Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 22 MU ZONSE abale yamikani,

  1. Home   »  
  2. Hymn 22 MU ZONSE abale yamikani,

Hymn 22 MU ZONSE abale yamikani,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 22 MU ZONSE abale yamikani,

 

MU ZONSE abale yamikani,
Mulungu ndi wamkulu,
Adziwa kupatsa anthu ake,
Zomwe iwo akuzisowa.

Akhrisitu pamavuto tiyeni timulemekeze,
Pamtendere tiyeni timulemekeze.
Maso ake ali pa anthu,
Okhala m’dziko lapansi.

Mu zonse abale yamikani,
Mulungu ndi wamkulu,
Adziwa kuveka anthu ake,
Ngakhale nyama zakuthengo.

Mu zonse abale yamikani,
Mulungu ndi wamkulu,
Adziwa kupatsa mphatso zake,
Ngakhalenso kwa tiŵanato.

Post navigation

Previous: Hymn 21 KUZANI Mlungu m’Mwambamo,
Next: Hymn 23 TIIMBE nyimbo zotamanda

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 113 Likalira llipengalo,
  • Hymn 417 M’BWERE Mlungu Mbuye wathu,
  • Hymn 37 YESU analikhanda
  • Hymn 1206 Ndidzakukondani
  • Hymn 1272 Muyambe ntchito yanuyi,
  • Hymn 1115 M’munda wa Mbuyako
  • Hymn 1194 Padziko lapansi
  • Hymn 1473 Anasenza pa bwanji uchimo wonsewo,
  • Hymn 1039 Usafune chuma chokha,
  • Hymn 969 Akathira nsembe
  • Hymn 644 M’wasunge, m’wayendetse
  • Hymn 1679 Tiyamike Dzina lake, Aleluya,
  • Hymn 1719 Ku Mzinda wakuyerawo
  • Hymn 262 Tumphatumpha moyo wanga,
  • Hymn 1084 “Khala mwa Ine,” munachotsa tsoka,
  • Hymn 790 Zimbalame zonsezi
  • Hymn 288 HAYA! ’nzanga taonani
  • Hymn 22 Mbuye mtsitsimutse!
  • Hymn 1819 Pokondwa ndi poona bvuto
  • Hymn 225 Yesu akhazika
  • Hymn 1442 Khulupira mawu onse
  • Hymn 794 Ambuye, tasonkhana
  • Hymn 197 Tidzatama Atate wathu
  • Hymn 475 Mbuye ndikhaletu
  • Hymn 224 LINDIKOMERA dzina la Ambuye Yesu wanga,
  • Hymn 1707 Andiferatu ‘Ye,
  • Hymn 97 TIYAMIKE Mlunguyo,
  • Hymn 368 MULUNGU wanga, Dzuŵatu
  • Hymn 221 A! CHIKONDI chopambana,
  • Hymn 421 Ine ndine mlendo
  • Hymn 292 Ndi makutu athu awanso nganu,
  • Hymn 435 ANAKWATIRA kale
  • Hymn 395 Usiku uno mutisungedi,
  • Hymn 199 NDINASOKERA kutali,
  • Hymn 450 YESU, munditsogoza
  • Hymn 58 Titasokera tinabwerera,
  • Hymn 1587 Nditama Mlungu m’mtimamo,
  • Hymn 424 MTIDZUTSE, Mbuyetu,
  • Hymn 1657 Mbuye, mutsaganebe
  • Hymn 1685 Nla Mlungu dzuwali;
  • Hymn 854 Timlemekeze Mlunguyu
  • Hymn 1741 Yesu munalaswa m’mtima,
  • Hymn 309 ANA akumwamba ndife,
  • Hymn 652 Munene Mbuye ‘nenetu,
  • Hymn 1670 Bwenzi ndiye wakufera,
  • Hymn 1630 Anthu anu amafoka,
  • Hymn 677 Ponse padakhala mdima
  • Hymn 268 Potuluka m’mudzimo
  • Hymn 1666 Yesu, ndinutu chitsime
  • Hymn 1173 Sindinanyengedwa konse
  • Hymn 968 Mzimu wakuipa
  • Hymn 594 Monga may’ asusuza
  • Hymn 1485 Unachimwachimwa ndithu,
  • Hymn 116 MBUYE, Mawu anu
  • Hymn 145 MBIRI yakale lomwe
  • Hymn 1557 M’phunzitsi, ndinu mudziwitse ine
  • Hymn 154 SING’ANGA ‘mkulu ndiye Yesu,
  • Hymn 738 Mommuno, Mbuye, mkate wanuwu,
  • Hymn 1414 Zonse zinathedwadi;
  • Hymn 1198 Mabala ake m’manja

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version