Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 296 TIYENI Akhristu,

  1. Home   »  
  2. Hymn 296 TIYENI Akhristu,

Hymn 296 TIYENI Akhristu,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 296 TIYENI Akhristu,

 

TIYENI Akhristu,
Nkhondo tigwire;
Yesu Mbuye wathu
Atitsogolera.
Mfumu yathu mwini
Atipatsa moyo;
Taonanitu mbendera
Yailoŵa nkhondo!

Tiyeni Akristu,
Nkhondo tiigwire;
Yesu Mbuye wathu
Atitsogolera

Nkhondo ya Satana
Idzakuthaŵani;
Tiyeni Akristu,
Kaipambaneni.
Idzanjenjemera
Mukapfu’litsatu;
Imbitsanitu anzathu,
Mau mukwezetse.

Mpingo wa Mulungu
Uli ngati nkhondo;
Titsagane nawo
Ana a Mulungu.
Sitipatukana,
Ndifetu amodzi;
Ch’yembekezo, chikondano,
Chonse ndi chimodzi.

Zonse zapadziko
Zidzamalizira,
Koma mpingo wake
Uli chikhalire;
Udzakhala ndithu
Mphamvu za Satana,
Yesu analonjezetsa,
Mawuwo sakana.

Tiyeni anzathu
Tizithandizana;
Imbirani nafe
Nyimbo zopambana
Kristu ayenera
Mphamvu ndi ulemu;
Komwe kuli Yesu.

Post navigation

Previous: Hymn 295 AMBUYE wa Kumwamba,
Next: Hymn 297 POKUMANA m’mayesero a dziko lino,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 266 Ukondwere moyo wanga,
  • Hymn 84 Aleluya, Aleluya,
  • Hymn 39 MUNASIYATU dziko lanulo,
  • Hymn 10 TSOPANO linoli,
  • Hymn 564 Ndi chifukwa atikonda,
  • Hymn 4 INU Mulungu, tikuyamikani;
  • Hymn 61 A! MUTU wakuyera,
  • Hymn 1831 M’mitsinje yamtendere mtima wanga aumwetsa;
  • Hymn 1627 Adzabwera, adzabwera;
  • Hymn 1340 Perekani mtima wanu
  • Hymn 215 TATE ndili mwana wanu,
  • Hymn 192 Apita anzathu dzuwa lino Kosaoneka,
  • Hymn 205 KWA Inu Yesu ndilira,
  • Hymn 454 TAONANI, m’kholamo,
  • Hymn 494 YESU Mbusa, mutimvere,
  • Hymn 1143 Tikhale ndithu pomwepo;
  • Hymn 252 MTIMA wa Mbuyako,
  • Hymn 670 Isaleke ntchito yake
  • Hymn 484 Mutiletse, Mbuye,
  • Hymn 908 Ndikonda kuganizirabe
  • Hymn 298 “Tadodoma, abusa,
  • Hymn 1449 Pena imfa idza mawa,
  • Hymn 1481 Timsankhe Yesu Mbuyeyo,
  • Hymn 1655 Mbuye Yesu,
  • Hymn 1414 Zonse zinathedwadi;
  • Hymn 30 YEHOVA, Mbusa wangadi,
  • Hymn 398 KODI mbale wasimba zachikhululukiro,
  • Hymn 464 Yesu atiuza tiyambemo,
  • Hymn 1730 Anapeputsidwako,
  • Hymn 483 Ndife akuchoka,
  • Hymn 7 NDI Aleluya imbirani,
  • Hymn 124 PAMTANDAPO, pamtanda,
  • Hymn 112 Pangano lake m’mwaziwo
  • Hymn 368 Yehova ndiye Mlungudi,
  • Hymn 693 Adzapambana Yesu ponse
  • Hymn 1249 Tsirizani ntchito yanu
  • Hymn 1117 Ndifuna Yesuyo
  • Hymn 1374 Inu mumvere anyamatawo,
  • Hymn 959 Ana akumwamba ndife,
  • Hymn 1315 Ambuye ‘naitana ‘ne:
  • Hymn 1643 Kufuna inetu, kufuna inetu,
  • Hymn 285 Ndipempha, Ambuye,
  • Hymn 28 Mbuye ndisaukadi,
  • Hymn 1257 Mtanda m’mtima ndiyang’na,
  • Hymn 677 Ponse padakhala mdima
  • Hymn 1413 Ndichitenji kukapeza
  • Hymn 326 Yesu, Bwenzi la ochimwa,
  • Hymn 1535 Lichepa dontho lokhali,
  • Hymn 799 Inu Mlungu kalelo
  • Hymn 531 Pakubweranso Inu m’Ufumuwo
  • Hymn 876 Mtidzutse, Mbuyetu,
  • Hymn 432 Ulendo ungoyamba
  • Hymn 403 Dzuwa liwala, m’tulotu
  • Hymn 456 ANA inu, ana inu,
  • Hymn 1810 Kalelo Mbuye Yesu
  • Hymn 86 Mwandipatulira ine,
  • Hymn 1658 Idza wolema,
  • Hymn 1623 Adzatenga anthu ake
  • Hymn 984 Mpingo wa Mulungu
  • Hymn 171 IWE tiye, iwe tiye,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version