Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 282 INU muli mehere,

  1. Home   »  
  2. Hymn 282 INU muli mehere,

Hymn 282 INU muli mehere,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 282 INU muli mehere,

 

INU muli mehere,
Wa dziko lapansi;
Ukasukuluka,
Sungakolerenso,

Yang’anani bwino,
Muyende m’njirayo;
Kuti mungagwetu,
M’zovuta za dziko.

Pamenepo sungakwanirenso kanthu,
Koma kuti ukaponyedwetu kunja.

Ndinu kuunika,
Kwa dziko lapansi;
Mudzi wapaphiri
Sungabisiketu.

Sungayatse nyali,
N’kuyivundikira;
Koma uyika pachoikapo chake.

Ndipo iwunikira onse
m’nyumbamo;
Chomwecho inu
muunikire dziko.

Kuti pakuwona,
Ntchitozo zabwino;
Alemekezedwe,
Mlungu ‘Tate wanu.

Post navigation

Previous: Hymn 281 MBUYE, mwatiuza ’fe
Next: Hymn 283 AMBUYE m’chipululu,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 423 MUNENE Mbuye, ’nenetu,
  • Hymn 1 NDINU wakuyera! Wamphamvu zonse.
  • Hymn 413 Yesu ndiye Bwenzi lathu,
  • Hymn 565 Koma sitimpenya m’khola
  • Hymn 1649 Kutenga inetu, kutenga inetu
  • Hymn 1355 Atate, Mwana, Mzimunso,
  • Hymn 864 Ndi chikondi mtithandize kuigwira nkhondoyi;
  • Hymn 588 Mlungu, Inutu,
  • Hymn 635 Tipempha madalitso ano mpatse ife tonse;
  • Hymn 1269 Ndifoka ndi zoipazo,
  • Hymn 138 Kumva ulikumva, ulikumva,
  • Hymn 1467 M’ulemerero mwake
  • Hymn 1101 Ngati mtima sumakonda
  • Hymn 151 Inde, Yesu, mulandira,
  • Hymn 1808 Kutuma wabwereza,
  • Hymn 1604 Yesu, dzina lakukonda,
  • Hymn 14 Tsiku ndi tsiku timalemekeza;
  • Hymn 1306 Ndi ine ndasaukadi,
  • Hymn 417 M’BWERE Mlungu Mbuye wathu,
  • Hymn 125 Aliponso mabvuto, ena ndi oipa;
  • Hymn 1473 Anasenza pa bwanji uchimo wonsewo,
  • Hymn 488 M’MANJA a Yesu wanga
  • Hymn 1672 Lambira Mfumuyo,
  • Hymn 175 Mlungu mverani, mphamvu patseni,
  • Hymn 261 M’NDIYANDIKITSE nanu Yesu,
  • Hymn 408 ABALE nonse mulindiranji?
  • Hymn 341 PAKUPEMPHERATU
  • Hymn 775 Mwa anthu onsewo
  • Hymn 1282 Ndilinkudza kwa Ambuye,
  • Hymn 343 ZOKOMA ndithu nthaŵizi
  • Hymn 1733 Adzabwera Iyenso
  • Hymn 255 Pakuona imfayo
  • Hymn 781 Tatsegukani inutu,
  • Hymn 1704 Zintchito zakezi
  • Hymn 1633 Adzabwera, adzabwera;
  • Hymn 1834 Chisomo ndi zokoma zake sizileka konse;
  • Hymn 1741 Yesu munalaswa m’mtima,
  • Hymn 1178 Mawu omwewo, nyimbo yomweyi,
  • Hymn 33 OWONADI mtima,
  • Hymn 1768 Ndiye wamphamvu zonse
  • Hymn 480 TIANA ife tingofoka,
  • Hymn 295 Kubadwa kwa Yesu
  • Hymn 235 ADALITSIKA munthuyo,
  • Hymn 1560 Mthandizi ndinu, mndithangate ine
  • Hymn 59 Tinachoka munjira ya imfa,
  • Hymn 229 Woba wakufa ‘napenya
  • Hymn 659 Anthu ali m’mdima akuitanitsa
  • Hymn 412 MOYO uli pafupi,
  • Hymn 691 Akukhala kunja,
  • Hymn 869 Anatipatsa Mawu onse olimbitsa mtima;
  • Hymn 854 Timlemekeze Mlunguyu
  • Hymn 1032 Ntchito za Yesu gwira
  • Hymn 1191 Ambuyanga Yesu
  • Hymn 398 Lero lino mwatipatsa
  • Hymn 1401 Imvani mawu ake, idzanitu,
  • Hymn 582 A! Mulungu,
  • Hymn 577 Adagona m’ndyeromo
  • Hymn 816 Mdima wafika,
  • Hymn 1452 Inu akutopawo,
  • Hymn 391 Mufafanize m’bukumo

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version