Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 312 NDIMAYENDA paulendo

  1. Home   »  
  2. Hymn 312 NDIMAYENDA paulendo

Hymn 312 NDIMAYENDA paulendo

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 312 NDIMAYENDA paulendo

 

NDIMAYENDA paulendo
Ndi yaminga njira yake;
Tsoka ndikapeza, koma
Ndinka kwa Atate;
Pena m’mtima mwanga mwada,
Pena andibvuta ‘dani,
Ndikatenga nkhaŵa, mantha,
Amadziŵako.

Ichi chindisangalatsa
M’mene nkhondo indigwira,
M’mene nsoni zazikulu
Zimanditsatira;
Mtima ukhazika m’mene
Kwathu kuja ndikumbuka
Kuti Mlungu ali ndine,
Andisungako.

Mbuye andipeza lero,
Andikonda, andisunga;
Adzapitikitsa mdani
Akamandibvuta.
E, ulendo wanga utha,
Tsono ine ndimwalira;
M’mene ndidzafika kwawo
And’landirako.

Komwe ndi chimwemwe ine
N’dzaonana ndi Atate,
N’dzagwadira ndi kumtama,
Amandikondabe.
Sakandisautsa kanthu
M’dziko lija lakukoma;
Adzandidalitsa Yesu,
Ndidzakondwako.

Post navigation

Previous: Hymn 311 VALANI zida tizinka kwathuko,
Next: Hymn 313 MUNDIŴALIRE m’njira mwangamo,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1334 Walandira inetu
  • Hymn 162 PENYETSETSA Yesu,
  • Hymn 351 CHIYEMBEKEZO changacho,
  • Hymn 1556 Mzimu Woyera, mudzetu kwa ine,
  • Hymn 1375 Ndi anamwali obvekedwa mbuu!
  • Hymn 302 NDIDZE pafupi pa
  • Hymn 1148 Ndiimba mumtima mokondwa
  • Hymn 140 NDINAMIRA m’machimo, wosaonekanso,
  • Hymn 1678 Yesu nkana saoneka, Aleluya,
  • Hymn 39 Poyang’ana ena ndi ndalamatu,
  • Hymn 1278 Kuti muyeretsa mtima ndibvomeratu;
  • Hymn 432 Ulendo ungoyamba
  • Hymn 39 MUNASIYATU dziko lanulo,
  • Hymn 196 Tidzimba komweko nyimbo
  • Hymn 317 Zambiri zagona m’kholamo,
  • Hymn 1812 Kuzani Mlungu m’Mwambamo,
  • Hymn 12 NDITAMATU Ambuyangayu,
  • Hymn 1033 Mkristu gwiratu ntchito
  • Hymn 479 ANYAMATA inutu,
  • Hymn 405 M’mtima mwangamu mlowemo,
  • Hymn 973 Tigwire nkhondo yomwe
  • Hymn 1713 Zochimwa zanga zonsezo
  • Hymn 170 YESU ponong’oneza, idzanitu;
  • Hymn 284 MAVUTO ndi ambiri,
  • Hymn 1285 Yesu, n’kupatsani zonse,
  • Hymn 469 NDIKONDA mbiri yomwe
  • Hymn 854 Timlemekeze Mlunguyu
  • Hymn 1336 Mwamva mawu a Mulungu;
  • Hymn 22 Mbuye mtsitsimutse!
  • Hymn 129 WODALA ndiye munthuyo,
  • Hymn 363 ATATE ndiyamika,
  • Hymn 1599 Inde, ndifuna kumvatu
  • Hymn 1281 Ndikhulupirira, Yesu, mndibvomereko;
  • Hymn 875 Mtidzutse, Mbuyetu,
  • Hymn 1175 Sindinanyengedwa konse,
  • Hymn 245 KHALANI duu! Ambuye adzatu;
  • Hymn 200 YESU mundimve, ndikuliratu,
  • Hymn 55 Ambiri tikondwera mwa Yesu,
  • Hymn 1695 Pokumbukira mtandawo
  • Hymn 1074 Mubweretu nomwe ‘Nu munatsika kalelo;
  • Hymn 81 Imva mawu akewo,
  • Hymn 908 Ndikonda kuganizirabe
  • Hymn 698 Polenga dzikoli,
  • Hymn 691 Akukhala kunja,
  • Hymn 1706 Pamutu minga kwe!
  • Hymn 574 A! Yesu Mbuye wakuyera,
  • Hymn 192 ZAKEYU mkulu wa misonkho,
  • Hymn 1299 Mzimu mndipatseko,
  • Hymn 572 Anadza nazo mphatso zake
  • Hymn 560 Kale m’mzinda wachifumu
  • Hymn 419 ANYAMATA a Mulungu,
  • Hymn 519 Mverani, aimba anawo,
  • Hymn 24 “Ndakupeza womanga,
  • Hymn 1227 Ndiyamika Mbuye wanga
  • Hymn 1276 Ndikhulupirira, Yesu, Inu nokhadi
  • Hymn 774 Tibatizidweko,
  • Hymn 1350 Mvera Yesu, mvera Yesu,
  • Hymn 617 Nthawi yina Mbuyeyu
  • Hymn 47 Anthu m’maiko onse
  • Hymn 1440 Yesu alindira,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version