Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 222 NDILIKUMVA m’mtima mwanga

  1. Home   »  
  2. Hymn 222 NDILIKUMVA m’mtima mwanga

Hymn 222 NDILIKUMVA m’mtima mwanga

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 222 NDILIKUMVA m’mtima mwanga

 

NDILIKUMVA m’mtima mwanga
Mau ake a MbuyAnga,
Ati, “Ndakukonda iwe,
Kodi undikonda Ine?”

Ati; “Mwana, kumbukira
Zonse ndinakuchitira;
Ndakukonda, ndakufera,
Ndakufuna posokera.

“Ku zoipa zonse zako,
Goli la pakhosi pako,
Ndi kunthenda zosautsa
Ndine ndakupulumutsa

“Kodi mayi wobereka
Mwana wake adzamleka
Pena adzamwiŵalira,
Koma ndikukumbukira.

“Nthaŵi ilikudza yonse
Sindisinthanika konse;
Imfa sindiletsa Ine
Ndisakondekonde iwe.

“Ine ndidzakuonetsa
Zonse zakukondweretsa
Za Kumwamba zanga izo,
Mwana, sundikonda ine?”

Ambuyanga, ndalephera,
Mwachisoni ndipemphera
Mundipatse ine ndithu
Mtima wakukonda Inu.

Post navigation

Previous: Hymn 221 A! CHIKONDI chopambana,
Next: Hymn 223 ATI Yesu Mbuyeyo:

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 984 Mpingo wa Mulungu
  • Hymn 481 USACHIMWE konse,
  • Hymn 1730 Anapeputsidwako,
  • Hymn 1561 Mzimu Woyera, n’dzipereka ndense,
  • Hymn 487 INE ndine mlendo
  • Hymn 602 Mpulumutsi wakukoma,
  • Hymn 1132 Mlungu adzandilandila,
  • Hymn 1507 Ndikampempha anditenge,
  • Hymn 93 Mverani mbiri yozizwitsa
  • Hymn 450 YESU, munditsogoza
  • Hymn 1412 Imfa idzafika msanga;
  • Hymn 1788 Mtimanga, bwera kuti upumule
  • Hymn 382 M’wabatize anzathuwa,
  • Hymn 493 DZUŴA li
  • Hymn 268 POKHALA mtendere mu mtimangamu,
  • Hymn 1575 Tifuna kuti komweko
  • Hymn 811 Wopulumutsa mudzetu;
  • Hymn 222 NDILIKUMVA m’mtima mwanga
  • Hymn 134 Aleluya, Aleluya!
  • Hymn 1538 Mzimu Woyera, mudzetu
  • Hymn 1175 Sindinanyengedwa konse,
  • Hymn 77 MMENE Yesu adzabwera,
  • Hymn 511 Ntchito zake zatha,
  • Hymn 35 Zonse za m’dziko zidzatha,
  • Hymn 817 Tibvomereze,
  • Hymn 47 YESU panjirayo,
  • Hymn 142 MULUNGU aŵakonda anthu
  • Hymn 735 Mwa chikho chokumbutsa
  • Hymn 983 Nkhondo ya Satana
  • Hymn 995 Taya zako zochenjera,
  • Hymn 262 “KHALA mwa Ine,” Yesu anatero;
  • Hymn 1143 Tikhale ndithu pomwepo;
  • Hymn 276 Dziko lonse mlambire
  • Hymn 826 Mutonthoze mtima
  • Hymn 144 AMENE adzavomereza ndithu,
  • Hymn 505 Ndikondwa kuti Atate wam’Mwamba
  • Hymn 456 Tizikondana, tisekere
  • Hymn 354 ATATE, tifika pamaso panu;
  • Hymn 248 Pena pakufadi,
  • Hymn 406 M’MENE umauka m’maŵa,
  • Hymn 127 POLUMIDWA ndi njokazo,
  • Hymn 1828 Timtamande Iye ndi moyo wathunso
  • Hymn 107 MUBWERE kuno Mzimu ’Nu
  • Hymn 368 Yehova ndiye Mlungudi,
  • Hymn 1623 Adzatenga anthu ake
  • Hymn 1481 Timsankhe Yesu Mbuyeyo,
  • Hymn 276 MKRISTU, ulimbike
  • Hymn 1581 Ndi nyimbo yabwino
  • Hymn 1248 ‘Dzanitu Wamphamvu yonse,
  • Hymn 724 Ndine mlendo pansi pano,
  • Hymn 1231 Nlokoma dzinalo la Yesu, ndilo thanthwe langa,
  • Hymn 893 Mtima wanga ndikonzera,
  • Hymn 338 Imvani
  • Hymn 469 NDIKONDA mbiri yomwe
  • Hymn 1589 Ndinasokera kalelo,
  • Hymn 982 Tiyeni Akristu,
  • Hymn 390 Lalowa dzuwa, kwada bii!
  • Hymn 256 NGATI mtima sumakonda
  • Hymn 408 Oipa tili tonsefe;
  • Hymn 21 KUZANI Mlungu m’Mwambamo,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version