Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 447 OYAMIKA Mlungu m’bwere,

  1. Home   »  
  2. Hymn 447 OYAMIKA Mlungu m’bwere,

Hymn 447 OYAMIKA Mlungu m’bwere,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 447 OYAMIKA Mlungu m’bwere,

 

OYAMIKA Mlungu m’bwere,
Zamasika mudzayimbe;
Dzinthu dzathu takolola,
Sidzionongeka m’minda.
Mlungu Mlengi asamala,
Zotisowa akonzera;
M’lowe m’nyumba ya Chauta.
M’kweze nyimbo zamasika.

Dziko lonse n’la Mulungu,
Kuti lim’balire dzinthu;
M’munda zonse zimamera,
Zakukoma ndi zoipa.
Mmera udza, bwino ngala,
Maso omwe amakhwima;
Mutilole, mwini dzinthu,
Tikakhale dzinthu dzanu.

Adzabwera Mbuye wathu,
Kukolola dzinthu dzake;
M’munda mwake akachotse,
Minga ndi zoipa zonse.
Adzatumanso angelo,
Minga akaponye m’moto;
Koma tirigu amsunge,
M’nkhokwe yake nthawi zonse.

Post navigation

Previous: Hymn 446 YAMIKANI nonse ’nu,
Next: Hymn 448 CHIFUKWA cha zokoma mtima zonse zaulelezo,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 462 ANANU, ziimbani,
  • Hymn 386 MONGATU mawu anuwo,
  • Hymn 1457 Ndidziwa kuti Yesu
  • Hymn 1379 Mulungu yemweyo
  • Hymn 236 NDIDZIWITSITSA
  • Hymn 1669 Ukafuna kumdziwitsa,
  • Hymn 136 MKAZI wa ku Samariya,
  • Hymn 35 Zonse za m’dziko zidzatha,
  • Hymn 64 Mantha, nkhawa, ndi chisoni
  • Hymn 490 Yesu, ndikabwera
  • Hymn 335 KWATHU sipadziko, ndingopitilira,
  • Hymn 1594 Chikondano chakechi
  • Hymn 605 Chifukwa cha zokoma mtima zonse za ulerezo,
  • Hymn 1458 Satana ndi unyolo
  • Hymn 1770 Iye amazichita zamphamvu
  • Hymn 330 N’LOKOMA Dziko langa!
  • Hymn 645 Kristu ndiye mwala wathu,
  • Hymn 797 Kwacha lero kwati mbee,
  • Hymn 101 Lodala tsiku lomwelo
  • Hymn 367 MPULUMUTSI, tikagona
  • Hymn 721 Anu Mbuye ndifetu!
  • Hymn 846 Kristu wakuyeratu,
  • Hymn 18 POKHALA Inu
  • Hymn 225 NDIDZAIMBA za Mulungu,
  • Hymn 190 Nsiku zonse kwanja kwake
  • Hymn 156 Yesu Mbuye, onani
  • Hymn 471 YESU Mbuye ’Nu wofatsa
  • Hymn 1248 ‘Dzanitu Wamphamvu yonse,
  • Hymn 1779 M’dzikomo Ambuye
  • Hymn 1389 Tithawire kwa Mulungu,
  • Hymn 205 KWA Inu Yesu ndilira,
  • Hymn 111 YAKOBO mwanatu wachinyengoyo;
  • Hymn 933 M’mene imfa yathu idza,
  • Hymn 312 NDIMAYENDA paulendo
  • Hymn 858 Anthu osawerengeka
  • Hymn 480 TIANA ife tingofoka,
  • Hymn 313 Muthire, Yesu, m’mtimanga
  • Hymn 277 Mbwere nonse muone
  • Hymn 89 INDE, ndifuna kumvatu,
  • Hymn 444 YEMWE afesa nalira,
  • Hymn 980 Tiyeni ku nkhondo iyi,
  • Hymn 413 ZIPATA zachitsulo zitseguke zonse mbee!
  • Hymn 819 Lero tigone,
  • Hymn 504 Pakumyamika Iye
  • Hymn 417 M’manja a Yesu wanga
  • Hymn 1332 Imba kawiri ndi kawirinso,
  • Hymn 963 Aulendo, munka kuti
  • Hymn 776 Tikondwereratu
  • Hymn 1655 Mbuye Yesu,
  • Hymn 527 Idzani mumtima mwanga,
  • Hymn 1532 Mubwere kuno Mzimu ‘Nu,
  • Hymn 24 “Ndakupeza womanga,
  • Hymn 242 M’mene mubwera
  • Hymn 47 YESU panjirayo,
  • Hymn 1468 Zobvala zake zonse
  • Hymn 466 OSANATU, osana,
  • Hymn 283 AMBUYE m’chipululu,
  • Hymn 46 O! ufulu tigwirizane
  • Hymn 379 Anditsogolera m’njira
  • Hymn 1850 Anthu a mitundu yonse,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version