Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 23 TIIMBE nyimbo zotamanda

  1. Home   »  
  2. Hymn 23 TIIMBE nyimbo zotamanda

Hymn 23 TIIMBE nyimbo zotamanda

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 23 TIIMBE nyimbo zotamanda

 

TIIMBE nyimbo zotamanda
Mulungu wathu wabwino,
Pakuti akondana nawo
Anthu okhala padziko;
Tero natuma Mwana wake,
Wakukondedwa kalelo,
Kutiphunzitsa ife tonse
Za chikondano chakecho.

Mulungu ndiye wachifundo,
Nadzalandira onsewa
Akuulula mphulupulu
Ndi kukondana ndi Yesu
Tilondelonde njira yake
Yopapatiza yaing’ono;
Adzatilondolera ndiye
Kutifikitsa m’Mwambamo.

Pakuwoloka mtsinje wa imfa
Dzanja Mbuyathu agwira;
Tikadagwira ntchito zake
Atipatsatu korona;
Komwe kulibe masauko,
Pena misozi maliro;
Mulungu tidzamtamandira,
Inde kosalekezanso.

Post navigation

Previous: Hymn 22 MU ZONSE abale yamikani,
Next: Hymn 24 TITAME Mlungu Wakumwamba,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 766 Monga zomera zonsezo
  • Hymn 277 Mbwere nonse muone
  • Hymn 1029 Nkhawa tilibe; Yesuyo
  • Hymn 322 Walira Yesu m’dziko linoli,
  • Hymn 134 INU ansembe ngakhale mufunsa,
  • Hymn 1094 Ambuye anachoka
  • Hymn 69 KONDWERANI dzuŵa lino,
  • Hymn 475 MZINDA woyerawo
  • Hymn 1644 Popachikidwa pa Golgotapo
  • Hymn 1751 Mbuye ngwodalitsika,
  • Hymn 1455 Uthenga wa Mulungu
  • Hymn 440 ZIKOMO Ambuye wathu,
  • Hymn 1315 Ambuye ‘naitana ‘ne:
  • Hymn 748 Ndiye wa moyo wonse Mwiniyo,
  • Hymn 1541 Tionetseni tonsetu
  • Hymn 1370 Mphepo yay’kulu yakuombayo,
  • Hymn 171 M’manda munalibe
  • Hymn 1436 Inde, lero lino Yesu
  • Hymn 506 Ndikondwa kuti Yesu akonda,
  • Hymn 378 Ku madzi ake odikha
  • Hymn 226 BWENZI ndinamkomanayo
  • Hymn 802 Ndife anthu aulendo,
  • Hymn 1355 Atate, Mwana, Mzimunso,
  • Hymn 310 Tafika kwa inu mutiunikire,
  • Hymn 206 YESU, mulikundipempha
  • Hymn 839 Adani sindiopa mukalipo;
  • Hymn 203 Pamtandapo, pamtanda,
  • Hymn 273 USAFUNE chuma chokha,
  • Hymn 232 Uchita kwombola,
  • Hymn 1821 Angelo amazinga nyumba
  • Hymn 855 Aulendo amayenda
  • Hymn 10 TSOPANO linoli,
  • Hymn 101 MZIMU Woyera, mudze mumitima mwathumo,
  • Hymn 1797 Chikondi chake chindidzera
  • Hymn 136 Atumwi atummika, atumika,
  • Hymn 108 MBUYE wondipulumutsa,
  • Hymn 1674 Lambira Yesuyo,
  • Hymn 157 Mbuye, Mzimu Woyera
  • Hymn 1132 Mlungu adzandilandila,
  • Hymn 1377 Ndi amithenga akumwambako,
  • Hymn 1235 Yesu wathadi
  • Hymn 265 MUDZAZE Yesu mtima wanga ndi chikondicho,
  • Hymn 326 TSIKU Iidzafika mbale,
  • Hymn 571 Kwa ife lero anabadwa
  • Hymn 1327 Bwezatu, bwezatu,
  • Hymn 865 Pakubweradi Woyesa tidzamlaka ifetu;
  • Hymn 1193 Tsopano Mulungu
  • Hymn 7 “Mbuye Woyera! E, Woyeranokha!
  • Hymn 1076 Khalatu woyera,
  • Hymn 1623 Adzatenga anthu ake
  • Hymn 998 Anatilemba Yesu tikagwire nkhondo yake,
  • Hymn 141 Yenda iwe, yenda,
  • Hymn 903 Iwo salekana, iwo salekana,
  • Hymn 1421 Alongo ‘nu, alongo ‘nu,
  • Hymn 920 Yatha misoziyo,
  • Hymn 1313 Zindichulukirazi
  • Hymn 862 Tidza kwa Mulungu Inu, ndinu wa chifundo;
  • Hymn 1213 Mwamva Yesu m’mtimamo,
  • Hymn 19 Mbuye mtsitsimutse
  • Hymn 1503 Ndikamzindikira ninji

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version