Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 447 OYAMIKA Mlungu m’bwere,

  1. Home   »  
  2. Hymn 447 OYAMIKA Mlungu m’bwere,

Hymn 447 OYAMIKA Mlungu m’bwere,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 447 OYAMIKA Mlungu m’bwere,

 

OYAMIKA Mlungu m’bwere,
Zamasika mudzayimbe;
Dzinthu dzathu takolola,
Sidzionongeka m’minda.
Mlungu Mlengi asamala,
Zotisowa akonzera;
M’lowe m’nyumba ya Chauta.
M’kweze nyimbo zamasika.

Dziko lonse n’la Mulungu,
Kuti lim’balire dzinthu;
M’munda zonse zimamera,
Zakukoma ndi zoipa.
Mmera udza, bwino ngala,
Maso omwe amakhwima;
Mutilole, mwini dzinthu,
Tikakhale dzinthu dzanu.

Adzabwera Mbuye wathu,
Kukolola dzinthu dzake;
M’munda mwake akachotse,
Minga ndi zoipa zonse.
Adzatumanso angelo,
Minga akaponye m’moto;
Koma tirigu amsunge,
M’nkhokwe yake nthawi zonse.

Post navigation

Previous: Hymn 440 ZIKOMO Ambuye wathu,
Next: Hymn 461 ANA inu, myamikeni

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 240 YESU ndiye Mbuye wanga,
  • Hymn 1451 Okoma ndiwo mawu
  • Hymn 1249 Tsirizani ntchito yanu
  • Hymn 1465 Akulu inu m’bwere nonse,
  • Hymn 30 YEHOVA, Mbusa wangadi,
  • Hymn 354 ATATE, tifika pamaso panu;
  • Hymn 7 NDI Aleluya imbirani,
  • Hymn 1612 Adzadza indetu
  • Hymn 313 Muthire, Yesu, m’mtimanga
  • Hymn 1516 Pakudera nkhawa ‘ne,
  • Hymn 729 Ndifuna kumva Inu,
  • Hymn 1077 Khalatu woyera,
  • Hymn 181 Zonse ndinakonda kale
  • Hymn 1367 Wamphamvu yosatha,
  • Hymn 496 MBUYE dalitsani Afirika.
  • Hymn 52 Mbwere Mzimu, mbwere!
  • Hymn 74 Ndipereka zanga zonse
  • Hymn 629 Tinayenda muli mdima
  • Hymn 1048 Kumwamba ndiona Ambuyangayo,
  • Hymn 1087 “Khala mwa Ine,” Mbuye, ndifunitsa;
  • Hymn 304 POZUNZIDWA inu ponseponse
  • Hymn 1389 Tithawire kwa Mulungu,
  • Hymn 614 Adzabwera Mbuye wathu
  • Hymn 307 Atate Wamkulu ndi wamphamvu zonse,
  • Hymn 854 Timlemekeze Mlunguyu
  • Hymn 58 Titasokera tinabwerera,
  • Hymn 1625 Ife tonse tikumbuke
  • Hymn 1557 M’phunzitsi, ndinu mudziwitse ine
  • Hymn 453 Tiana ta Ambuye tili
  • Hymn 472 Amakumbukira zonse
  • Hymn 964 Kodi simuona njira,
  • Hymn 1740 Yesu, ndi chifundo chanu
  • Hymn 909 Ife tikondwera, ife tikondwera,
  • Hymn 516 Zitsamba zakuyera
  • Hymn 1129 Mbuyanga Yesu, ndikapanda Inu
  • Hymn 829 Titamadi ‘Tate,
  • Hymn 719 Anu Mbuye ndifetu!
  • Hymn 697 Zolengedwa zonse zidze
  • Hymn 1732 Anapachikidwatu,
  • Hymn 997 Mawu ake atipatsa
  • Hymn 428 Tiyandika, Mbuye,
  • Hymn 121 Imbira!
  • Hymn 1523 Atisangalatsa,
  • Hymn 1337 Bvomerani, Bvomerani,
  • Hymn 548 Kale anthu m’kholamo
  • Hymn 80 Utsegule mtimawo,
  • Hymn 122 Musadziunjikire chuma cha padziko,
  • Hymn 1047 Ambuye, chotsani zonse zomwezo
  • Hymn 1772 Iye amakhutitsa
  • Hymn 1252 Pakukumbukira zanga
  • Hymn 1041 Zosauka unvomere,
  • Hymn 443 M’MAŴA tizifesa
  • Hymn 967 Mbuye, ndapangana
  • Hymn 625 Chaka chino mutipatse
  • Hymn 1382 E, chifundo chake chonse
  • Hymn 613 Dziko lonse nla Mulungu
  • Hymn 98 Ndidzamwona maso ndi maso
  • Hymn 1448 Yesu ndiye Bwenzi lanu,
  • Hymn 871 Tiphatikane tonsefe okonda Yesu Kristu;
  • Hymn 440 Yesu wakufatsa mtima

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version