Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 23 TIIMBE nyimbo zotamanda

  1. Home   »  
  2. Hymn 23 TIIMBE nyimbo zotamanda

Hymn 23 TIIMBE nyimbo zotamanda

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 23 TIIMBE nyimbo zotamanda

 

TIIMBE nyimbo zotamanda
Mulungu wathu wabwino,
Pakuti akondana nawo
Anthu okhala padziko;
Tero natuma Mwana wake,
Wakukondedwa kalelo,
Kutiphunzitsa ife tonse
Za chikondano chakecho.

Mulungu ndiye wachifundo,
Nadzalandira onsewa
Akuulula mphulupulu
Ndi kukondana ndi Yesu
Tilondelonde njira yake
Yopapatiza yaing’ono;
Adzatilondolera ndiye
Kutifikitsa m’Mwambamo.

Pakuwoloka mtsinje wa imfa
Dzanja Mbuyathu agwira;
Tikadagwira ntchito zake
Atipatsatu korona;
Komwe kulibe masauko,
Pena misozi maliro;
Mulungu tidzamtamandira,
Inde kosalekezanso.

Post navigation

Previous: Hymn 22 MU ZONSE abale yamikani,
Next: Hymn 24 TITAME Mlungu Wakumwamba,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 166 Yendani, Munthu Wachisoni,
  • Hymn 530 Munaneneratu mawu a moyonso
  • Hymn 211 TIDZALAKALAKA kuwonana naye,
  • Hymn 428 MBUYE mtsitsimutse
  • Hymn 377 Yehova, Mbusa wangadi,
  • Hymn 592 Kuti m’Mwambamo
  • Hymn 544 Zoopsya sitidziwapo
  • Hymn 1758 Poti Mulungu wathu
  • Hymn 165 Yendanitu m’ulemudi,
  • Hymn 814 Mutichiritse ifenso
  • Hymn 464 AKAZI anadza kwa Yesu ndi anawo,
  • Hymn 821 Aleluya!
  • Hymn 681 Ankhondo a Mulungu ‘nu, yendani m’njiramo,
  • Hymn 534 Bwerani, kondwerani,
  • Hymn 332 Perekani mtima wanu,
  • Hymn 734 Ndi mkate wanu, Yesu
  • Hymn 409 ANTHU akum’maŵa
  • Hymn 441 Tamverani, aitana:
  • Hymn 342 BWENZI lathu ndiye Yesu,
  • Hymn 470 YESU andikonda ine,
  • Hymn 554 Iye ndani pamtanda
  • Hymn 1222 Bwenzi ndimamkomanayo
  • Hymn 662 Tisaleme pakuchita zabwinozi,
  • Hymn 494 Yesu, E, ndikufunani,
  • Hymn 1043 Mbiri yake ubukitse,
  • Hymn 1798 Mukondwe anthu a Mulungu,
  • Hymn 739 Ndilibe wondithangata ‘ne ‘yi,
  • Hymn 62 AMBUYE Yesu,
  • Hymn 820 Ndife ananu,
  • Hymn 548 Kale anthu m’kholamo
  • Hymn 340 Imvani,
  • Hymn 949 Mundiwalire m’njira mwangamo,
  • Hymn 1722 Ambuye tikondweratu
  • Hymn 155 Pemphero ndiko kufuna
  • Hymn 962 Inde Mbuye, tibweradi,
  • Hymn 15 Mbuye, chifundo chanu chitigwere
  • Hymn 1653 Mulungu ali wokhulula mtimatu,
  • Hymn 725 Munafera ine kale
  • Hymn 297 Anapita nasiya
  • Hymn 1569 Mtima wodetsa mukonzere,
  • Hymn 1467 M’ulemerero mwake
  • Hymn 1308 Ndi ine, m’mtima Mwanu mbee!
  • Hymn 1105 Khala chete mtima wanga
  • Hymn 819 Lero tigone,
  • Hymn 1830 Ndiye M’busa wanga
  • Hymn 529 Zili nazotu nkhwimba zirombozo,
  • Hymn 303 MEMA nkhondoyo, wadza mdaniyo,
  • Hymn 358 MLUNGU ali muno,
  • Hymn 181 Zonse ndinakonda kale
  • Hymn 34 AMITHENGA a Mulungu,
  • Hymn 996 Leka zakuipa zako,
  • Hymn 550 Wosauka Iyedi
  • Hymn 1497 Simbani mobwereza,
  • Hymn 1268 Mundilandiretu,
  • Hymn 599 Mlengi wathu Wakuyera,
  • Hymn 1058 Chimwemwe chija chamumtima
  • Hymn 73 M’SANDIPITILIRE Yesu,
  • Hymn 1807 Chithawa m’talitali
  • Hymn 1426 Wina panalibe
  • Hymn 13 Mtiwerengere m’Mwamba ndi oyera;

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version