Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 111 YAKOBO mwanatu wachinyengoyo;

  1. Home   »  
  2. Hymn 111 YAKOBO mwanatu wachinyengoyo;

Hymn 111 YAKOBO mwanatu wachinyengoyo;

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 111 YAKOBO mwanatu wachinyengoyo;

 

YAKOBO mwanatu wachinyengoyo;
Wanyenga bambo ake
Kuti, “Inetu ndinetu
Esau mwana wanu.”

Esau analira, “abambo
Inu, abambo anga,
Ndabwera nayo nyama,
Mulandire, mudye.”

Thupi ndi Esau, koma mawuwo,
Ngatitu a Yakobo;
“Bwera mwana wanga,
Bwera pafupi n’kusisite.”

Ndapezatu bwenzi latsopanolo,
Ndi Yesu Mpulumutsi;
Yemwe angathe, kuchotsa,
Machimo anga onse.

Machimo andizunza ine;
Mtima mwangamu inedi,
Ndifuna Inu Mbuye,
Mulowe m’mtima mwanga.

Post navigation

Previous: Hymn 110 MZIMU ndi mtogoleri
Next: Hymn 112 ELISA mneneri,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 658 Ndichitireni, Mbuye ‘ne,
  • Hymn 794 Ambuye, tasonkhana
  • Hymn 1715 Kodi misozi itisowa,
  • Hymn 273 USAFUNE chuma chokha,
  • Hymn 153 NDAKUMANA ndi bwenzi lokomalo,
  • Hymn 715 Mwapatsa Mwana wanu, ndi
  • Hymn 416 Woyenera ndani kunka
  • Hymn 1230 Lichiza mzimu wophwetekwa ukakhale bata,
  • Hymn 425 AKRISTU ndi abale, tiziyenderana tonse,
  • Hymn 1100 Inde wakukonda ndinu;
  • Hymn 938 A! Yesu Bwenzi langa
  • Hymn 764 “Chikho cha mwazi wangachi
  • Hymn 625 Chaka chino mutipatse
  • Hymn 189 MLENDO ali pakhomo,
  • Hymn 469 NDIKONDA mbiri yomwe
  • Hymn 1812 Kuzani Mlungu m’Mwambamo,
  • Hymn 1138 Masiku onse m’mtima mwanga
  • Hymn 552 Analira ndaniyo
  • Hymn 362 MUKHALE ndine, dzuŵalo laloŵa,
  • Hymn 497 TILIKUIMBA nyimbo yomweyi,
  • Hymn 309 ANA akumwamba ndife,
  • Hymn 1582 Konda dzinalo la Yesu
  • Hymn 298 “Tadodoma, abusa,
  • Hymn 22 MU ZONSE abale yamikani,
  • Hymn 584 Ndi angelo,
  • Hymn 312 Atate, mupatse zomwe tapemphazi,
  • Hymn 844 Pogona ife, amadzuka
  • Hymn 707 Dalitseni, Mbuye, zonse
  • Hymn 1247 A Chikondi chopambana,
  • Hymn 1360 Ndi Aleluya imbirani
  • Hymn 1188 Akumangidwa ndi mzimuwo,
  • Hymn 581 Mtiphunzitse bwinotu,
  • Hymn 463 MNANDIDZERA, Ambuye,
  • Hymn 1362 Mulungu wathu tiyamika,
  • Hymn 1294 Wakuba uja nachiona,
  • Hymn 76 Ndipereka zanga zonse
  • Hymn 222 Ndilikudzatu,
  • Hymn 688 Anthu akum’mawa
  • Hymn 1062 Mkatero ndidzayenda m’njira
  • Hymn 1404 “Undipatsetu
  • Hymn 1388 Tiimbire Mlungu wathu
  • Hymn 59 Tinachoka munjira ya imfa,
  • Hymn 235 ADALITSIKA munthuyo,
  • Hymn 207 AMBUYE ndamvatu Mawu anu,
  • Hymn 34 AMITHENGA a Mulungu,
  • Hymn 470 YESU andikonda ine,
  • Hymn 380 Ndipyola kodi chikhwawa
  • Hymn 1140 Paja athira Yesutu
  • Hymn 102 MZIMU Woyera, mudzetu kwa ine
  • Hymn 210 Nyumba yodyera ilikudzaza;
  • Hymn 223 Ndafoka, ndaipa,
  • Hymn 603 Mzimu wanu Wakuyera,
  • Hymn 1369 Paphiri paja papakulupo,
  • Hymn 1783 Tinasokera ngati nkhosa,
  • Hymn 1065 Ngakhale Satana andizunza ‘ne,
  • Hymn 253 YESU ndinutu wanga m’njira zonse,
  • Hymn 1520 Mbuye, Mawu anu
  • Hymn 1024 Anasauka Mbuyeyo,
  • Hymn 390 A! YESU, ndapangana
  • Hymn 299 TIYENI, Akristu inu,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version