Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 222 NDILIKUMVA m’mtima mwanga

  1. Home   »  
  2. Hymn 222 NDILIKUMVA m’mtima mwanga

Hymn 222 NDILIKUMVA m’mtima mwanga

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 222 NDILIKUMVA m’mtima mwanga

 

NDILIKUMVA m’mtima mwanga
Mau ake a MbuyAnga,
Ati, “Ndakukonda iwe,
Kodi undikonda Ine?”

Ati; “Mwana, kumbukira
Zonse ndinakuchitira;
Ndakukonda, ndakufera,
Ndakufuna posokera.

“Ku zoipa zonse zako,
Goli la pakhosi pako,
Ndi kunthenda zosautsa
Ndine ndakupulumutsa

“Kodi mayi wobereka
Mwana wake adzamleka
Pena adzamwiŵalira,
Koma ndikukumbukira.

“Nthaŵi ilikudza yonse
Sindisinthanika konse;
Imfa sindiletsa Ine
Ndisakondekonde iwe.

“Ine ndidzakuonetsa
Zonse zakukondweretsa
Za Kumwamba zanga izo,
Mwana, sundikonda ine?”

Ambuyanga, ndalephera,
Mwachisoni ndipemphera
Mundipatse ine ndithu
Mtima wakukonda Inu.

Post navigation

Previous: Hymn 220 MULUNGU mundichitire chifundo,
Next: Hymn 241 MTENDERE uli m’mtima mwathumu,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 98 Ndidzamwona maso ndi maso
  • Hymn 320 NDIKONDA Mlungu pomva Mbuye wanga
  • Hymn 389 Ambuye, mtidalitsetu,
  • Hymn 735 Mwa chikho chokumbutsa
  • Hymn 395 AMBUYE, Mwini zonsezi,
  • Hymn 1362 Mulungu wathu tiyamika,
  • Hymn 115 Mbulu wanding’amba m’nthiti,
  • Hymn 1070 Mthandize Mbuye, timvetu,
  • Hymn 466 Yesu, muli pa chimpando
  • Hymn 1697 Onani m’mutu, m’manjanso
  • Hymn 2 YEHOVA Mthandizi,
  • Hymn 1465 Akulu inu m’bwere nonse,
  • Hymn 1633 Adzabwera, adzabwera;
  • Hymn 1723 Unakhetsedwa mwazi do!
  • Hymn 267 AMBUYE, thandizenitu
  • Hymn 92 KONDA dzinalo la Yesu,
  • Hymn 1376 Akulu nonse ndi mafumu ‘nu,
  • Hymn 1618 Anakwera,
  • Hymn 455 Mdileke kulimbna ndi
  • Hymn 300 AKRISTU limbikani,
  • Hymn 1504 Kodi ali ndi chilemba
  • Hymn 973 Tigwire nkhondo yomwe
  • Hymn 120 MUNDINYEMERE ’ne
  • Hymn 414 INU bambo, inu mayi,
  • Hymn 1077 Khalatu woyera,
  • Hymn 1682 Atha masiku aja ansoni,
  • Hymn 1093 Odala ndi onsewo
  • Hymn 1026 Inde nditaya chumacho,
  • Hymn 823 M’mwambamo nyenyezi
  • Hymn 423 MUNENE Mbuye, ’nenetu,
  • Hymn 182 Kondwani nonsenu,
  • Hymn 407 ADZAPAMBANA Yesu ponse
  • Hymn 220 Kalekale ndinathawa,
  • Hymn 921 Komwe Mbusa kwawoko
  • Hymn 562 Mwa ubwana wake wonse
  • Hymn 1388 Tiimbire Mlungu wathu
  • Hymn 515 Kuphiri la ‘Zitona,
  • Hymn 765 Chikondi chili m’chikhomu
  • Hymn 1812 Kuzani Mlungu m’Mwambamo,
  • Hymn 260 Angelo aitana,
  • Hymn 777 Mulungu ali muno,
  • Hymn 707 Dalitseni, Mbuye, zonse
  • Hymn 749 Ndiye wodyetsa anthu omwewo,
  • Hymn 605 Chifukwa cha zokoma mtima zonse za ulerezo,
  • Hymn 763 Ndiponso m’manja chikhocho
  • Hymn 228 Ataya zoipa,
  • Hymn 633 Tikasokera m’njira mutilondolere ndithu,
  • Hymn 117 CHOLIMBITSA mtima ndi chonditsogolera;
  • Hymn 527 Idzani mumtima mwanga,
  • Hymn 866 Pa la Mulungu tibwera kulandira zidazo;
  • Hymn 1546 Mubwere Mzimu Inu
  • Hymn 502 Ndikonda mbiri yomwe
  • Hymn 649 Inde, tikuyamikani, Atate, leroli,
  • Hymn 259 CHISOMO chodabwitsacho,
  • Hymn 521 Apunzitsi, ana omwe,
  • Hymn 30 Tamandani Mbuye,
  • Hymn 428 Tiyandika, Mbuye,
  • Hymn 1165 Dzanja la Mulungu
  • Hymn 269 NDILIRA ine kukayenda
  • Hymn 1703 Zathedwa zonsetu

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version