Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 22 MU ZONSE abale yamikani,

  1. Home   »  
  2. Hymn 22 MU ZONSE abale yamikani,

Hymn 22 MU ZONSE abale yamikani,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 22 MU ZONSE abale yamikani,

 

MU ZONSE abale yamikani,
Mulungu ndi wamkulu,
Adziwa kupatsa anthu ake,
Zomwe iwo akuzisowa.

Akhrisitu pamavuto tiyeni timulemekeze,
Pamtendere tiyeni timulemekeze.
Maso ake ali pa anthu,
Okhala m’dziko lapansi.

Mu zonse abale yamikani,
Mulungu ndi wamkulu,
Adziwa kuveka anthu ake,
Ngakhale nyama zakuthengo.

Mu zonse abale yamikani,
Mulungu ndi wamkulu,
Adziwa kupatsa mphatso zake,
Ngakhalenso kwa tiŵanato.

Post navigation

Previous: Hymn 20 CHIKONDI cha Mulungu wathu,
Next: Hymn 41 MKATI mwa zovuta zathu

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 175 A! MBUSA wathu amvatu
  • Hymn 797 Kwacha lero kwati mbee,
  • Hymn 318 Ambuye, muli nazo zambirizi,
  • Hymn 216 NDISAUKA, ndinachimwa,
  • Hymn 1042 Zonse umazinyadira
  • Hymn 954 Mbuye andipeza lero,
  • Hymn 1689 Dzukani nayetu,
  • Hymn 92 KONDA dzinalo la Yesu,
  • Hymn 1015 Mbuye, mwatiuza ‘fe
  • Hymn 1282 Ndilinkudza kwa Ambuye,
  • Hymn 294 POYESEDWA ine
  • Hymn 449 MLENGI wathu Woyeranu,
  • Hymn 1387 Amaweta nyama zonse,
  • Hymn 570 Ndikhulupirira Yesu
  • Hymn 621 Wolenga ndi Yemweyo
  • Hymn 1269 Ndifoka ndi zoipazo,
  • Hymn 369 LERO mwatipatsa moyo,
  • Hymn 1008 Wakuchezacheza naye
  • Hymn 1474 Zilepheradi zonse kugula moyowo,
  • Hymn 196 NDI inetu sinditha’yi
  • Hymn 1374 Inu mumvere anyamatawo,
  • Hymn 932 Munabvala thupi lathu,
  • Hymn 187 UFUNA kuwomboledwa kodi?
  • Hymn 1702 Pakufa ine Mbuye
  • Hymn 477 Mpulumutsi, Mbusa wathu,
  • Hymn 462 ANANU, ziimbani,
  • Hymn 558 Mwanayo wa Mulunguyo
  • Hymn 235 Kumwamba ndikaimbanso
  • Hymn 1273 Ndasiya zonse ndi Yesu kalelo,
  • Hymn 811 Wopulumutsa mudzetu;
  • Hymn 124 Aliponso adani am’kati ndi akunja;
  • Hymn 851 E, nthawi ya mamawayi
  • Hymn 60 Chitetezo chachikulu
  • Hymn 1129 Mbuyanga Yesu, ndikapanda Inu
  • Hymn 245 Ngakhale kuthengo
  • Hymn 1019 Tsata, tsata, nditsatadi Yesu;
  • Hymn 308 AULENDO, munka kuti
  • Hymn 254 Adzanena kwa anthuwo
  • Hymn 1402 Mverani Iye ati: idzanitu;
  • Hymn 478 Ndife ana, mutikonda,
  • Hymn 400 ONA Mwana wa Nkhosa,
  • Hymn 719 Anu Mbuye ndifetu!
  • Hymn 778 Mwini madalitso,
  • Hymn 325 KODI uli ndi chisoni
  • Hymn 675 Pamaiko pali mdima,
  • Hymn 47 Anthu m’maiko onse
  • Hymn 1828 Timtamande Iye ndi moyo wathunso
  • Hymn 1199 Ndikhumba ine ndithu
  • Hymn 1692 Timwimbire zomtamanda, Aleluya
  • Hymn 933 M’mene imfa yathu idza,
  • Hymn 410 MAWU akewo anamveka ponse,
  • Hymn 704 Monga tilandira, Mbuye,
  • Hymn 1264 Chifuniro change, Mbuye, Ndiperekachi;
  • Hymn 1740 Yesu, ndi chifundo chanu
  • Hymn 994 Limba mtima mbale wanga,
  • Hymn 359 TADZUKA mzimu wanga ‘we,
  • Hymn 1150 Pamtanda Mbuyanga ‘nafera,
  • Hymn 446 YAMIKANI nonse ’nu,
  • Hymn 84 Aleluya, Aleluya,
  • Hymn 252 MTIMA wa Mbuyako,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version