Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 30 YEHOVA, Mbusa wangadi,

  1. Home   »  
  2. Hymn 30 YEHOVA, Mbusa wangadi,

Hymn 30 YEHOVA, Mbusa wangadi,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 30 YEHOVA, Mbusa wangadi,

 

YEHOVA, Mbusa wangadi,
Ndilibe kusoŵa;
Andigonetsa bwinoli
Mumsipu wokoma.

Ku madzi ake odikha
Anditsogolera;
Ndi moyo wanga wofoka
Aulimbikitsa.

Anditsogolera m’njira
Zakulungamazo;
Chifukwa changa ay’, koma
Cha dzina lakelo.

Ndipyola kodi chikhwaŵa
Cha mthunzi wa imfa?
Ndilibe mantha ngati ’Nu
Mundiperekeza.

Chakudya changa chabwino
Mwandikonzera pha!
Pamaso pa adaniwo
Mudyetsa mtimanga.

Mwadzoza mutu wanga ndi
Mafuta okoma;
Mwadzadza chikho changadi,
Inde, chisefuka.

Zokoma ndi zakuyanja
Zidzanditsatako;
Ndikhala m’nyumba ya Mlungu
Ku nthaŵi zonsezo.

Post navigation

Previous: Hymn 29 CHIKONDI cha
Next: Hymn 31 MULUNGU Wamkulu,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1759 Powalitsira omwe
  • Hymn 1539 Kudzoza kwa Kumwambako
  • Hymn 90 WINA atikonda ife,
  • Hymn 745 Anatifera nsembe Iyeyo,
  • Hymn 282 Ine ndili munthu
  • Hymn 518 Ana a Yerusalemu
  • Hymn 528 Amithenga ‘naimba pamlengapo,
  • Hymn 177 Tate, ndili mwana wanu,
  • Hymn 551 Ndani kodi Munthuyo
  • Hymn 1632 Ndi chiyembekezo ichi
  • Hymn 60 ZATHEDWA zonsetu
  • Hymn 1322 Ntchito zanga zonsezo
  • Hymn 294 Yesu anali khanda
  • Hymn 348 CHIKHULUPIRIRO chathu
  • Hymn 222 NDILIKUMVA m’mtima mwanga
  • Hymn 87 Aleluya, mwandigula,
  • Hymn 75 MBUYE, mutsaganetu
  • Hymn 470 Mutiletse tisaname
  • Hymn 582 A! Mulungu,
  • Hymn 1040 Ukafuna kulemera,
  • Hymn 1527 Ndiye Mzimu Wakuyera
  • Hymn 1655 Mbuye Yesu,
  • Hymn 1834 Chisomo ndi zokoma zake sizileka konse;
  • Hymn 579 Pochezera m’dambomo,
  • Hymn 175 A! MBUSA wathu amvatu
  • Hymn 917 Ndi nkhondo ikaleka
  • Hymn 737 Mommuno, Mbuye, tionanetu,
  • Hymn 438 TIYAMIKE Ambuye,
  • Hymn 384 USIKU uja kalero,
  • Hymn 734 Ndi mkate wanu, Yesu
  • Hymn 1101 Ngati mtima sumakonda
  • Hymn 158 WOCHIMWA iwe, bweratu,
  • Hymn 232 WAFUNAFUNA ine
  • Hymn 103 Bwenzi lathu ndinutu,
  • Hymn 160 Kamwana kaja ‘nayamba
  • Hymn 253 YESU ndinutu wanga m’njira zonse,
  • Hymn 70 Mbuye ndinu bwenzi langa ndithu,
  • Hymn 968 Mzimu wakuipa
  • Hymn 253 Adzakhala pampandopo
  • Hymn 399 Tchimo lathu lonse, Yesu,
  • Hymn 445 Mlewe oipawo,
  • Hymn 896 Mbuye, ndinalema ine,
  • Hymn 389 Ambuye, mtidalitsetu,
  • Hymn 554 Iye ndani pamtanda
  • Hymn 316 Ndikhazikike inetu,
  • Hymn 44 Mlungu dalitsani Malawi,
  • Hymn 1584 Konda dzinalo la Yesu
  • Hymn 197 Tidzatama Atate wathu
  • Hymn 198 CHITSIMECHO cha mwaziwo
  • Hymn 600 Mbuye Yesu, myandikire,
  • Hymn 37 YESU analikhanda
  • Hymn 259 Zoipa zakanikadi,
  • Hymn 257 NJIRA yanga sindiziŵa,
  • Hymn 226 Nditama mwaziwo!
  • Hymn 700 Mzimu woonadi
  • Hymn 1508 Mundinyemere ‘ne
  • Hymn 1487 Bvumbulutsa zonse zako
  • Hymn 496 Yesu Mbuye ‘Nu wabwino,
  • Hymn 304 Imva kulira kwa Yesu
  • Hymn 1512 Cholimbitsa mtima ndi

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version