Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 296 TIYENI Akhristu,

  1. Home   »  
  2. Hymn 296 TIYENI Akhristu,

Hymn 296 TIYENI Akhristu,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 296 TIYENI Akhristu,

 

TIYENI Akhristu,
Nkhondo tigwire;
Yesu Mbuye wathu
Atitsogolera.
Mfumu yathu mwini
Atipatsa moyo;
Taonanitu mbendera
Yailoŵa nkhondo!

Tiyeni Akristu,
Nkhondo tiigwire;
Yesu Mbuye wathu
Atitsogolera

Nkhondo ya Satana
Idzakuthaŵani;
Tiyeni Akristu,
Kaipambaneni.
Idzanjenjemera
Mukapfu’litsatu;
Imbitsanitu anzathu,
Mau mukwezetse.

Mpingo wa Mulungu
Uli ngati nkhondo;
Titsagane nawo
Ana a Mulungu.
Sitipatukana,
Ndifetu amodzi;
Ch’yembekezo, chikondano,
Chonse ndi chimodzi.

Zonse zapadziko
Zidzamalizira,
Koma mpingo wake
Uli chikhalire;
Udzakhala ndithu
Mphamvu za Satana,
Yesu analonjezetsa,
Mawuwo sakana.

Tiyeni anzathu
Tizithandizana;
Imbirani nafe
Nyimbo zopambana
Kristu ayenera
Mphamvu ndi ulemu;
Komwe kuli Yesu.

Post navigation

Previous: Hymn 295 AMBUYE wa Kumwamba,
Next: Hymn 297 POKUMANA m’mayesero a dziko lino,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1696 Mndiletse, ndisateme ‘yi
  • Hymn 440 Yesu wakufatsa mtima
  • Hymn 729 Ndifuna kumva Inu,
  • Hymn 751 Mongatu mawu anuwo,
  • Hymn 1638 Alinkudza wansoni Munthu
  • Hymn 897 Ndine mlendo pansi pano,
  • Hymn 221 Yesu and’itana,
  • Hymn 1388 Tiimbire Mlungu wathu
  • Hymn 135 USANABADWE, Yeremiya,
  • Hymn 88 Ufuna kuwomboledwa kodi?
  • Hymn 730 A! Yesu mwapangana
  • Hymn 285 Ndipempha, Ambuye,
  • Hymn 1203 Zambiri zangazo
  • Hymn 1067 Ambuyathu, ndikhumba tsiku lija
  • Hymn 325 KODI uli ndi chisoni
  • Hymn 1112 Masiku anga onse
  • Hymn 105 Tiyamike Mbuye Yesu
  • Hymn 1063 Pokhala mtendere mu mtimangamu,
  • Hymn 519 Mverani, aimba anawo,
  • Hymn 650 Tikondwa tonse ndi kukuthokazani Nu
  • Hymn 1140 Paja athira Yesutu
  • Hymn 812 Ndi ena sanamvera ‘yi,
  • Hymn 1026 Inde nditaya chumacho,
  • Hymn 1051 Zin’sowa indedi
  • Hymn 497 Yesu andikonda ine,
  • Hymn 491 KWA Yesu ndi kwabwinoko,
  • Hymn 334 Tsugulani mtima wanu
  • Hymn 443 Tchimo musalole,
  • Hymn 982 Tiyeni Akristu,
  • Hymn 436 YEHOVA Mlungu wathu,
  • Hymn 888 Polowa ndi Inu
  • Hymn 568 Taukani, taonani
  • Hymn 1637 Tisaleke kugwirabe
  • Hymn 527 Idzani mumtima mwanga,
  • Hymn 1739 Ife timakufunani
  • Hymn 1264 Chifuniro change, Mbuye, Ndiperekachi;
  • Hymn 330 Yesu ndiye Mtsogoleri
  • Hymn 468 NDIKONDWA kuti
  • Hymn 962 Inde Mbuye, tibweradi,
  • Hymn 561 Uyu ‘natsikira kuno,
  • Hymn 1165 Dzanja la Mulungu
  • Hymn 449 Mzimu wakuipa
  • Hymn 1722 Ambuye tikondweratu
  • Hymn 927 Pakutsazikana nanu
  • Hymn 408 ABALE nonse mulindiranji?
  • Hymn 459 Aphunzitse anthuwo,
  • Hymn 1710 Pamtandapo, pamtandapo
  • Hymn 79 PAKWITANA Mbuye wanga
  • Hymn 199 NDINASOKERA kutali,
  • Hymn 796 Timvere Mawu anu
  • Hymn 238 MULUNGU wanga,
  • Hymn 277 Mbwere nonse muone
  • Hymn 1827 Abramu kalelo anamvera bwino;
  • Hymn 1602 M’mawu a Yesu Mbuyeyo,
  • Hymn 279 MBUYE, nditsate bwanjiko?
  • Hymn 11 Imfa mutagonjetsa ndi zowawa,
  • Hymn 911 Mokhala mokhamokha
  • Hymn 1269 Ndifoka ndi zoipazo,
  • Hymn 1845 Zabwino ndi zokoma zinditsata chitsatire;
  • Hymn 1435 Ndiwe mlendo lero lino,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version