Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 194 AMBUYE’naitan’ne;

  1. Home   »  
  2. Hymn 194 AMBUYE’naitan’ne;

Hymn 194 AMBUYE’naitan’ne;

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 194 AMBUYE’naitan’ne;

 

AMBUYE’naitan’ne;
“Dzapumulire kuno,
Tsamira mutu, mwana’we
M’chifuwa mwanga muno.”

Ndabwera kwa Ambuyeyo;
Wolema, wachisoni;
Anandipulumutsako,
Nakondweretsa ine.

Ambuye naitana’ne;
“Ndipatsa anthu madzi,
Wotopa ndi waludzu’we
Dzamwere moyo kuno.”

Ndabwera kwa Ambuyeyo.
Ndamwera madzi awa;
Laleka ndithu ludzulo,
Tsopano moyo wadza

Ambuye naitana’ne;
“La dziko ndine Dzuŵa,
Yang’ana Ine, kwacha’we,
Wachoka mdima uja.”

Ndayang’anira Mbuyeyo
Ndzapeza Dzuŵa langa
Londiyendetsa bwinoli
Pa njira yanga yonse.

Post navigation

Previous: Hymn 193 THANTHWE long’ambikatu,
Next: Hymn 195 YESU wondikondadi,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 895 Ndikabwera ndi katundu
  • Hymn 574 A! Yesu Mbuye wakuyera,
  • Hymn 868 Atate yemwe anatuma Mpulumutsi mmodzi
  • Hymn 439 MLUNGU wathu mwatifitsa
  • Hymn 1347 Akukonda, akukonda,
  • Hymn 321 PAKUONA imfayo
  • Hymn 26 “Ndakukonda ku imfa
  • Hymn 443 M’MAŴA tizifesa
  • Hymn 91 Ufuna kuyera kopambana?
  • Hymn 186 MVERANI mbiri yozizwitsa
  • Hymn 1207 Poyambapo ndakondwadi,
  • Hymn 609 Zanu zapansi nzokoma Mbuye; tikondwera ‘fe,
  • Hymn 428 Tiyandika, Mbuye,
  • Hymn 1591 Sizitha ntchito zangazo,
  • Hymn 329 Yesu atonthoza mtima
  • Hymn 154 Pemphero ndiko kulira,
  • Hymn 1118 Ndifuna Inu Yesu,
  • Hymn 1481 Timsankhe Yesu Mbuyeyo,
  • Hymn 135 USANABADWE, Yeremiya,
  • Hymn 1695 Pokumbukira mtandawo
  • Hymn 406 M’MENE umauka m’maŵa,
  • Hymn 1845 Zabwino ndi zokoma zinditsata chitsatire;
  • Hymn 275 NTHAWI yathu yafikatu,
  • Hymn 1213 Mwamva Yesu m’mtimamo,
  • Hymn 467 NGOLIZO zilira
  • Hymn 615 Yamikani nonse ‘nu,
  • Hymn 500 >AMEN, Amen, Amen.
  • Hymn 885 Mndimvetse chisoni
  • Hymn 843 M’maiko monse, zisi zomwe,
  • Hymn 1037 Mapemphero athu
  • Hymn 261 Munafera pa mtanda
  • Hymn 76 E, MOYO wanga’we
  • Hymn 819 Lero tigone,
  • Hymn 1014 Tingolira kaya,
  • Hymn 572 Anadza nazo mphatso zake
  • Hymn 286 ZOVUTA zoopsya ndi zosaukazi
  • Hymn 359 TADZUKA mzimu wanga ‘we,
  • Hymn 338 Imvani
  • Hymn 230 Ndisamba ndiyera,
  • Hymn 176 Mleke mdaniyo, mwimbe m’njiramo
  • Hymn 1084 “Khala mwa Ine,” munachotsa tsoka,
  • Hymn 893 Mtima wanga ndikonzera,
  • Hymn 1174 Sindinanyengedwa konse;
  • Hymn 1034 Mkristu, ulimbike
  • Hymn 104 M’mene ntchito yathatu,
  • Hymn 818 Mkhululukire,
  • Hymn 230 AMBUYANGA Yesu,
  • Hymn 1611 Nadzuka m’mandamo
  • Hymn 820 Ndife ananu,
  • Hymn 158 Mzimu, mlonge m’mtimamo
  • Hymn 524 Wokoma Mbuyathu
  • Hymn 107 Panalibe mwa abale
  • Hymn 1067 Ambuyathu, ndikhumba tsiku lija
  • Hymn 1239 Ndipo pakuima phe!
  • Hymn 1236 Mbuye ndimva leroli
  • Hymn 402 M’mtima mwangamu mlowemo,
  • Hymn 459 KALE anthu m’kholamo,
  • Hymn 108 Tikondwera ife tonse
  • Hymn 854 Timlemekeze Mlunguyu
  • Hymn 393 ZOPEREKA tiperekazi,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version