Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 79 PAKWITANA Mbuye wanga

  1. Home   »  
  2. Hymn 79 PAKWITANA Mbuye wanga

Hymn 79 PAKWITANA Mbuye wanga

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 79 PAKWITANA Mbuye wanga

 

PAKWITANA Mbuye wanga
Potsiriza dzikoli,
Pakufika tsiku la kuŵalalo,
Posonkhana akumvera,
Pakuona Yesuyo,
Ndidzakondwerera naye komweko.

Pakuyiitana Mbuye wanga,
Pakuyiitana Mbuye wanga,
Pakuyiitana Mbuye wanga,
Ndidzakondwerera naye komweko.

Potuluka m’manda mwawo
Anthu ake onsewo,
Tidzasanganatu nawo nthaŵiyo.
Pakuluka osankhidwa,
Kunka naye Yesuyo,
Ndidzakondwerera naye komweko.

Tisaleke kugwirabe
Ntchito ya Mulunguyo,
Tibukitse mbiri yake m’dzikoli,
Ndi podzatha moyo wathu
Ndi zintchito zathuzo,
Tidzakondwerera naye komweko.

Post navigation

Previous: Hymn 78 ALINKUDZA wansoni Munthu,
Next: Hymn 80 KUDZA kwa Mbuye

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 226 Nditama mwaziwo!
  • Hymn 298 IFE tazingidwa ndi zinthu zoopsa,
  • Hymn 611 Tidzakhala naye nthawi zonse ndi kuimbako,
  • Hymn 836 Kamoyo kanga katha lero lino,
  • Hymn 368 MULUNGU wanga, Dzuŵatu
  • Hymn 92 Ufuna kugwira ntchito yake?
  • Hymn 1665 Nkhope yanu ndifunitsa,
  • Hymn 784 Mugwade pansi m’nyumbayo,
  • Hymn 1759 Powalitsira omwe
  • Hymn 138 Kumva ulikumva, ulikumva,
  • Hymn 266 MBUYE ndamva mwawazira
  • Hymn 222 Ndilikudzatu,
  • Hymn 230 AMBUYANGA Yesu,
  • Hymn 13 Mtiwerengere m’Mwamba ndi oyera;
  • Hymn 935 Mtima ukachita nkhawa
  • Hymn 1046 Ndiyere mbuu! E, ndiyere mbuu!
  • Hymn 997 Mawu ake atipatsa
  • Hymn 294 Yesu anali khanda
  • Hymn 1202 Ndikhumba mtimawo
  • Hymn 416 Woyenera ndani kunka
  • Hymn 259 CHISOMO chodabwitsacho,
  • Hymn 289 Ndi manja athu awa nawo nganu,
  • Hymn 123 Koma mudzisungire chuma cha Kumwamba
  • Hymn 1471 Ukapenya kwa Yesu uliko moyoko,
  • Hymn 33 Tamandani Mbuye,
  • Hymn 567 M’nyumba zonse ponseponse
  • Hymn 449 MLENGI wathu Woyeranu,
  • Hymn 257 Ndinasiya amayi,
  • Hymn 43 GETSEMANI, Getsemani,
  • Hymn 1146 Khalani duu! Pakufa mnzathuyo,
  • Hymn 1738 “Senzani mtanda wanuwo.”
  • Hymn 1091 Mulamulire mtima, Yesu,
  • Hymn 166 NDICHITENJI kukapeza
  • Hymn 878 Zokoma inde nthawizi
  • Hymn 826 Mutonthoze mtima
  • Hymn 518 Ana a Yerusalemu
  • Hymn 1846 Mtima wanga uyamike
  • Hymn 1582 Konda dzinalo la Yesu
  • Hymn 1611 Nadzuka m’mandamo
  • Hymn 389 NDIMAMVA njala, Yesu,
  • Hymn 1510 Mtume tsopanoli
  • Hymn 1256 Chitsime ndi chokoma
  • Hymn 407 ADZAPAMBANA Yesu ponse
  • Hymn 544 Zoopsya sitidziwapo
  • Hymn 672 Mbwere Yesu Mwini moyo,
  • Hymn 57 TIYENI, dzalireni nane,
  • Hymn 56 KU Mzinda wakuyerawo
  • Hymn 318 TINALI ambiri ife,
  • Hymn 354 ATATE, tifika pamaso panu;
  • Hymn 1558 Wosangalatsa, ine ndikalira
  • Hymn 1702 Pakufa ine Mbuye
  • Hymn 1817 Ndi m’munda muja chete, phee!
  • Hymn 1189 Ambuye Mulungu,
  • Hymn 1354 Mzimu Woyera, m’mtimamo
  • Hymn 646 Mudalitse nyumba yathu;
  • Hymn 1098 M’mene mantha andigwira,
  • Hymn 1608 Yesu, dzina lakukonda
  • Hymn 229 Woba wakufa ‘napenya
  • Hymn 346 PEMPHERO ndiko kufuna,
  • Hymn 154 SING’ANGA ‘mkulu ndiye Yesu,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version