Site icon Treasure Hymns – Chichewa

Hymn 181 PANALITU wakudwala

Chichewa Christian Hymns

Hymn 181 PANALITU wakudwala

 

PANALITU wakudwala
Amene akakhala
Pakhomo la sunagoge:
Kuti anthu ena
Amuone iye.

Yenda iwe, yenda.
Yenda iwe, yenda,
Siliva ndilibe;
Mwa Yesuyo, yenda!

Kukondwa kwa wodwalayo
Kunali kopambana;
Iye anatumphatumpha,
Kuzungulira
Sunagoge yense.

Lero lino Mbuye Yesu
Aitana nonsenu;
Mukamvera ndi kumtsata,
Mudzakondwera
Ndi mdalitso wake.

Exit mobile version