Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 22 MU ZONSE abale yamikani,

  1. Home   »  
  2. Hymn 22 MU ZONSE abale yamikani,

Hymn 22 MU ZONSE abale yamikani,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 22 MU ZONSE abale yamikani,

 

MU ZONSE abale yamikani,
Mulungu ndi wamkulu,
Adziwa kupatsa anthu ake,
Zomwe iwo akuzisowa.

Akhrisitu pamavuto tiyeni timulemekeze,
Pamtendere tiyeni timulemekeze.
Maso ake ali pa anthu,
Okhala m’dziko lapansi.

Mu zonse abale yamikani,
Mulungu ndi wamkulu,
Adziwa kuveka anthu ake,
Ngakhale nyama zakuthengo.

Mu zonse abale yamikani,
Mulungu ndi wamkulu,
Adziwa kupatsa mphatso zake,
Ngakhalenso kwa tiŵanato.

Post navigation

Previous: Hymn 21 KUZANI Mlungu m’Mwambamo,
Next: Hymn 23 TIIMBE nyimbo zotamanda

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 420 Mtima umabisala
  • Hymn 336 KULINSO dziko lowala M’mwamba,
  • Hymn 297 POKUMANA m’mayesero a dziko lino,
  • Hymn 1847 Ife tonse, ife tonse,
  • Hymn 348 CHIKHULUPIRIRO chathu
  • Hymn 1820 Kwezani nane Ambuyathu,
  • Hymn 1410 Nthawi zonse mufunabe
  • Hymn 1350 Mvera Yesu, mvera Yesu,
  • Hymn 74 IDZA wolema,
  • Hymn 1186 Yesu anafa pamtandapo,
  • Hymn 298 IFE tazingidwa ndi zinthu zoopsa,
  • Hymn 29 Tamandani Mbuye,
  • Hymn 1132 Mlungu adzandilandila,
  • Hymn 391 Mufafanize m’bukumo
  • Hymn 237 Munasiyatu
  • Hymn 1218 Pakufa pangapo
  • Hymn 172 TADZA kukudyaku,
  • Hymn 1690 Titama Yesuyo,
  • Hymn 61 Ndi chimwemwe ndimaona
  • Hymn 367 MPULUMUTSI, tikagona
  • Hymn 697 Zolengedwa zonse zidze
  • Hymn 149 RUTE, Rute anaumilira,
  • Hymn 421 Ine ndine mlendo
  • Hymn 1485 Unachimwachimwa ndithu,
  • Hymn 1045 Ambuye, ndifuna nditsukenitu;
  • Hymn 174 YESU wathu Mbuyeyo
  • Hymn 120 MUNDINYEMERE ’ne
  • Hymn 1424 Malo anachepa,
  • Hymn 1407 Tula mtolo wako
  • Hymn 934 Mnamwalira Inu paja,
  • Hymn 815 Dzuwa lapita,
  • Hymn 535 Mbuye timlemekeze,
  • Hymn 18 Mbuye mtsitsimutse
  • Hymn 215 TATE ndili mwana wanu,
  • Hymn 918 Ntchito yonse yakeyo
  • Hymn 1809 Yampatsa Nowa yemwe,
  • Hymn 1654 Mbuye, mutsaganetu
  • Hymn 542 Kuli kaphiri m’talimo
  • Hymn 532 Ukondwere mtima wanga
  • Hymn 381 MONGA zomera zonsezo
  • Hymn 257 NJIRA yanga sindiziŵa,
  • Hymn 577 Adagona m’ndyeromo
  • Hymn 410 Ana ake angonga
  • Hymn 77 Ndipereka zanga zonse,
  • Hymn 345 ATATE, ndipempha
  • Hymn 391 MUNDIMVERE, Mbuye wanga
  • Hymn 1791 Tiimbe nyimbo zotamanda
  • Hymn 1308 Ndi ine, m’mtima Mwanu mbee!
  • Hymn 1732 Anapachikidwatu,
  • Hymn 1371 Mitengo yaitalitali ‘nu
  • Hymn 1119 Ndifuna Yesuyo
  • Hymn 299 TIYENI, Akristu inu,
  • Hymn 565 Koma sitimpenya m’khola
  • Hymn 1682 Atha masiku aja ansoni,
  • Hymn 702 Mbuye wathu mutipatsa
  • Hymn 318 TINALI ambiri ife,
  • Hymn 1782 Poyamba paja analenga
  • Hymn 88 Yesu, dzina lakukonda,
  • Hymn 1078 Khalatu woyera
  • Hymn 23 TIIMBE nyimbo zotamanda

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version