Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 453 A! MULUNGU

  1. Home   »  
  2. Hymn 453 A! MULUNGU

Hymn 453 A! MULUNGU

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 453 A! MULUNGU

 

A! MULUNGU
A! Mulungu
Anatuma mwana wake
Uja, ndiye Yesu

Anabadwa,
Anabadwa
Ndi Maria Mbeta ija
M’Betlehem muja.

Ndi angelo,
Ndi angelo
Anaimba: “Ndiye Yesu
Mpulumutsi wanu.”

Alanditsa,
Alanditsa
Ife anthu muzoipa
Zonse tazichita.

Yesu Mfumu
Yesu Mfumu,
Timagonja, mutisunge
Moyo wathu wonse.

Mutisuke,
Mutisuke
M’mwazi wanu, tikakhale
Ana anu tonse.

Post navigation

Previous: Hymn 440 ZIKOMO Ambuye wathu,
Next: Hymn 461 ANA inu, myamikeni

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 167 KODI mwalandira Yesu?
  • Hymn 152 Inde, Yesu, mundikonda,
  • Hymn 170 M’manda naukamo
  • Hymn 564 Ndi chifukwa atikonda,
  • Hymn 174 YESU wathu Mbuyeyo
  • Hymn 1065 Ngakhale Satana andizunza ‘ne,
  • Hymn 1174 Sindinanyengedwa konse;
  • Hymn 532 Ukondwere mtima wanga
  • Hymn 182 YESU watidzera, watidzera,
  • Hymn 1715 Kodi misozi itisowa,
  • Hymn 166 Yendani, Munthu Wachisoni,
  • Hymn 1763 Amithenga anaimba
  • Hymn 12 NDITAMATU Ambuyangayu,
  • Hymn 822 Dzuwa lapitira,
  • Hymn 1767 Ndiye anayang’ana
  • Hymn 605 Chifukwa cha zokoma mtima zonse za ulerezo,
  • Hymn 444 YEMWE afesa nalira,
  • Hymn 1380 Tilemekezetu
  • Hymn 122 Musadziunjikire chuma cha padziko,
  • Hymn 307 Atate Wamkulu ndi wamphamvu zonse,
  • Hymn 460 E! ang’ono ndifetu,
  • Hymn 764 “Chikho cha mwazi wangachi
  • Hymn 48 IMFA ya Mwana wa Mulungu,
  • Hymn 1464 Nditama Nsembe ya Mulungu,
  • Hymn 24 TITAME Mlungu Wakumwamba,
  • Hymn 350 MBUYE ndayima pano,
  • Hymn 1373 Zamoyo zili m’thengo zonsezo,
  • Hymn 927 Pakutsazikana nanu
  • Hymn 580 Mwana wakuyera ‘Nu,
  • Hymn 1349 Salephera, salephera,
  • Hymn 1351 Aleluya, Aleluya,
  • Hymn 140 NDINAMIRA m’machimo, wosaonekanso,
  • Hymn 1754 Ndiye akumbukira
  • Hymn 46 O! ufulu tigwirizane
  • Hymn 469 NDIKONDA mbiri yomwe
  • Hymn 1414 Zonse zinathedwadi;
  • Hymn 613 Dziko lonse nla Mulungu
  • Hymn 1636 Potuluka m’manda mwawo
  • Hymn 327 Yesu salephera ‘yi.
  • Hymn 1426 Wina panalibe
  • Hymn 995 Taya zako zochenjera,
  • Hymn 41 MKATI mwa zovuta zathu
  • Hymn 73 M’SANDIPITILIRE Yesu,
  • Hymn 1714 Tiyeni, dzalireni nane,
  • Hymn 363 Funani Mlungu tsopano,
  • Hymn 306 YAMBA ulendo mnzanga,
  • Hymn 318 Ambuye, muli nazo zambirizi,
  • Hymn 419 M’manja a Yesu wanga
  • Hymn 1639 Aleluya, aleluya,
  • Hymn 1456 Pakuti anthu akumvera
  • Hymn 1660 Ndikakhumudwa
  • Hymn 1042 Zonse umazinyadira
  • Hymn 292 NDIPULUMUTSENI Mbuye,
  • Hymn 1415 Iye anatsika m’Mwamba,
  • Hymn 1675 Lambira Mfumuyo
  • Hymn 615 Yamikani nonse ‘nu,
  • Hymn 53 Dalitsani mafumu athu,
  • Hymn 1315 Ambuye ‘naitana ‘ne:
  • Hymn 439 Nthawi yaubwana yatha,
  • Hymn 484 YESU ndiye Mbusa,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version