Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 103 MPUME pa inetu, Mpweya wa Mulungu,

  1. Home   »  
  2. Hymn 103 MPUME pa inetu, Mpweya wa Mulungu,

Hymn 103 MPUME pa inetu, Mpweya wa Mulungu,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 103 MPUME pa inetu, Mpweya wa Mulungu,

 

MPUME pa inetu, Mpweya wa Mulungu,
Ndi kundidzaza moyo wanuwo,
Kuti ndikonde zomwe mukondanso,
Ndichite chomwe mumachitanso.

Mpume pa inetu, Mpweya wa Mulungu,
Mpaka mtimanga ukayeretu,
Ndipo zokhumba zanga zilingane
Nazo zanuzo zakuyera mbuu!

Mpume pa inetu, Mpweya wa Mulungu,
Mpaka ndikhale wanu nokhatu;
Ayeretsedwe makhalidwe anga
Ndi mphamvu yanu yondisunga nji!

Mpume pa inetu, Mpweya wa Mulungu,
Kuti inedi ndisafe ’yitu,
Koma ndikhale nanu m’moyo womwe
Wangwiro ndi wa nthaŵi zonsetu.

Post navigation

Previous: Hymn 102 MZIMU Woyera, mudzetu kwa ine
Next: Hymn 104 MUBWERE Mzimu Inu

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1702 Pakufa ine Mbuye
  • Hymn 35 KODI mwaona chiyani,
  • Hymn 1249 Tsirizani ntchito yanu
  • Hymn 678 Ibukike mbiri yanu,
  • Hymn 1168 Aleluya, muyenera!
  • Hymn 672 Mbwere Yesu Mwini moyo,
  • Hymn 1369 Paphiri paja papakulupo,
  • Hymn 843 M’maiko monse, zisi zomwe,
  • Hymn 139 MLUNGU anapatsa moyo,
  • Hymn 1725 Zochimwa zanga zonsezo
  • Hymn 701 Inu Atatuwo,
  • Hymn 80 Utsegule mtimawo,
  • Hymn 73 M’SANDIPITILIRE Yesu,
  • Hymn 1830 Ndiye M’busa wanga
  • Hymn 612 Oyamika Mlungu mbwere,
  • Hymn 374 Pakuti Mfumuyo
  • Hymn 565 Koma sitimpenya m’khola
  • Hymn 320 NDIKONDA Mlungu pomva Mbuye wanga
  • Hymn 429 Haya! Tipitenso
  • Hymn 212 NDI MISOZI, ndi chisoni,
  • Hymn 482 Ndinu wakuyera,
  • Hymn 443 Tchimo musalole,
  • Hymn 1115 M’munda wa Mbuyako
  • Hymn 14 MTIMA wanga uyamike,
  • Hymn 121 Imbira!
  • Hymn 300 AKRISTU limbikani,
  • Hymn 503 Ndikondwa kuti Yesu
  • Hymn 459 Aphunzitse anthuwo,
  • Hymn 955 Komwe ndi chimwemwe ine
  • Hymn 352 NONSE okhala pansipa,
  • Hymn 391 Mufafanize m’bukumo
  • Hymn 1053 Mtimatu wopirira ndi
  • Hymn 1776 Tiyeni timgwadire
  • Hymn 1358 Lemekeza Mfumu yathu,
  • Hymn 1305 Ndi ine pondibvutapo
  • Hymn 41 Tiyeni, tiyeni,
  • Hymn 437 Yesu ndiye Mbusa,
  • Hymn 1076 Khalatu woyera,
  • Hymn 446 Yesu alandira
  • Hymn 509 Ndikadzaona Ambuye Kumwamba,
  • Hymn 232 Uchita kwombola,
  • Hymn 185 Kondwani nonsenu,
  • Hymn 475 Mbuye ndikhaletu
  • Hymn 1283 Yesu ndikhulupirira
  • Hymn 100 M’mene masautso onse,
  • Hymn 863 A! maliro m’Mpingo mwanu kulirira ‘balewo
  • Hymn 299 TIYENI, Akristu inu,
  • Hymn 370 KWACHA lero kwati mbee,
  • Hymn 1424 Malo anachepa,
  • Hymn 1726 Linadetsedwa dzuwa bii!
  • Hymn 276 MKRISTU, ulimbike
  • Hymn 1735 “Sezani mtanda wanuwu.”
  • Hymn 1717 Mtima wangawe, uyenera
  • Hymn 1470 Chikondi cha Mbuyathu
  • Hymn 690 Mu ulemerero,
  • Hymn 1554 Mpume pa inetu, Mpweya wa Mulungu,
  • Hymn 1225 Ndinachita mphulupulu,
  • Hymn 1074 Mubweretu nomwe ‘Nu munatsika kalelo;
  • Hymn 800 Yesu munadzukanso
  • Hymn 1280 Kuti mundipatsa mphamvu yopambanayo;

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version