Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 111 YAKOBO mwanatu wachinyengoyo;

  1. Home   »  
  2. Hymn 111 YAKOBO mwanatu wachinyengoyo;

Hymn 111 YAKOBO mwanatu wachinyengoyo;

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 111 YAKOBO mwanatu wachinyengoyo;

 

YAKOBO mwanatu wachinyengoyo;
Wanyenga bambo ake
Kuti, “Inetu ndinetu
Esau mwana wanu.”

Esau analira, “abambo
Inu, abambo anga,
Ndabwera nayo nyama,
Mulandire, mudye.”

Thupi ndi Esau, koma mawuwo,
Ngatitu a Yakobo;
“Bwera mwana wanga,
Bwera pafupi n’kusisite.”

Ndapezatu bwenzi latsopanolo,
Ndi Yesu Mpulumutsi;
Yemwe angathe, kuchotsa,
Machimo anga onse.

Machimo andizunza ine;
Mtima mwangamu inedi,
Ndifuna Inu Mbuye,
Mulowe m’mtima mwanga.

Post navigation

Previous: Hymn 110 MZIMU ndi mtogoleri
Next: Hymn 112 ELISA mneneri,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 241 Munadzera ndi Mawu a moyo
  • Hymn 1683 Nsinga za imfa Iye ‘nadula,
  • Hymn 138 SANGALATSA akusowa, masiku alikutha,
  • Hymn 713 Ambuye, Mwini zonsezi,
  • Hymn 572 Anadza nazo mphatso zake
  • Hymn 134 INU ansembe ngakhale mufunsa,
  • Hymn 686 Imbadi za Iyeyo,
  • Hymn 243 KONDWANI nonsenu,
  • Hymn 1422 Abwenzi ‘nu, abwenzi ‘nu,
  • Hymn 860 Nthawi yina adzadzuka
  • Hymn 254 PAMENE ndisawuka,
  • Hymn 1815 Choposa nalo thupilo,
  • Hymn 69 KONDWERANI dzuŵa lino,
  • Hymn 1462 Dzina la Yesu ndi lokoma,
  • Hymn 281 MBUYE, mwatiuza ’fe
  • Hymn 199 Watitsogolera Mbuye,
  • Hymn 350 MBUYE ndayima pano,
  • Hymn 1820 Kwezani nane Ambuyathu,
  • Hymn 1324 M’moyo uno kunsiku
  • Hymn 275 NTHAWI yathu yafikatu,
  • Hymn 1022 Mbuye, nditsate bwanjiko?
  • Hymn 500 Mbuye Yesu andisunga
  • Hymn 541 Ana inu, yamikani
  • Hymn 773 Mtsinje woyerawo
  • Hymn 1694 Timwimbire Mlungu wathu, Aleluya
  • Hymn 123 Koma mudzisungire chuma cha Kumwamba
  • Hymn 189 Koma Iye wandipeza;
  • Hymn 1678 Yesu nkana saoneka, Aleluya,
  • Hymn 518 Ana a Yerusalemu
  • Hymn 21 Mbuye mtsitsimutse!
  • Hymn 272 Ankhondowo poona
  • Hymn 246 Pajapo ndipenya
  • Hymn 601 Akaona masautso
  • Hymn 544 Zoopsya sitidziwapo
  • Hymn 1040 Ukafuna kulemera,
  • Hymn 441 MBUYE, tikuthokozani,
  • Hymn 1700 Ambuye Mwini moyo,
  • Hymn 105 IDZANI, Mzimu Inu,
  • Hymn 1092 Ndimamva njala kuno, Yesu,
  • Hymn 1298 Ndikhulupira ‘Nu,
  • Hymn 245 Ngakhale kuthengo
  • Hymn 966 Kodi inu, aulendo,
  • Hymn 247 Tsono poukanso
  • Hymn 1771 Iye natsitsa kunsi
  • Hymn 288 HAYA! ’nzanga taonani
  • Hymn 1157 Mtendere wapambana m’Mwambamo
  • Hymn 913 Kulibe gombe, nyanja,
  • Hymn 770 Atate, muwapenye
  • Hymn 1360 Ndi Aleluya imbirani
  • Hymn 244 Ndidze pafupi pa
  • Hymn 1653 Mulungu ali wokhulula mtimatu,
  • Hymn 565 Koma sitimpenya m’khola
  • Hymn 104 M’mene ntchito yathatu,
  • Hymn 38 Kodi mubvutidwa naye katundu?
  • Hymn 422 DZIKO lonse lapansi,
  • Hymn 1857 Ndinagona mwa zoipa,
  • Hymn 24 “Ndakupeza womanga,
  • Hymn 78 ALINKUDZA wansoni Munthu,
  • Hymn 1552 Mpume pa inetu, Mpweya wa Mulungu,
  • Hymn 214 Msanga adzachitseka chitseko,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version