aulendo,
  • Hymn 441 Tamverani, aitana:
  • Hymn 72 YESU wakukoma mtima,
  • Hymn 435 ANAKWATIRA kale
  • Hymn 215 TATE ndili mwana wanu,
  • Hymn 1722 Ambuye tikondweratu
  • Hymn 1577 “Kwa Iye atikonda
  • Hymn 535 Mbuye timlemekeze,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version