Site icon Treasure Hymns – Chichewa

Hymn 453 A! MULUNGU

Chichewa Christian Hymns

Hymn 453 A! MULUNGU

 

A! MULUNGU
A! Mulungu
Anatuma mwana wake
Uja, ndiye Yesu

Anabadwa,
Anabadwa
Ndi Maria Mbeta ija
M’Betlehem muja.

Ndi angelo,
Ndi angelo
Anaimba: “Ndiye Yesu
Mpulumutsi wanu.”

Alanditsa,
Alanditsa
Ife anthu muzoipa
Zonse tazichita.

Yesu Mfumu
Yesu Mfumu,
Timagonja, mutisunge
Moyo wathu wonse.

Mutisuke,
Mutisuke
M’mwazi wanu, tikakhale
Ana anu tonse.

Exit mobile version