Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 161 LERO lino mbale wanga,

  1. Home   »  
  2. Hymn 161 LERO lino mbale wanga,

Hymn 161 LERO lino mbale wanga,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 161 LERO lino mbale wanga,

 

LERO lino mbale wanga,
Ndilo tsiku lakukoma;
Talandira Mpulumutsi,
Mmene ali kuyitana.

Lero lino mbale wanga,
Usazengereze ayi;
Ngati ulandira Yesu,
Lero, udzachita mwayi.

Lero lino ndi labwino,
Moyo wako uli nawo;
Pena mawa umwalira,
Udzatani mlandu wako?

Lero lino mbale wanga,
Lapa mtima, lapa tchimo;
Yesu adzakulandira,
Ukam’pempha lero lino.

Ndiwe mlendo lero lino,
Myera ndikupempha iwe:
Yesu Mwana wa Mulungu,
Akufuna ndithu iwe.

Inde, lero lino Yesu,
Ayitana inu nonse;
Landirani Mpulumutsi,
Musazengereze konse.

Post navigation

Previous: Hymn 160 MADALITSO ngati mvumbi,
Next: Hymn 162 PENYETSETSA Yesu,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 227 Kasupe ali wodzaza
  • Hymn 789 Ndi lokoma m’Mwambamo,
  • Hymn 278 TITHAŴIRENJI ifetu
  • Hymn 993 Pakumalizidwa
  • Hymn 1780 Titame Mlungu Wakumwamba,
  • Hymn 848 Mudze, mlowe m’mtimamu,
  • Hymn 101 MZIMU Woyera, mudze mumitima mwathumo,
  • Hymn 325 KODI uli ndi chisoni
  • Hymn 1622 Anthu onse amlambire
  • Hymn 987 Ambuye wa Kumwamba,
  • Hymn 606 Dzinja lokondweretsa lafikanso,litapumatu,
  • Hymn 542 Kuli kaphiri m’talimo
  • Hymn 453 A! MULUNGU
  • Hymn 1357 Mlemekeze, anakonda
  • Hymn 32 Tamandani Mbuye,
  • Hymn 252 M’dziko lino chimwemwecho
  • Hymn 1842 Pabande lolunjika andilondolera njira;
  • Hymn 329 MUMZINDA wa Mulungu
  • Hymn 6 Nanu akukuzani amithenga,
  • Hymn 1309 Ndi inetu ndidziwedi
  • Hymn 932 Munabvala thupi lathu,
  • Hymn 1231 Nlokoma dzinalo la Yesu, ndilo thanthwe langa,
  • Hymn 390 Lalowa dzuwa, kwada bii!
  • Hymn 45 IFE timakufunani
  • Hymn 1364 Uzani zamphamvu,
  • Hymn 221 Yesu and’itana,
  • Hymn 1215 Ndimkonde Kristuyo,
  • Hymn 592 Kuti m’Mwambamo
  • Hymn 1067 Ambuyathu, ndikhumba tsiku lija
  • Hymn 241 MTENDERE uli m’mtima mwathumu,
  • Hymn 363 ATATE ndiyamika,
  • Hymn 851 E, nthawi ya mamawayi
  • Hymn 1036 Mtima wakufatsa
  • Hymn 1168 Aleluya, muyenera!
  • Hymn 174 YESU wathu Mbuyeyo
  • Hymn 1430 Ndipo pakulowa
  • Hymn 968 Mzimu wakuipa
  • Hymn 902 Ndikondwa kuganizabe
  • Hymn 659 Anthu ali m’mdima akuitanitsa
  • Hymn 301 MBUYE, ndapangana
  • Hymn 750 Yesu Mbuyathu, Inu nomwe ‘Nu,
  • Hymn 736 Mndidyetse m’chipululu
  • Hymn 1807 Chithawa m’talitali
  • Hymn 1473 Anasenza pa bwanji uchimo wonsewo,
  • Hymn 194 Kuli dziko labwino m’Mwamba
  • Hymn 1779 M’dzikomo Ambuye
  • Hymn 1569 Mtima wodetsa mukonzere,
  • Hymn 1493 Mbiri yakalelomwe
  • Hymn 319 NDIDZATANI ine,
  • Hymn 69 KONDWERANI dzuŵa lino,
  • Hymn 125 Aliponso mabvuto, ena ndi oipa;
  • Hymn 1554 Mpume pa inetu, Mpweya wa Mulungu,
  • Hymn 213 INE ndili ndi manyazi
  • Hymn 1370 Mphepo yay’kulu yakuombayo,
  • Hymn 1389 Tithawire kwa Mulungu,
  • Hymn 554 Iye ndani pamtanda
  • Hymn 122 Musadziunjikire chuma cha padziko,
  • Hymn 492 DZIKO lilipolo
  • Hymn 906 Mulibe zoipa m’Dzikolo,
  • Hymn 174 Haya, anzathu, itilinda nkhondo;

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version