Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 333 M’DZIKO lino tikhalamo

  1. Home   »  
  2. Hymn 333 M’DZIKO lino tikhalamo

Hymn 333 M’DZIKO lino tikhalamo

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 333 M’DZIKO lino tikhalamo

 

M’DZIKO lino tikhalamo
Utibvuta moyo,
Koma dziko la mtendere
Lili kwa Mulungu.

Watitsogolera Mbuye,
Komwe kwa Atate,
Ndimo tidzatsata naye
Moyo wathu wonse.

Ndi tsopano tilindira
M`dziko lathu lino;
Ntchito atipatsa Mlungu,
Tizigwira bwino.

Ngati zakuipa zathu
Zikatisautsa,
Tithaŵire kwa Mbuyathu,
Atipulumutsa.

Timpemphere kutipatsa
Mtima watsopano,
Kutithandizira kunka
Paulendo uno.

Post navigation

Previous: Hymn 332 NDIKONDWA kuganizirabe
Next: Hymn 334 KULI dziko labwino M’mwamba,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1753 Adzatipulumutsa
  • Hymn 360 Muli ndi ludzu, idzani
  • Hymn 995 Taya zako zochenjera,
  • Hymn 377 Yehova, Mbusa wangadi,
  • Hymn 1736 “Senzani mtanda wanuwu.”
  • Hymn 1207 Poyambapo ndakondwadi,
  • Hymn 923 Dothili kudothilo,
  • Hymn 1673 Lambira Yesuyo
  • Hymn 61 A! MUTU wakuyera,
  • Hymn 23 TIIMBE nyimbo zotamanda
  • Hymn 1214 Mwamva Mzimu wakewo,
  • Hymn 808 Atipsinjadi masoka,
  • Hymn 444 YEMWE afesa nalira,
  • Hymn 479 Munanena mulandira
  • Hymn 113 Likalira llipengalo,
  • Hymn 31 Tamandani mbuye,
  • Hymn 1512 Cholimbitsa mtima ndi
  • Hymn 1658 Idza wolema,
  • Hymn 426 Mpulumutsi Yesu,
  • Hymn 1365 Zozizwa za m’dziko,
  • Hymn 1005 Mdani adza nazo mphamvu,
  • Hymn 15 Mbuye, chifundo chanu chitigwere
  • Hymn 371 Mulungu, anthu ‘fe
  • Hymn 1015 Mbuye, mwatiuza ‘fe
  • Hymn 1671 Akhululukira iwe,
  • Hymn 590 Mbuye, Msungi ‘Nu,
  • Hymn 1398 Nditama mphamvu yake
  • Hymn 202 Timpemphere kutipatsa
  • Hymn 473 YESU wa Kumwamba,
  • Hymn 1542 Titamire nthawi zonse
  • Hymn 1243 Kodi mayi wobereka
  • Hymn 1566 Mufike monga ngati mphepo yokokomayo,
  • Hymn 1370 Mphepo yay’kulu yakuombayo,
  • Hymn 814 Mutichiritse ifenso
  • Hymn 497 TILIKUIMBA nyimbo yomweyi,
  • Hymn 532 Ukondwere mtima wanga
  • Hymn 1031 Gwira zintchito zako,
  • Hymn 1538 Mzimu Woyera, mudzetu
  • Hymn 1120 Ndifuna Yesuyo
  • Hymn 943 Onse aliko takonda kalelo,
  • Hymn 54 MUNTHU wazisoniyo,
  • Hymn 229 POYAMBAPO ndakondwadi.
  • Hymn 185 NDINE Mbusayo wabwino,
  • Hymn 1421 Alongo ‘nu, alongo ‘nu,
  • Hymn 1184 Akondwerera nthawiyi
  • Hymn 1098 M’mene mantha andigwira,
  • Hymn 1416 Mbuye wanga ndilikumva,
  • Hymn 190 CHITETEZO chachikulu
  • Hymn 22 MU ZONSE abale yamikani,
  • Hymn 32 Tamandani Mbuye,
  • Hymn 1193 Tsopano Mulungu
  • Hymn 1833 Podwala ine pobvutidwa Andisamalira;
  • Hymn 1806 Nowayo anatuma,
  • Hymn 456 ANA inu, ana inu,
  • Hymn 337 PADZIKO pano tikhalira M’moyo wosauka;
  • Hymn 51 PANTHAWI yakufa Ambuye,
  • Hymn 131 MAWU a Mulungu awa,
  • Hymn 1125 Ndifuna Inu, Yesu,
  • Hymn 556 Ndani pachimpandocho
  • Hymn 396 Mtitsogolere nthawi zonsezo;

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version