Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 181 PANALITU wakudwala

  1. Home   »  
  2. Hymn 181 PANALITU wakudwala

Hymn 181 PANALITU wakudwala

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 181 PANALITU wakudwala

 

PANALITU wakudwala
Amene akakhala
Pakhomo la sunagoge:
Kuti anthu ena
Amuone iye.

Yenda iwe, yenda.
Yenda iwe, yenda,
Siliva ndilibe;
Mwa Yesuyo, yenda!

Kukondwa kwa wodwalayo
Kunali kopambana;
Iye anatumphatumpha,
Kuzungulira
Sunagoge yense.

Lero lino Mbuye Yesu
Aitana nonsenu;
Mukamvera ndi kumtsata,
Mudzakondwera
Ndi mdalitso wake.

Post navigation

Previous: Hymn 180 MALO alimo m’nyumba ya Yesu,
Next: Hymn 182 YESU watidzera, watidzera,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 59 Tinachoka munjira ya imfa,
  • Hymn 1228 Lindikomera dzina la Ambuye Yesu wanga,
  • Hymn 64 Mantha, nkhawa, ndi chisoni
  • Hymn 1389 Tithawire kwa Mulungu,
  • Hymn 1723 Unakhetsedwa mwazi do!
  • Hymn 249 MBUYANGA Yesu, mundigwire
  • Hymn 646 Mudalitse nyumba yathu;
  • Hymn 69 Kwathu sipadziko, ndingopitirira,
  • Hymn 883 Pokupempherani
  • Hymn 626 Inde, ‘Tate, mtiyendetse
  • Hymn 1008 Wakuchezacheza naye
  • Hymn 1219 Bwenzi ndinamkomanayo
  • Hymn 499 ‘Nafera Mbuye wanga
  • Hymn 632 Tsopano tipereka mapemphero athu ano,
  • Hymn 1816 Anatikondakonda ‘Ye,
  • Hymn 1557 M’phunzitsi, ndinu mudziwitse ine
  • Hymn 478 Ndife ana, mutikonda,
  • Hymn 32 Tamandani Mbuye,
  • Hymn 994 Limba mtima mbale wanga,
  • Hymn 444 YEMWE afesa nalira,
  • Hymn 251 Kuli chimwemwe m’dzuwalo
  • Hymn 1131 M’mene ine ndisauka
  • Hymn 330 Yesu ndiye Mtsogoleri
  • Hymn 1617 Anadzuka,
  • Hymn 1486 M’dziko lino pansi pano
  • Hymn 1684 Mbuye mabala anu olimba
  • Hymn 404 Dzuwa la lero lonseli
  • Hymn 360 KRISTU wakuyeratu,
  • Hymn 1048 Kumwamba ndiona Ambuyangayo,
  • Hymn 1334 Walandira inetu
  • Hymn 156 Yesu Mbuye, onani
  • Hymn 1314 Mulungu ali nane!
  • Hymn 241 MTENDERE uli m’mtima mwathumu,
  • Hymn 635 Tipempha madalitso ano mpatse ife tonse;
  • Hymn 328 Yesu ndiye mphamvu yanga,
  • Hymn 1138 Masiku onse m’mtima mwanga
  • Hymn 621 Wolenga ndi Yemweyo
  • Hymn 408 ABALE nonse mulindiranji?
  • Hymn 1086 “Khala mwa Ine,” ndinu mwini moyo,
  • Hymn 1431 Lero lino m’bale wanga,
  • Hymn 1293 Chitsimecho cha mwaziwo
  • Hymn 158 Mzimu, mlonge m’mtimamo
  • Hymn 986 Tiyeni anzathu
  • Hymn 1492 Sakukanani Yesudi,
  • Hymn 384 Mulungu akhale nawo
  • Hymn 716 Tibwezeretu bwanjiko?
  • Hymn 356 YESU Mbuye onani,
  • Hymn 212 Onse am’Mwamba ali mowemo,
  • Hymn 202 NDIKHULUPIRIRA, Yesu,
  • Hymn 98 Ndidzamwona maso ndi maso
  • Hymn 1316 Ndabwera kwa Ambuyeyo:
  • Hymn 763 Ndiponso m’manja chikhocho
  • Hymn 1103 Ndakudani, mnandikonda
  • Hymn 1032 Ntchito za Yesu gwira
  • Hymn 5 ATATE wa Kumwambako,
  • Hymn 997 Mawu ake atipatsa
  • Hymn 1609 Idzani nose’nu
  • Hymn 1727 Pokumbukira mtandawo
  • Hymn 1595 Ndani mwa abale athu
  • Hymn 947 Akristu tonsefe, tikondwe m’Dzikoli

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version