Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 13 PAPHIRI ndi padambo,

  1. Home   »  
  2. Hymn 13 PAPHIRI ndi padambo,

Hymn 13 PAPHIRI ndi padambo,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 13 PAPHIRI ndi padambo,

 

PAPHIRI ndi padambo,
Ponsepo pali Mlungu;
Poyenda ife m’njira,
MpoYima pali Mlungu.
Kokwera Maganizo,
Komwe kuli Mlungu;
Kumwamba ndi pansipo,
Ponsepo pali Mlungu.

(Mulungu ali nane!)
(Ali nane, ali nane,
ali nane, ali nane, Aa!
Mulungu ali nane!)

Ndi maso Ambuyathu,
Apenyetsetsa ife;
Amadalitsa onse,
Okhulupi’ra Iye.
Amamva timbalame,
Naveka dziko lonse;
Sataya tizirombo,
Asunga zina zonse.

Okwaŵa pansi inu,
Oyenda m’madzi inu;
Oyesa dziko n’kwanu,
A m’mlengalenga inu.
Nonsenu ntchito zake,
Muwona tsiku n’tsiku;
Saleka kusamala,
Ndikudalitsa inu.

Nditama mphamvu yake,
Ya Mlungu yondizinga;
N’kafoka andilimbitsa,
N’kadwala andichiza.
Pakundisiya bwenzi,
Mulungu ali paja;
N’kaloŵa imfa ine,
Alipo Mlungu wanga.

Post navigation

Previous: Hymn 12 NDITAMATU Ambuyangayu,
Next: Hymn 14 MTIMA wanga uyamike,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1661 Ndimachitira
  • Hymn 975 Tiyeni, Akristu inu,
  • Hymn 1553 Mpume pa inetu, Mpweya wa Mulungu,
  • Hymn 723 Mundimvere, Mbuye wanga
  • Hymn 51 Mbuye dalitsani Afrika,
  • Hymn 1511 Mndidalitsere ‘ne
  • Hymn 971 Ndinu Mbusa wanga;
  • Hymn 1159 Mwalembedwa mukalata
  • Hymn 438 TIYAMIKE Ambuye,
  • Hymn 296 TIYENI Akhristu,
  • Hymn 412 MOYO uli pafupi,
  • Hymn 455 Mdileke kulimbna ndi
  • Hymn 264 Bvinabvina moyo wanga,
  • Hymn 437 MULUNGU wa Yakobo Inu, mdyetsa anthu anu,
  • Hymn 1782 Poyamba paja analenga
  • Hymn 155 UTHENGA wa Mulungu
  • Hymn 485 POMPANO pandikonda
  • Hymn 907 Dziko labwinotu, dziko labwinotu,
  • Hymn 274 E! tidzakomanansotu
  • Hymn 306 YAMBA ulendo mnzanga,
  • Hymn 1795 A! chikondi chachikulu
  • Hymn 21 Mbuye mtsitsimutse!
  • Hymn 425 AKRISTU ndi abale, tiziyenderana tonse,
  • Hymn 70 LAMBIRA, Mfumuyo,
  • Hymn 1240 Ndilikuva m’mtima mwanga
  • Hymn 160 MADALITSO ngati mvumbi,
  • Hymn 393 ZOPEREKA tiperekazi,
  • Hymn 1204 Ambuyanga Yesu,
  • Hymn 214 KUNALI munthu ku Yeriko,
  • Hymn 739 Ndilibe wondithangata ‘ne ‘yi,
  • Hymn 118 PANALI munthu amene,
  • Hymn 1746 Mwachimwemwe, mwachisoni,
  • Hymn 365 DZUŴA lapita,
  • Hymn 1013 Tizifesa m’dzuwa,
  • Hymn 1209 Mnyamata wake ndinetu,
  • Hymn 824 Yesu mutipatse
  • Hymn 785 Yehova adalitse ‘nu,
  • Hymn 980 Tiyeni ku nkhondo iyi,
  • Hymn 1097 Njira yanga sindidziwa,
  • Hymn 1740 Yesu, ndi chifundo chanu
  • Hymn 851 E, nthawi ya mamawayi
  • Hymn 337 PADZIKO pano tikhalira M’moyo wosauka;
  • Hymn 1272 Muyambe ntchito yanuyi,
  • Hymn 156 OKOMA ndiwo mawu
  • Hymn 592 Kuti m’Mwambamo
  • Hymn 211 Chakudya ichi ndi cha iwenso,
  • Hymn 51 PANTHAWI yakufa Ambuye,
  • Hymn 216 Ndi misozi ndi chisoni
  • Hymn 80 Utsegule mtimawo,
  • Hymn 361 AMBUYE munapatsa tsiku
  • Hymn 1547 Mtisangalatse m’zonse,
  • Hymn 121 Imbira!
  • Hymn 200 Ndi tsopano tilindira
  • Hymn 1158 Yesu ndiye Mbuye wanga,
  • Hymn 346 Aitana,
  • Hymn 328 Yesu ndiye mphamvu yanga,
  • Hymn 102 Mzimu ndi mtsogoleri
  • Hymn 1152 Pokonda Yesuyo, mtendere!
  • Hymn 1339 Musaope pokumbuka
  • Hymn 1858 Ha! Chikondi cha Mulungu,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version