Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 14 MTIMA wanga uyamike,

  1. Home   »  
  2. Hymn 14 MTIMA wanga uyamike,

Hymn 14 MTIMA wanga uyamike,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 14 MTIMA wanga uyamike,

 

MTIMA wanga uyamike,
Mfumu ya Kumwambako,
Anandiwombola ine;
Nanditsuka m’mtimamo.

Ife tonse, ife tonse,
Tiyamike Mlunguyo.

Tiyamike Mulungu wathu,
Kaamba ka chifundocho;
Nthaŵi zonse sasinthika,
Mlungu wathu yemweyo.

Nthaŵi zonse monga Tate,
Atisamaliratu;
Atisunga m’manja mwake,
Atipulumutsatu.

Anthu a mitundu yonse,
Ndiponso a Kumwamba;
Yamikani Mungu wathu,
Ndiye wakukomatu.

Anthu onse, anthu onse,
Yamikani Mlunguyo.

Post navigation

Previous: Hymn 13 PAPHIRI ndi padambo,
Next: Hymn 15 YEHOVA ndiye Mbusa wanga,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 454 Kapena m’mtima ndimakwiya,
  • Hymn 1786 Ndikonda Mlungu pomva Mbuye wanga
  • Hymn 1713 Zochimwa zanga zonsezo
  • Hymn 55 UNAKHETSEDWA mwazi do!
  • Hymn 268 Potuluka m’mudzimo
  • Hymn 541 Ana inu, yamikani
  • Hymn 56 Masiku onse timakondwera
  • Hymn 39 Poyang’ana ena ndi ndalamatu,
  • Hymn 155 UTHENGA wa Mulungu
  • Hymn 478 Ndife ana, mutikonda,
  • Hymn 341 Ayenda,
  • Hymn 271 Zoipa zangazi
  • Hymn 233 M’mene ndapenya mwazi wa
  • Hymn 1815 Choposa nalo thupilo,
  • Hymn 590 Mbuye, Msungi ‘Nu,
  • Hymn 120 MUNDINYEMERE ’ne
  • Hymn 481 USACHIMWE konse,
  • Hymn 390 Lalowa dzuwa, kwada bii!
  • Hymn 407 Zochimwa sizilowako,
  • Hymn 633 Tikasokera m’njira mutilondolere ndithu,
  • Hymn 834 Tiyamike Mlungu wotipatsa zachifundozi,
  • Hymn 1747 Yesu aitana ife;
  • Hymn 683 Musamaopa kanthu ‘yi, tamani Yesuyo;
  • Hymn 34 AMITHENGA a Mulungu,
  • Hymn 866 Pa la Mulungu tibwera kulandira zidazo;
  • Hymn 397 Yesu Mbusa, mutimvere,
  • Hymn 1219 Bwenzi ndinamkomanayo
  • Hymn 1665 Nkhope yanu ndifunitsa,
  • Hymn 1392 Mlungu kuona athiratu
  • Hymn 313 MUNDIŴALIRE m’njira mwangamo,
  • Hymn 174 Haya, anzathu, itilinda nkhondo;
  • Hymn 96 MTIMA wanga uyamiketu,
  • Hymn 600 Mbuye Yesu, myandikire,
  • Hymn 261 M’NDIYANDIKITSE nanu Yesu,
  • Hymn 70 LAMBIRA, Mfumuyo,
  • Hymn 1360 Ndi Aleluya imbirani
  • Hymn 206 YESU, mulikundipempha
  • Hymn 595 Mbuye, ndinu wamphamvu,
  • Hymn 1148 Ndiimba mumtima mokondwa
  • Hymn 1534 Mukonze mtima wangawu,
  • Hymn 859 Pakufika tsidya lija,
  • Hymn 1188 Akumangidwa ndi mzimuwo,
  • Hymn 497 Yesu andikonda ine,
  • Hymn 351 CHIYEMBEKEZO changacho,
  • Hymn 243 Mtima wanga udzakondwera,
  • Hymn 847 Konse kuli mdima bii
  • Hymn 1555 Mpume pa inetu, Mpweya wa Mulungu,
  • Hymn 289 Ndi manja athu awa nawo nganu,
  • Hymn 1572 Mumbveke, mbveke, mbveke,
  • Hymn 139 MLUNGU anapatsa moyo,
  • Hymn 254 Adzanena kwa anthuwo
  • Hymn 476 MBUYE, tili ana anu,
  • Hymn 651 Ikhale ngati nyali
  • Hymn 58 PAMTANDAPO Ambuyeyo
  • Hymn 194 AMBUYE’naitan’ne;
  • Hymn 1727 Pokumbukira mtandawo
  • Hymn 475 MZINDA woyerawo
  • Hymn 232 WAFUNAFUNA ine
  • Hymn 1599 Inde, ndifuna kumvatu
  • Hymn 138 SANGALATSA akusowa, masiku alikutha,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version