Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 397 MBUYE wathu, mutipatsa

  1. Home   »  
  2. Hymn 397 MBUYE wathu, mutipatsa

Hymn 397 MBUYE wathu, mutipatsa

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 397 MBUYE wathu, mutipatsa

 

MBUYE wathu, mutipatsa
Zonse tili nazozo,
Mutikomeratu mtima
Osaleka konseko,
Mutikonda, mutisunga,
Mutisamalira ’fe.

Dzuŵa, madzi, kudya, mpweya,
Moyo, zonse nzanuzi,
Si za ife, nzaulere,
Tingozilandiradi;
Zifumira kwa Aate
Wotikondakondatu.

Monga tilandira, Mbuye,
Mtiphunzitse tonsefe
Tipere chuma chathu
Ndi kusangalalatu;
Zakukhala m’manja mwathu
Tiziyese nzanudi.

Tikhaletu nawo, Mbuye,
Mtima wosauma ’yi
Ndi wofatsa ndi wabwino
Ndi woyerayeradi,
Kuti tiyenere Dzina
La Mbuyathu Yesuyo.

Tisaiwalire ’bale
Athu osadziŵa ’Nu,
Akulira ndi odwala
Tiŵapemphereratu;
Titsanzenso Mbuye Yesu
Ndi k’ŵathangatira ’wo.

Dalitseni, Mbuye, zonse
Zomwe taperekazi,
Mzilandire, nsembe yathu,
Mziyeretse Inudi
Ndi mitima yathu yonse
Tikuyamikirani.

Post navigation

Previous: Hymn 396 PETURO ’nafunsa Hananiya:
Next: Hymn 398 KODI mbale wasimba zachikhululukiro,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 813 Wopulumutsa, Inunso
  • Hymn 1665 Nkhope yanu ndifunitsa,
  • Hymn 1843 Chigwa choopsacho cha imfa ndikachilowera,
  • Hymn 1204 Ambuyanga Yesu,
  • Hymn 43 GETSEMANI, Getsemani,
  • Hymn 1690 Titama Yesuyo,
  • Hymn 889 Pemphera m’mbanda kucha,
  • Hymn 225 NDIDZAIMBA za Mulungu,
  • Hymn 622 Tiyamikira ‘Tate,
  • Hymn 1200 Ambuye, m’imfamo
  • Hymn 485 POMPANO pandikonda
  • Hymn 1652 Mabala ajawo
  • Hymn 7 NDI Aleluya imbirani,
  • Hymn 1825 Zobvuta zoopsa ndi zosaukazi
  • Hymn 291 Ndi milomo yathu iyinso njanu,
  • Hymn 353 ATATE Wamkulu ndi Wamphamvu zonse,
  • Hymn 117 CHOLIMBITSA mtima ndi chonditsogolera;
  • Hymn 349 MOSE anamenya thanthwe kawiri,
  • Hymn 280 YESU, afuna iwe unke kwawoko,
  • Hymn 1301 Moyo ukatha zi,
  • Hymn 1239 Ndipo pakuima phe!
  • Hymn 524 Wokoma Mbuyathu
  • Hymn 855 Aulendo amayenda
  • Hymn 1324 M’moyo uno kunsiku
  • Hymn 410 MAWU akewo anamveka ponse,
  • Hymn 69 KONDWERANI dzuŵa lino,
  • Hymn 1733 Adzabwera Iyenso
  • Hymn 428 Tiyandika, Mbuye,
  • Hymn 125 Aliponso mabvuto, ena ndi oipa;
  • Hymn 487 Yesu, ndikabwera
  • Hymn 220 Kalekale ndinathawa,
  • Hymn 274 E! tidzakomanansotu
  • Hymn 1616 Anafera
  • Hymn 607 Dziko lonse lilikukondwa, mlengalenga mpheponso,
  • Hymn 1269 Ndifoka ndi zoipazo,
  • Hymn 1491 Zokandweretsa m’dzikomu
  • Hymn 1637 Tisaleke kugwirabe
  • Hymn 1210 Kumwamba ndidzanenadi
  • Hymn 1716 Anena mawu m’mtanda momwe,
  • Hymn 263 Mulungu wakwezekatu,
  • Hymn 825 Mpatse ana ‘ng’ono
  • Hymn 113 Likalira llipengalo,
  • Hymn 287 POKONDWA ndi poona vuto
  • Hymn 1758 Poti Mulungu wathu
  • Hymn 68 Kwathu ndidzaimba nyimbo
  • Hymn 1333 Idzatu kwa Yesuyo,
  • Hymn 1476 Mipingo iyo idzatu,
  • Hymn 9 TAMANI Ambuye,
  • Hymn 1786 Ndikonda Mlungu pomva Mbuye wanga
  • Hymn 1078 Khalatu woyera
  • Hymn 725 Munafera ine kale
  • Hymn 998 Anatilemba Yesu tikagwire nkhondo yake,
  • Hymn 1256 Chitsime ndi chokoma
  • Hymn 245 KHALANI duu! Ambuye adzatu;
  • Hymn 1425 Apempha malo Ambuye;
  • Hymn 1063 Pokhala mtendere mu mtimangamu,
  • Hymn 1 Ndinu wakuyera!
  • Hymn 992 Mukandipweteka,
  • Hymn 743 Mudze, anthuni, talawani ‘nu
  • Hymn 814 Mutichiritse ifenso

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version