Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 199 NDINASOKERA kutali,

  1. Home   »  
  2. Hymn 199 NDINASOKERA kutali,

Hymn 199 NDINASOKERA kutali,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 199 NDINASOKERA kutali,

 

NDINASOKERA kutali,
Ndinadya ndi nguluwe,
Ndinakhala mu zoipa,
Chifukwa ndinachimwa.

Mmene ndafika
kwa ‘tate,
Nandikonzeratu phwando;
“Tidye tisekere naye,
Mwanayu anasowa.”

Koma mkulu wanga ndiye,
Sanandirandiretu;
Sanafune tate wanga,
Andikhululukire.

Ambuye amayitana,
Anthu onse ochimwa;
Kuti adzetu kwa Iye,
Kumene kuli moyo.

Post navigation

Previous: Hymn 198 CHITSIMECHO cha mwaziwo
Next: Hymn 200 YESU mundimve, ndikuliratu,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1062 Mkatero ndidzayenda m’njira
  • Hymn 214 Msanga adzachitseka chitseko,
  • Hymn 361 AMBUYE munapatsa tsiku
  • Hymn 1762 Anamva abusa omwe
  • Hymn 1461 Sing’anga ‘mkulu ndiye Yesu,
  • Hymn 270 Zoopsya zopambana
  • Hymn 1841 Kumadzi kuli njiratu andiyendetsa bwino,
  • Hymn 1655 Mbuye Yesu,
  • Hymn 231 Mwazi wa Yesu wokondwa
  • Hymn 174 YESU wathu Mbuyeyo
  • Hymn 1273 Ndasiya zonse ndi Yesu kalelo,
  • Hymn 252 M’dziko lino chimwemwecho
  • Hymn 1681 Mphamvu za imfa ndi za Satana
  • Hymn 240 YESU ndiye Mbuye wanga,
  • Hymn 163 Mukonda nyimbo za ana,
  • Hymn 29 Tamandani Mbuye,
  • Hymn 876 Mtidzutse, Mbuyetu,
  • Hymn 499 ‘Nafera Mbuye wanga
  • Hymn 411 Yesu adza kukundika
  • Hymn 114 Ndine Mbusayo wabwino,
  • Hymn 1545 Mundilimbitse m’mtima
  • Hymn 97 Maso ndi maso ndi Kristu,
  • Hymn 997 Mawu ake atipatsa
  • Hymn 1156 Imfa ndi manda sitiopa ‘yi,
  • Hymn 64 Mantha, nkhawa, ndi chisoni
  • Hymn 189 Koma Iye wandipeza;
  • Hymn 511 Ntchito zake zatha,
  • Hymn 1303 Aa! Mulungu wanga,
  • Hymn 1073 Mwa ine myatse moto wanu wakuyera mbuu,
  • Hymn 980 Tiyeni ku nkhondo iyi,
  • Hymn 1046 Ndiyere mbuu! E, ndiyere mbuu!
  • Hymn 1488 Musawalole mawuwo
  • Hymn 32 YENDANI, Mfumu yamtendere
  • Hello world!
  • Hymn 5 ATATE wa Kumwambako,
  • Hymn 1178 Mawu omwewo, nyimbo yomweyi,
  • Hymn 1032 Ntchito za Yesu gwira
  • Hymn 75 Ndiperekatu
  • Hymn 1352 Atate wa Kumwambako,
  • Hymn 461 ANA inu, myamikeni
  • Hymn 353 ATATE Wamkulu ndi Wamphamvu zonse,
  • Hymn 21 KUZANI Mlungu m’Mwambamo,
  • Hymn 1017 Tisasungaluke ‘yi,
  • Hymn 965 Mundiuze, aulendo,
  • Hymn 1759 Powalitsira omwe
  • Hymn 1003 Kanganani nkhondo yanu
  • Hymn 633 Tikasokera m’njira mutilondolere ndithu,
  • Hymn 216 NDISAUKA, ndinachimwa,
  • Hymn 327 NTCHITO yonse yakeyo
  • Hymn 495 MLUNGU dalitsani Malaŵi,
  • Hymn 183 Mlemekeze, bukitsani,
  • Hymn 738 Mommuno, Mbuye, mkate wanuwu,
  • Hymn 722 Anu Mbuye ndifetu!
  • Hymn 1203 Zambiri zangazo
  • Hymn 155 UTHENGA wa Mulungu
  • Hymn 859 Pakufika tsidya lija,
  • Hymn 256 NGATI mtima sumakonda
  • Hymn 381 MONGA zomera zonsezo
  • Hymn 711 Ife tonse tichenjere
  • Hymn 127 POLUMIDWA ndi njokazo,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version